Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,

  1. Home   »  
  2. Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,

Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,

 

IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,
Zachisautso chomwechili nkudza;
Cha nambala ya a sikisi atatu;
Kodi tidzapiliradi?

Kodi inu mayi mudzapiliradi
Kuyenda inu wausiwa.
Kodi inu bambo mudzapiliradi
Panthawi ya masautsowo?

Zizindikirozo zili kuwoneka,
Kutitu nkhondoyo yayandikadi;
Tisakhaletu odabwitsika konse,
Tilimbike kupemphera.

Tidzawona ena a ifetu zedi,
Tili kudindidwa pamphumi pathu;
Tidziwetu kuti sitinalembedwe,
Mayina m’buku mulibe.

Post navigation

Previous: Hymn 297 POKUMANA m’mayesero a dziko lino,
Next: Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 196 NDI inetu sinditha’yi
  • Hymn 928 Usalire; Mpulumutsi
  • Hymn 346 PEMPHERO ndiko kufuna,
  • Hymn 75 MBUYE, mutsaganetu
  • Hymn 304 POZUNZIDWA inu ponseponse
  • Hymn 1108 Khala chete mtima wanga,
  • Hymn 476 Mpaka ndabvala mbuu!
  • Hymn 632 Tsopano tipereka mapemphero athu ano,
  • Hymn 1300 Poyenda m’mdima bii,
  • Hymn 434 CHIKONDI cha Mulunguyo,
  • Hymn 1394 Paphiri ndi padambo
  • Hymn 344 ’TATE, ’Nu.
  • Hymn 1396 Ndi maso Ambuyathu
  • Hymn 1169 Mwazi wa Yesu
  • Hymn 691 Akukhala kunja,
  • Hymn 267 Usekere moyo wanga,
  • Hymn 846 Kristu wakuyeratu,
  • Hymn 947 Akristu tonsefe, tikondwe m’Dzikoli
  • Hymn 810 Tsopano lino kwada bii,
  • Hymn 293 LIMBA mtima mbale wanga
  • Hymn 602 Mpulumutsi wakukoma,
  • Hymn 55 Ambiri tikondwera mwa Yesu,
  • Hymn 1066 Uchimo unapachikidwa pomwe
  • Hymn 294 Yesu anali khanda
  • Hymn 814 Mutichiritse ifenso
  • Hymn 206 YESU, mulikundipempha
  • Hymn 58 PAMTANDAPO Ambuyeyo
  • Hymn 1565 Mufike monga ngati njiwa yamtenderewo,
  • Hymn 216 Ndi misozi ndi chisoni
  • Hymn 682 Tsatani Mbuye Yesuyo ndi mtanda wakewo;
  • Hymn 203 Pamtandapo, pamtanda,
  • Hymn 863 A! maliro m’Mpingo mwanu kulirira ‘balewo
  • Hymn 498 AMBUYE, mtidalitsetu,
  • Hymn 1814 Thupi lamwazi wathu’li
  • Hymn 890 Kumbuka ‘bale ako
  • Hymn 876 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 219 Mtenderewo wosanyenga
  • Hymn 49 Ndi ife akudziwa
  • Hymn 1202 Ndikhumba mtimawo
  • Hymn 1178 Mawu omwewo, nyimbo yomweyi,
  • Hymn 220 MULUNGU mundichitire chifundo,
  • Hymn 531 Pakubweranso Inu m’Ufumuwo
  • Hymn 1692 Timwimbire zomtamanda, Aleluya
  • Hymn 1817 Ndi m’munda muja chete, phee!
  • Hymn 327 NTCHITO yonse yakeyo
  • Hymn 432 KRISTU ndiye Mwala wathu,
  • Hymn 1039 Usafune chuma chokha,
  • Hymn 1270 Ndayesa kudzikonzadi,
  • Hymn 1594 Chikondano chakechi
  • Hymn 1536 Ndilira Mzimu leroli,
  • Hymn 713 Ambuye, Mwini zonsezi,
  • Hymn 292 NDIPULUMUTSENI Mbuye,
  • Hymn 1295 Ambuye, mwazi wanuwo
  • Hymn 397 Yesu Mbusa, mutimvere,
  • Hymn 319 NDIDZATANI ine,
  • Hymn 644 M’wasunge, m’wayendetse
  • Hymn 1087 “Khala mwa Ine,” Mbuye, ndifunitsa;
  • Hymn 1286 E, ndikukhulupirani,
  • Hymn 478 Ndife ana, mutikonda,
  • Hymn 585 Alanditsa,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version