Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,

  1. Home   »  
  2. Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,

Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,

 

IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,
Zachisautso chomwechili nkudza;
Cha nambala ya a sikisi atatu;
Kodi tidzapiliradi?

Kodi inu mayi mudzapiliradi
Kuyenda inu wausiwa.
Kodi inu bambo mudzapiliradi
Panthawi ya masautsowo?

Zizindikirozo zili kuwoneka,
Kutitu nkhondoyo yayandikadi;
Tisakhaletu odabwitsika konse,
Tilimbike kupemphera.

Tidzawona ena a ifetu zedi,
Tili kudindidwa pamphumi pathu;
Tidziwetu kuti sitinalembedwe,
Mayina m’buku mulibe.

Post navigation

Previous: Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
Next: Hymn 301 MBUYE, ndapangana

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1215 Ndimkonde Kristuyo,
  • Hymn 248 M’MENE ine ndisauka
  • Hymn 477 Mpulumutsi, Mbusa wathu,
  • Hymn 1596 Anamnyoza pansi pano,
  • Hymn 1325 Maiwe! Thanthwe long’ambikatu,
  • Hymn 835 Mukhale ndine, dzuwalo lalowa,
  • Hymn 278 TITHAŴIRENJI ifetu
  • Hymn 150 Ndisauka, sindiona;
  • Hymn 956 Mbuye munditsogolere,
  • Hymn 450 Koma usalole
  • Hymn 742 Tikadya phando zaka zonsezi,
  • Hymn 1234 Ati Yesu Mbuyeyo:
  • Hymn 10 TSOPANO linoli,
  • Hymn 175 Mlungu mverani, mphamvu patseni,
  • Hymn 1523 Atisangalatsa,
  • Hymn 1116 Kwawo kwa Mbuyako
  • Hymn 787 Mzimu Wakuyera
  • Hymn 166 NDICHITENJI kukapeza
  • Hymn 756 Sindili woyenera ‘ne,
  • Hymn 817 Tibvomereze,
  • Hymn 186 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 1563 Mufike monga nyali younika m’mtimamo,
  • Hymn 1542 Titamire nthawi zonse
  • Hymn 1041 Zosauka unvomere,
  • Hymn 330 Yesu ndiye Mtsogoleri
  • Hymn 673 Mbwere Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 1303 Aa! Mulungu wanga,
  • Hymn 1551 Mukhale m’kati mwathu,
  • Hymn 805 Madzulo ano mkhaletu
  • Hymn 192 ZAKEYU mkulu wa misonkho,
  • Hymn 466 Yesu, muli pa chimpando
  • Hymn 663 Anyamata a Mulungu,
  • Hymn 1313 Zindichulukirazi
  • Hymn 34 Yesu Mbuyetu, mwafera
  • Hymn 899 ‘Tate wa Kumwambako,
  • Hymn 1787 Mulungu wanga ndiye wachifundo
  • Hymn 299 “Posunga nkhosa ife
  • Hymn 407 Zochimwa sizilowako,
  • Hymn 229 POYAMBAPO ndakondwadi.
  • Hymn 675 Pamaiko pali mdima,
  • Hymn 1386 Ndi chifundo atipenya
  • Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;
  • Hymn 1714 Tiyeni, dzalireni nane,
  • Hymn 180 MALO alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 1619 Adzabwera,
  • Hymn 272 Ankhondowo poona
  • Hymn 1687 Alonda onsewo
  • Hymn 372 DZUŴA la Mulungu
  • Hymn 1085 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini mphamvu,
  • Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,
  • Hymn 448 CHIFUKWA cha zokoma mtima zonse zaulelezo,
  • Hymn 166 Yendani, Munthu Wachisoni,
  • Hymn 1142 Tidzathawira kuti ‘fe
  • Hymn 356 Tinafena m’nyanjamo,
  • Hymn 706 Tisaiwalire ‘bale
  • Hymn 837 Koma kalelo mnakhalitsa pano,
  • Hymn 1795 A! chikondi chachikulu
  • Hymn 450 YESU, munditsogoza
  • Hymn 253 Adzakhala pampandopo
  • Hymn 370 Pakuti Mbuye Mlunguyo

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version