Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 296 TIYENI Akhristu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 296 TIYENI Akhristu,

Hymn 296 TIYENI Akhristu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 296 TIYENI Akhristu,

 

TIYENI Akhristu,
Nkhondo tigwire;
Yesu Mbuye wathu
Atitsogolera.
Mfumu yathu mwini
Atipatsa moyo;
Taonanitu mbendera
Yailoŵa nkhondo!

Tiyeni Akristu,
Nkhondo tiigwire;
Yesu Mbuye wathu
Atitsogolera

Nkhondo ya Satana
Idzakuthaŵani;
Tiyeni Akristu,
Kaipambaneni.
Idzanjenjemera
Mukapfu’litsatu;
Imbitsanitu anzathu,
Mau mukwezetse.

Mpingo wa Mulungu
Uli ngati nkhondo;
Titsagane nawo
Ana a Mulungu.
Sitipatukana,
Ndifetu amodzi;
Ch’yembekezo, chikondano,
Chonse ndi chimodzi.

Zonse zapadziko
Zidzamalizira,
Koma mpingo wake
Uli chikhalire;
Udzakhala ndithu
Mphamvu za Satana,
Yesu analonjezetsa,
Mawuwo sakana.

Tiyeni anzathu
Tizithandizana;
Imbirani nafe
Nyimbo zopambana
Kristu ayenera
Mphamvu ndi ulemu;
Komwe kuli Yesu.

Post navigation

Previous: Hymn 295 AMBUYE wa Kumwamba,
Next: Hymn 297 POKUMANA m’mayesero a dziko lino,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 645 Kristu ndiye mwala wathu,
  • Hymn 1148 Ndiimba mumtima mokondwa
  • Hymn 900 Mutipatse leroli
  • Hymn 297 POKUMANA m’mayesero a dziko lino,
  • Hymn 969 Akathira nsembe
  • Hymn 458 Anyamata inutu,
  • Hymn 415 Tidzalandirabe komwe
  • Hymn 16 Chikhulupiriro chathu
  • Hymn 1639 Aleluya, aleluya,
  • Hymn 45 IFE timakufunani
  • Hymn 1257 Mtanda m’mtima ndiyang’na,
  • Hymn 1437 Yesu ndi wokonda;
  • Hymn 320 Ambuye, wakuti ndi mwaziwo
  • Hymn 16 MTIMA wanga lemekeza,
  • Hymn 1252 Pakukumbukira zanga
  • Hymn 1479 Ndi Yesu yemwe kalelo
  • Hymn 1593 Wina atikonda ife,
  • Hymn 1509 Mkate wamoyowo
  • Hymn 908 Ndikonda kuganizirabe
  • Hymn 327 NTCHITO yonse yakeyo
  • Hymn 1528 Naye Mzimu mndiphunzitse
  • Hymn 1139 Namondwe akawombabe,
  • Hymn 1273 Ndasiya zonse ndi Yesu kalelo,
  • Hymn 246 NAMONDWE akawombabe,
  • Hymn 359 Tonse timyamiketu,
  • Hymn 687 Bukitsani mawunso
  • Hymn 1221 Bwenzi ndinamkomanayo,
  • Hymn 159 Kamwana Yesu ‘nabadwa,
  • Hymn 1364 Uzani zamphamvu,
  • Hymn 1147 Khalani duu! Pakufa ifetu,
  • Hymn 1060 Mubwere, Mzimu wa mpumulo
  • Hymn 919 ‘Tate, mwa kusunga kwanu
  • Hymn 1072 Mudzaze Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
  • Hymn 193 THANTHWE long’ambikatu,
  • Hymn 483 Ndife akuchoka,
  • Hymn 1769 Ndiye amachitira
  • Hymn 216 Ndi misozi ndi chisoni
  • Hymn 342 Ambiri,
  • Hymn 584 Ndi angelo,
  • Hymn 1068 Ambuye, thandizenitu
  • Hymn 200 YESU mundimve, ndikuliratu,
  • Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,
  • Hymn 1458 Satana ndi unyolo
  • Hymn 417 M’manja a Yesu wanga
  • Hymn 87 Aleluya, mwandigula,
  • Hymn 125 ODALA ali iwo,
  • Hymn 108 MBUYE wondipulumutsa,
  • Hymn 1169 Mwazi wa Yesu
  • Hymn 238 MULUNGU wanga,
  • Hymn 233 M’mene ndapenya mwazi wa
  • Hymn 344 M’watame,
  • Hymn 911 Mokhala mokhamokha
  • Hymn 897 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 963 Aulendo, munka kuti
  • Hymn 364 DZUŴA lapitira,
  • Hymn 876 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 1434 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 156 Yesu Mbuye, onani
  • Hymn 201 NDILINKUDZA kwa Ambuye,
  • Hymn 743 Mudze, anthuni, talawani ‘nu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version