Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 285 DZIKO lino lapansi,

  1. Home   »  
  2. Hymn 285 DZIKO lino lapansi,

Hymn 285 DZIKO lino lapansi,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 285 DZIKO lino lapansi,

 

DZIKO lino lapansi,
Moyo ndi wovuta;
Nthawi zina kuseka,
Nthawi zina kulira;
Komatu Ambuye wathu,
Amatisamalira;
Mbale wanga pilira.

Pilira, pilira, mbale wanga pilira,
Dziko lino ndi lovuta
Mbale wanga pilira;
Linadana naye Mwana wa Mulungu,
Mbale wanga pilira.

Zabwino zimabwera,
Ndipo zimapita;
Dziwa kuti Ambuye,
Afunitsa iwedi;
Kuti ugwiretu ntchito,
Yakeyi m’dziko lino;
Mbale wanga pilira.

Tsikulo lilinkudza,
Lomwe Mbuye Yesu;
Adzanena kwa iwe,
Bwera upumuletu;
Kuzovuta ndi zowawa,
Zam’dziko lapansili;
Mbale wanga pilira.

Post navigation

Previous: Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
Next: Hymn 301 MBUYE, ndapangana

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 243 Mtima wanga udzakondwera,
  • Hymn 703 Dzuwa, madzi, kudya, mpweya,
  • Hymn 1835 Mtima wanga lemekeza
  • Hymn 899 ‘Tate wa Kumwambako,
  • Hymn 1585 Dzina ili ndi lokoma
  • Hymn 1840 Ndiye M’busa wanga,
  • Hymn 106 Ife, tapulumukadi,
  • Hymn 1289 Ndinasokeratu kutaliko,
  • Hymn 271 Pomwalira Mbuyeyo
  • Hymn 773 Mtsinje woyerawo
  • Hymn 560 Kale m’mzinda wachifumu
  • Hymn 390 Lalowa dzuwa, kwada bii!
  • Hymn 933 M’mene imfa yathu idza,
  • Hymn 569 Tiimbe ndi kulalikira
  • Hymn 1427 Penyetsetsa Yesu,
  • Hymn 358 Dzina lake Yesuyo,
  • Hymn 1773 Monga anapangana
  • Hymn 706 Tisaiwalire ‘bale
  • Hymn 1131 M’mene ine ndisauka
  • Hymn 1255 Chitha nchiani kund’yeretsa?
  • Hymn 1403 ‘Mvani liwu lomwe
  • Hymn 1483 Pakupempha ife pano,
  • Hymn 1104 Mndisungire mtima wanga,
  • Hymn 1343 M’dzina la Yesuyo
  • Hymn 1136 Mulungu anditsogolera
  • Hymn 1563 Mufike monga nyali younika m’mtimamo,
  • Hymn 68 Kwathu ndidzaimba nyimbo
  • Hymn 417 M’manja a Yesu wanga
  • Hymn 1817 Ndi m’munda muja chete, phee!
  • Hymn 1288 Yesu mundimve, ndikuliratu,
  • Hymn 926 Mbale wako unamkonda,
  • Hymn 1628 Dziko lino linaona
  • Hymn 330 Yesu ndiye Mtsogoleri
  • Hymn 378 KWEZANI mitu yanuyo,
  • Hymn 824 Yesu mutipatse
  • Hymn 128 ANTHU m’maiko onse
  • Hymn 12 NDITAMATU Ambuyangayu,
  • Hymn 1328 Ndani afuna kunkako
  • Hymn 689 Anapeza Mwana
  • Hymn 35 KODI mwaona chiyani,
  • Hymn 192 ZAKEYU mkulu wa misonkho,
  • Hymn 547 Anatikondakonda ‘Ye.
  • Hymn 1641 Pakufika asonkhanitsa
  • Hymn 483 Ndife akuchoka,
  • Hymn 142 Kukondwa kwa wodwalayo
  • Hymn 1287 Wadza Yesu wandidzoza,
  • Hymn 45 Malawi dziko lokongola,
  • Hymn 1782 Poyamba paja analenga
  • Hymn 1091 Mulamulire mtima, Yesu,
  • Hymn 1062 Mkatero ndidzayenda m’njira
  • Hymn 489 Yesu, ndikabwera,
  • Hymn 1843 Chigwa choopsacho cha imfa ndikachilowera,
  • Hymn 711 Ife tonse tichenjere
  • Hymn 1613 A Mulungu
  • Hymn 1056 Mkhalidwe wanu mundipatse,
  • Hymn 691 Akukhala kunja,
  • Hymn 1438 Yesu akukonda,
  • Hymn 1695 Pokumbukira mtandawo
  • Hymn 289 ANATILEMBA Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 490 Yesu, ndikabwera

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version