Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 285 DZIKO lino lapansi,

  1. Home   »  
  2. Hymn 285 DZIKO lino lapansi,

Hymn 285 DZIKO lino lapansi,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 285 DZIKO lino lapansi,

 

DZIKO lino lapansi,
Moyo ndi wovuta;
Nthawi zina kuseka,
Nthawi zina kulira;
Komatu Ambuye wathu,
Amatisamalira;
Mbale wanga pilira.

Pilira, pilira, mbale wanga pilira,
Dziko lino ndi lovuta
Mbale wanga pilira;
Linadana naye Mwana wa Mulungu,
Mbale wanga pilira.

Zabwino zimabwera,
Ndipo zimapita;
Dziwa kuti Ambuye,
Afunitsa iwedi;
Kuti ugwiretu ntchito,
Yakeyi m’dziko lino;
Mbale wanga pilira.

Tsikulo lilinkudza,
Lomwe Mbuye Yesu;
Adzanena kwa iwe,
Bwera upumuletu;
Kuzovuta ndi zowawa,
Zam’dziko lapansili;
Mbale wanga pilira.

Post navigation

Previous: Hymn 284 MAVUTO ndi ambiri,
Next: Hymn 286 ZOVUTA zoopsya ndi zosaukazi

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 433 MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku
  • Hymn 383 Zokoma ndi zakuyanja
  • Hymn 463 Yesu atiuza tiwale ‘fe,
  • Hymn 1843 Chigwa choopsacho cha imfa ndikachilowera,
  • Hymn 1431 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 1769 Ndiye amachitira
  • Hymn 1046 Ndiyere mbuu! E, ndiyere mbuu!
  • Hymn 1591 Sizitha ntchito zangazo,
  • Hymn 245 Ngakhale kuthengo
  • Hymn 986 Tiyeni anzathu
  • Hymn 8 MITAMBO inu yakumwambako
  • Hymn 66 Chisomocho chachotsadi
  • Hymn 1493 Mbiri yakalelomwe
  • Hymn 1248 ‘Dzanitu Wamphamvu yonse,
  • Hymn 576 Kondwerani nonsenu
  • Hymn 1557 M’phunzitsi, ndinu mudziwitse ine
  • Hymn 1128 Mbuyanga Yesu, mundisunge ine
  • Hymn 753 Getsemane ndionako
  • Hymn 402 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 1582 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 1238 M’mene ndifa inedi,
  • Hymn 426 Mpulumutsi Yesu,
  • Hymn 271 Pomwalira Mbuyeyo
  • Hymn 1344 Yamba ulendowo
  • Hymn 254 PAMENE ndisawuka,
  • Hymn 1579 Akhala mafumu
  • Hymn 1255 Chitha nchiani kund’yeretsa?
  • Hymn 1719 Ku Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 1440 Yesu alindira,
  • Hymn 407 Zochimwa sizilowako,
  • Hymn 1648 Uko Kumwambako Mbuyangayo
  • Hymn 197 NDIKHULUPIRA’Nu,
  • Hymn 1534 Mukonze mtima wangawu,
  • Hymn 1217 Chisoni chonsecho
  • Hymn 1802 Mulungu anatuma,
  • Hymn 699 Inu wakudzatu
  • Hymn 941 Ndi Mbuyeyo tikhalamo,
  • Hymn 526 Mnandidzera, Ambuye,
  • Hymn 72 Mayi watsogola ku Ulemerero,
  • Hymn 1472 Ona! Ona! Onatu!
  • Hymn 1434 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 237 SINDINANYENGEDWA konse
  • Hymn 738 Mommuno, Mbuye, mkate wanuwu,
  • Hymn 485 POMPANO pandikonda
  • Hymn 1425 Apempha malo Ambuye;
  • Hymn 1427 Penyetsetsa Yesu,
  • Hymn 1022 Mbuye, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 1299 Mzimu mndipatseko,
  • Hymn 1097 Njira yanga sindidziwa,
  • Hymn 455 Mdileke kulimbna ndi
  • Hymn 742 Tikadya phando zaka zonsezi,
  • Hymn 142 MULUNGU aŵakonda anthu
  • Hymn 831 Mundikumbutse, ndikapanda tulo, za Kumwambako;
  • Hymn 790 Zimbalame zonsezi
  • Hymn 1633 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 472 Amakumbukira zonse
  • Hymn 1525 Mbuye, mtiphunzitse
  • Hymn 48 Ngakhale alemera
  • Hymn 1454 Ambuye, musendeze
  • Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version