Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,

Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,

 

M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,
Ndiyenderane nanu;
E, nditsamire pa ‘nu Yesu,
Panjira yonseyi.

Ndiwonetsere kuunika,
Kokoma kwanu Yesu!
Yabwino mbiri ndibukitse,
Yokondweretsayo.

Chitsime chakuyera ine,
Ndifananetu nacho;
Mundigwiritse ntchito zanu,
E, zanu zokhazo.

Mulamulire mtima, Yesu,
Ndi chifuniro changa;
Mulowe mwanga ngati Mfumu;
Kuti ndimvere ‘Nu.

Ndimamva njala kuno, Yesu,
Yakufunitsa Inu;
Kumwamba kwanu ndikukhumba.
Kukondwa nanuko.

Post navigation

Previous: Hymn 260 ODALA ndi onsewo,
Next: Hymn 262 “KHALA mwa Ine,” Yesu anatero;

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 752 Chakudya chakumwambachi
  • Hymn 1383 Dzina lake tibukitsa,
  • Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,
  • Hymn 1751 Mbuye ngwodalitsika,
  • Hymn 1567 Mubwere Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 1029 Nkhawa tilibe; Yesuyo
  • Hymn 146 Inu ndidzatama
  • Hymn 15 Mbuye, chifundo chanu chitigwere
  • Hymn 791 Anthu opembedzawo
  • Hymn 341 Ayenda,
  • Hymn 100 M’mene masautso onse,
  • Hymn 388 MOMMUNO, Mbuye tionanetu,
  • Hymn 419 ANYAMATA a Mulungu,
  • Hymn 440 Yesu wakufatsa mtima
  • Hymn 771 Tsopano alandira
  • Hymn 1688 Mulibe m’mandamu,
  • Hymn 556 Ndani pachimpandocho
  • Hymn 59 IMVANI uthenga,
  • Hymn 1101 Ngati mtima sumakonda
  • Hymn 798 M’nyumba yanu, Mlungu, ‘yi
  • Hymn 672 Mbwere Yesu Mwini moyo,
  • Hymn 189 Koma Iye wandipeza;
  • Hymn 191 Sindifuna Mbuye wina,
  • Hymn 1492 Sakukanani Yesudi,
  • Hymn 552 Analira ndaniyo
  • Hymn 1518 Zonse mwazilembamo,
  • Hymn 302 NDIDZE pafupi pa
  • Hymn 1834 Chisomo ndi zokoma zake sizileka konse;
  • Hymn 153 NDAKUMANA ndi bwenzi lokomalo,
  • Hymn 753 Getsemane ndionako
  • Hymn 5 Inu Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 1180 Ndine kapolo wa Mbuye wanga;
  • Hymn 1593 Wina atikonda ife,
  • Hymn 1666 Yesu, ndinutu chitsime
  • Hymn 353 ATATE Wamkulu ndi Wamphamvu zonse,
  • Hymn 10 Kristu Mfumuyo yaulemerero!
  • Hymn 1152 Pokonda Yesuyo, mtendere!
  • Hymn 211 Chakudya ichi ndi cha iwenso,
  • Hymn 822 Dzuwa lapitira,
  • Hymn 180 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 584 Ndi angelo,
  • Hymn 1330 Etu, zilira konseko
  • Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,
  • Hymn 1752 Napulumutsa tonse
  • Hymn 479 Munanena mulandira
  • Hymn 1475 Anathera pamtanda zintchito zonsezi
  • Hymn 551 Ndani kodi Munthuyo
  • Hymn 63 POKUMBUKIRA mtandawo
  • Hymn 306 YAMBA ulendo mnzanga,
  • Hymn 988 Ndikhumba Mzimu wanu
  • Hymn 1139 Namondwe akawombabe,
  • Hymn 838 E, tsiku lonse Inu ndifunitsa;
  • Hymn 332 Perekani mtima wanu,
  • Hymn 910 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 229 Woba wakufa ‘napenya
  • Hymn 1548 Mtitsitsimutse ife
  • Hymn 1304 Ndi ine sizitheka ‘yi
  • Hymn 1025 Ndikamayenda m’mdimamo,
  • Hymn 170 M’manda naukamo
  • Hymn 1584 Konda dzinalo la Yesu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version