Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 258 MWA ine, moyo wanga ndi Yesu

  1. Home   »  
  2. Hymn 258 MWA ine, moyo wanga ndi Yesu

Hymn 258 MWA ine, moyo wanga ndi Yesu

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 258 MWA ine, moyo wanga ndi Yesu

 

MWA ine, moyo wanga ndi Yesu
(Yesu) Yemwe anafera ine,
Ndiye anandiwombola;
Yesu, Yesu.

Mwazi wake ndi chitsime changa,
(Yesu) Pamene ndikasambamo
Zochimwa zanga zidzatha;
Yesu, Yesu.

Yesu Mfumu, ine ndingadzafe
(Yesu) ngati mundisiya ndekha,
Kukhala ndekha sinditha;
Yesu, Yesu.

Yesu Mfumu, ine ndisekere
(Yesu) Inu Mpulumutsi wanga
Pamene mukhala nane;
Yesu, Yesu.

Post navigation

Previous: Hymn 257 NJIRA yanga sindiziŵa,
Next: Hymn 259 CHISOMO chodabwitsacho,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 767 Munali mwana, Yesu ‘Nu
  • Hymn 371 Mulungu, anthu ‘fe
  • Hymn 515 Kuphiri la ‘Zitona,
  • Hymn 187 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,
  • Hymn 1718 Ona chikondi cha Mulungu,
  • Hymn 1805 Anafa m’mvula muja
  • Hymn 1336 Mwamva mawu a Mulungu;
  • Hymn 280 Tisonkhane tonsefe,
  • Hymn 909 Ife tikondwera, ife tikondwera,
  • Hymn 597 Mlungu ali nane
  • Hymn 867 Akristu ndi abale, tiziyenderana tonse,
  • Hymn 1185 Imfa ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 227 NDIM’KONDE Kristuyo,
  • Hymn 788 Moyo watsopano
  • Hymn 897 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 285 DZIKO lino lapansi,
  • Hymn 1619 Adzabwera,
  • Hymn 54 MUNTHU wazisoniyo,
  • Hymn 369 LERO mwatipatsa moyo,
  • Hymn 1258 Zonse zina sizikwana,
  • Hymn 97 Maso ndi maso ndi Kristu,
  • Hymn 329 Yesu atonthoza mtima
  • Hymn 465 ANA a Yerusalemu
  • Hymn 537 Aleluya! Aleluya!
  • Hymn 1270 Ndayesa kudzikonzadi,
  • Hymn 1146 Khalani duu! Pakufa mnzathuyo,
  • Hymn 1463 Zoipa zakhululukidwa,
  • Hymn 941 Ndi Mbuyeyo tikhalamo,
  • Hymn 1575 Tifuna kuti komweko
  • Hymn 459 KALE anthu m’kholamo,
  • Hymn 1318 Ndibwera kwa Ambuyeyo,
  • Hymn 1079 Khalatu woyera,
  • Hymn 1812 Kuzani Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 1148 Ndiimba mumtima mokondwa
  • Hymn 1607 Yesu, dzina ndi lomweli
  • Hymn 1358 Lemekeza Mfumu yathu,
  • Hymn 645 Kristu ndiye mwala wathu,
  • Hymn 422 Kwathu nkopambana,
  • Hymn 106 Ife, tapulumukadi,
  • Hymn 539 Anafika ‘kazi omwe
  • Hymn 1620 Aleluya,
  • Hymn 72 Mayi watsogola ku Ulemerero,
  • Hymn 1143 Tikhale ndithu pomwepo;
  • Hymn 43 GETSEMANI, Getsemani,
  • Hymn 276 MKRISTU, ulimbike
  • Hymn 172 Imfa yalephera
  • Hymn 414 Ana ake adzapuma
  • Hymn 1702 Pakufa ine Mbuye
  • Hymn 741 Chakudya ichi chidzapita du,
  • Hymn 183 Mlemekeze, bukitsani,
  • Hymn 260 ODALA ndi onsewo,
  • Hymn 382 M’wabatize anzathuwa,
  • Hymn 177 Tate, ndili mwana wanu,
  • Hymn 1125 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 1386 Ndi chifundo atipenya
  • Hymn 1168 Aleluya, muyenera!
  • Hymn 1569 Mtima wodetsa mukonzere,
  • Hymn 1331 Yesu wathu Mbuyeyo
  • Hymn 343 ZOKOMA ndithu nthaŵizi

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version