Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 247 MULUNGU anditsogolera,

  1. Home   »  
  2. Hymn 247 MULUNGU anditsogolera,

Hymn 247 MULUNGU anditsogolera,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 247 MULUNGU anditsogolera,

 

MULUNGU anditsogolera,
Ndapumula m’mtimamo;
Ayang’anira njira zanga
Nsiku zanga zonsezo.

Mulungu anditsogolera
Nsiku zanga zonsezo;
Ndidzatsatira Mbuye wanga
M’njira mwake momwemo.

Masiku ena pali mdima,
Ndivutidwa m’mtimamo;
Masiku ena ndikondwera
Ndi zabwino zangazo.

Masiku onse m’mtima mwanga
Ndili ndi mtenderewo,
Chifukwa ndimakhulupira
Mtsogoleri wangayo.

Post navigation

Previous: Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
Next: Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 563 Ndipo Mwana uyu Yesu
  • Hymn 217 CHIPULUMUTSO chathu chayandika,
  • Hymn 1241 Ati: Mwana, kumbukira
  • Hymn 1283 Yesu ndikhulupirira
  • Hymn 297 Anapita nasiya
  • Hymn 675 Pamaiko pali mdima,
  • Hymn 1606 Yesu, dzina lakufatsa,
  • Hymn 1558 Wosangalatsa, ine ndikalira
  • Hymn 1852 Mbuye ndamva mwawazira
  • Hymn 508 Mzimu Woyera akhala mwa ine,
  • Hymn 1305 Ndi ine pondibvutapo
  • Hymn 148 PAKUPEMPHA ife pano,
  • Hymn 168 Yendani mwaulemerero,
  • Hymn 962 Inde Mbuye, tibweradi,
  • Hymn 112 Pangano lake m’mwaziwo
  • Hymn 1651 Kwa Mulungu m’Mwambamo
  • Hymn 1443 Ambuye Yesu anatsira
  • Hymn 947 Akristu tonsefe, tikondwe m’Dzikoli
  • Hymn 1735 “Sezani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 1325 Maiwe! Thanthwe long’ambikatu,
  • Hymn 1610 Waleka koronayo,
  • Hymn 188 Ine ndili ndi manyazi
  • Hymn 840 Ambuye munapatsa tsiku
  • Hymn 132 MVERA mtima wanga ’we
  • Hymn 1474 Zilepheradi zonse kugula moyowo,
  • Hymn 1720 Padzanja lachifundolo
  • Hymn 631 Mulungu wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 310 Tafika kwa inu mutiunikire,
  • Hymn 469 Lero mkhale nafe ndithu,
  • Hymn 654 Ndilimbikitse, Mbuye, nji!
  • Hymn 79 Mlendo ali pakhomo,
  • Hymn 1257 Mtanda m’mtima ndiyang’na,
  • Hymn 318 TINALI ambiri ife,
  • Hymn 195 Bwinoli tipita,
  • Hymn 500 >AMEN, Amen, Amen.
  • Hymn 378 KWEZANI mitu yanuyo,
  • Hymn 1532 Mubwere kuno Mzimu ‘Nu,
  • Hymn 1451 Okoma ndiwo mawu
  • Hymn 1714 Tiyeni, dzalireni nane,
  • Hymn 536 Ana inu, myamikeni
  • Hymn 969 Akathira nsembe
  • Hymn 1411 Yesu akuitanani
  • Hymn 269 NDILIRA ine kukayenda
  • Hymn 102 Mzimu ndi mtsogoleri
  • Hymn 1814 Thupi lamwazi wathu’li
  • Hymn 1708 Pakugomedwapo
  • Hymn 978 Mtima wanu wonse ndithu
  • Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira
  • Hymn 1530 Mndilimbitse ndipirire
  • Hymn 496 Yesu Mbuye ‘Nu wabwino,
  • Hymn 44 Mlungu dalitsani Malawi,
  • Hymn 1191 Ambuyanga Yesu
  • Hymn 1422 Abwenzi ‘nu, abwenzi ‘nu,
  • Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda
  • Hymn 1611 Nadzuka m’mandamo
  • Hymn 1187 M’mitima mwathu mwakhala mbee!
  • Hymn 449 Mzimu wakuipa
  • Hymn 2 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 1723 Unakhetsedwa mwazi do!
  • Hymn 1678 Yesu nkana saoneka, Aleluya,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version