Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 247 MULUNGU anditsogolera,

  1. Home   »  
  2. Hymn 247 MULUNGU anditsogolera,

Hymn 247 MULUNGU anditsogolera,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 247 MULUNGU anditsogolera,

 

MULUNGU anditsogolera,
Ndapumula m’mtimamo;
Ayang’anira njira zanga
Nsiku zanga zonsezo.

Mulungu anditsogolera
Nsiku zanga zonsezo;
Ndidzatsatira Mbuye wanga
M’njira mwake momwemo.

Masiku ena pali mdima,
Ndivutidwa m’mtimamo;
Masiku ena ndikondwera
Ndi zabwino zangazo.

Masiku onse m’mtima mwanga
Ndili ndi mtenderewo,
Chifukwa ndimakhulupira
Mtsogoleri wangayo.

Post navigation

Previous: Hymn 246 NAMONDWE akawombabe,
Next: Hymn 248 M’MENE ine ndisauka

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 747 Tadzanitu, okhulupiradi,
  • Hymn 1375 Ndi anamwali obvekedwa mbuu!
  • Hymn 1807 Chithawa m’talitali
  • Hymn 932 Munabvala thupi lathu,
  • Hymn 206 Uzanitu abale,
  • Hymn 392 Chimwemwe chomwe mpatseko
  • Hymn 930 Leroli chisoni chokha,
  • Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,
  • Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,
  • Hymn 492 Yesu Mbuye ‘Nu wafatsa
  • Hymn 934 Mnamwalira Inu paja,
  • Hymn 1457 Ndidziwa kuti Yesu
  • Hymn 743 Mudze, anthuni, talawani ‘nu
  • Hymn 194 Kuli dziko labwino m’Mwamba
  • Hymn 1544 Wakunga mwana ine,
  • Hymn 1550 Kutiyeretsa m’mtima
  • Hymn 928 Usalire; Mpulumutsi
  • Hymn 1018 Yesu afuna iwe unnke kwawoko,
  • Hymn 672 Mbwere Yesu Mwini moyo,
  • Hymn 1655 Mbuye Yesu,
  • Hymn 1486 M’dziko lino pansi pano
  • Hymn 269 NDILIRA ine kukayenda
  • Hymn 1790 Imfa ya anthu ake imkomera,
  • Hymn 949 Mundiwalire m’njira mwangamo,
  • Hymn 224 LINDIKOMERA dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 313 MUNDIŴALIRE m’njira mwangamo,
  • Hymn 29 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 1632 Ndi chiyembekezo ichi
  • Hymn 1566 Mufike monga ngati mphepo yokokomayo,
  • Hymn 785 Yehova adalitse ‘nu,
  • Hymn 954 Mbuye andipeza lero,
  • Hymn 1411 Yesu akuitanani
  • Hymn 174 Haya, anzathu, itilinda nkhondo;
  • Hymn 25 “Akaleka amake
  • Hymn 494 YESU Mbusa, mutimvere,
  • Hymn 660 Tumizani kuunikako,
  • Hymn 617 Nthawi yina Mbuyeyu
  • Hymn 1271 Onani Mbuye ndigonja,
  • Hymn 662 Tisaleme pakuchita zabwinozi,
  • Hymn 59 Tinachoka munjira ya imfa,
  • Hymn 286 ZOVUTA zoopsya ndi zosaukazi
  • Hymn 736 Mndidyetse m’chipululu
  • Hymn 61 A! MUTU wakuyera,
  • Hymn 1204 Ambuyanga Yesu,
  • Hymn 1363 Tamani Ambuye,
  • Hymn 1684 Mbuye mabala anu olimba
  • Hymn 511 Ntchito zake zatha,
  • Hymn 1236 Mbuye ndimva leroli
  • Hymn 1313 Zindichulukirazi
  • Hymn 777 Mulungu ali muno,
  • Hymn 1062 Mkatero ndidzayenda m’njira
  • Hymn 251 Kuli chimwemwe m’dzuwalo
  • Hymn 192 ZAKEYU mkulu wa misonkho,
  • Hymn 798 M’nyumba yanu, Mlungu, ‘yi
  • Hymn 274 E! tidzakomanansotu
  • Hymn 1377 Ndi amithenga akumwambako,
  • Hymn 1412 Imfa idzafika msanga;
  • Hymn 1105 Khala chete mtima wanga
  • Hymn 1368 Mitambo inu yakumwambako,
  • Hymn 720 Anu Mbuye ndifetu!

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version