Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,

  1. Home   »  
  2. Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,

Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,

 

TIMVE za anamwali khumi,
Okonzeka mosiyana;
Asanu anali opusa zedi,
Ena anachenjeradi.

Asanu anatenga mafuta padera,
Iwowa anachenjera,
Asanu sanatenge mafuta adera,
Iwowa anapusadi.

Mkwati pamene anafika,
Pakati pa usikuwo,
Asanu osatenga mafutawo,
Sanathe kulowa m’nyumba.

Tisakhale ngati opusa,
Osatenga mafutawo.
Tikhale ngatitu ochenjerawo,
Titenge mafuta athu.

Mbale ukhale wochenjera,
Pakulapa zoipazo;
Pakukhulupiliratu Mulungu,
Kuti tikalowe M’mwamba.

Post navigation

Previous: Hymn 243 KONDWANI nonsenu,
Next: Hymn 245 KHALANI duu! Ambuye adzatu;

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 639 Mulungu mwa Atatu,
  • Hymn 1222 Bwenzi ndimamkomanayo
  • Hymn 459 KALE anthu m’kholamo,
  • Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu
  • Hymn 31 Tamandani mbuye,
  • Hymn 1020 Ngati umtsata Mpulumutsi wakoyo,
  • Hymn 288 Ndi maso athu awa nawo nganu,
  • Hymn 1010 Ndipo ngati ungolema,
  • Hymn 1373 Zamoyo zili m’thengo zonsezo,
  • Hymn 263 Mulungu wakwezekatu,
  • Hymn 1322 Ntchito zanga zonsezo
  • Hymn 334 KULI dziko labwino M’mwamba,
  • Hymn 799 Inu Mlungu kalelo
  • Hymn 326 Yesu, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 268 Potuluka m’mudzimo
  • Hymn 1187 M’mitima mwathu mwakhala mbee!
  • Hymn 1039 Usafune chuma chokha,
  • Hymn 664 Komwe asauka anthu
  • Hymn 830 Atate ndiyamika, mwandisamalira leroli;
  • Hymn 42 “SENZANI mtanda wanuwu,
  • Hymn 454 Kapena m’mtima ndimakwiya,
  • Hymn 825 Mpatse ana ‘ng’ono
  • Hymn 1497 Simbani mobwereza,
  • Hymn 976 Muyendenso kunka komwe,
  • Hymn 487 Yesu, ndikabwera
  • Hymn 1599 Inde, ndifuna kumvatu
  • Hymn 1225 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 1732 Anapachikidwatu,
  • Hymn 1398 Nditama mphamvu yake
  • Hymn 1586 Mbuye Yesu timtamanda
  • Hymn 122 KUNALI munthu wa Mlungu,
  • Hymn 450 YESU, munditsogoza
  • Hymn 1273 Ndasiya zonse ndi Yesu kalelo,
  • Hymn 1677 Zomkweza zili m’Mwamba,Aleluya
  • Hymn 581 Mtiphunzitse bwinotu,
  • Hymn 324 Walira Yesu pazobvutazo,
  • Hymn 570 Ndikhulupirira Yesu
  • Hymn 305 M’mwazi wake tisambamo;
  • Hymn 465 Yesu atiuza tiwale pa
  • Hymn 1243 Kodi mayi wobereka
  • Hymn 675 Pamaiko pali mdima,
  • Hymn 313 Muthire, Yesu, m’mtimanga
  • Hymn 235 ADALITSIKA munthuyo,
  • Hymn 1852 Mbuye ndamva mwawazira
  • Hymn 1424 Malo anachepa,
  • Hymn 37 Pozunzidwa inu ponseponsepo
  • Hymn 411 TAMVA mawu omwewo,
  • Hymn 226 Nditama mwaziwo!
  • Hymn 1266 E, chimwemwe chachikulu, N’taperekadi
  • Hymn 828 Ndidzukanso m’mawa,
  • Hymn 853 Pa tsikuli, Mbuyanga ‘Nu,
  • Hymn 269 NDILIRA ine kukayenda
  • Hymn 1662 Msandipitire, Yesu,
  • Hymn 741 Chakudya ichi chidzapita du,
  • Hymn 660 Tumizani kuunikako,
  • Hymn 41 Tiyeni, tiyeni,
  • Hymn 93 YAMIKANI dzina la Yesu Khrisituyo,
  • Hymn 892 Tilibe madalitso
  • Hymn 1111 Pamene ndilemedwa
  • Hymn 148 Ndisauka, ndimasowa

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version