Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,

  1. Home   »  
  2. Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,

Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,

 

TIMVE za anamwali khumi,
Okonzeka mosiyana;
Asanu anali opusa zedi,
Ena anachenjeradi.

Asanu anatenga mafuta padera,
Iwowa anachenjera,
Asanu sanatenge mafuta adera,
Iwowa anapusadi.

Mkwati pamene anafika,
Pakati pa usikuwo,
Asanu osatenga mafutawo,
Sanathe kulowa m’nyumba.

Tisakhale ngati opusa,
Osatenga mafutawo.
Tikhale ngatitu ochenjerawo,
Titenge mafuta athu.

Mbale ukhale wochenjera,
Pakulapa zoipazo;
Pakukhulupiliratu Mulungu,
Kuti tikalowe M’mwamba.

Post navigation

Previous: Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
Next: Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 259 CHISOMO chodabwitsacho,
  • Hymn 432 Ulendo ungoyamba
  • Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,
  • Hymn 1219 Bwenzi ndinamkomanayo
  • Hymn 403 NDIYIMBA ndi chimwemwe lero,
  • Hymn 1057 Ndilira ine kukayenda
  • Hymn 316 Ndikhazikike inetu,
  • Hymn 1232 Ambuye ndinu Mbusa, Bwenzi, ndi Wansembe wanga,
  • Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,
  • Hymn 1010 Ndipo ngati ungolema,
  • Hymn 216 Ndi misozi ndi chisoni
  • Hymn 709 Munthu aganize
  • Hymn 551 Ndani kodi Munthuyo
  • Hymn 83 MBUYEYO adzabwera,
  • Hymn 1261 Kale ndinakana Inu, Ndinathawatu;
  • Hymn 59 IMVANI uthenga,
  • Hymn 1666 Yesu, ndinutu chitsime
  • Hymn 11 NDI mitima yokondwera,
  • Hymn 995 Taya zako zochenjera,
  • Hymn 1120 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 1857 Ndinagona mwa zoipa,
  • Hymn 204 NDASIYA zonse ndi Yesu kalelo,
  • Hymn 1264 Chifuniro change, Mbuye, Ndiperekachi;
  • Hymn 1004 A! mizimu yakuipa
  • Hymn 729 Ndifuna kumva Inu,
  • Hymn 1415 Iye anatsika m’Mwamba,
  • Hymn 1521 Poyensedwa ife
  • Hymn 177 ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,
  • Hymn 389 Ambuye, mtidalitsetu,
  • Hymn 1541 Tionetseni tonsetu
  • Hymn 1017 Tisasungaluke ‘yi,
  • Hymn 1250 Mndilandire ine Mbuye
  • Hymn 1068 Ambuye, thandizenitu
  • Hymn 1015 Mbuye, mwatiuza ‘fe
  • Hymn 285 Ndipempha, Ambuye,
  • Hymn 865 Pakubweradi Woyesa tidzamlaka ifetu;
  • Hymn 1675 Lambira Mfumuyo
  • Hymn 124 PAMTANDAPO, pamtanda,
  • Hymn 911 Mokhala mokhamokha
  • Hymn 204 Kumandako, kumanda
  • Hymn 326 Yesu, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 76 E, MOYO wanga’we
  • Hymn 608 Maluwa abwino aphuka m’mapiri ndi m’madambomo,
  • Hymn 228 MWAKHULUPIRIRADI
  • Hymn 1533 Ndipatsa inu mtimawu,
  • Hymn 762 “Ndi thupi lopatsidwali
  • Hymn 558 Mwanayo wa Mulunguyo
  • Hymn 236 NDIDZIWITSITSA
  • Hymn 175 A! MBUSA wathu amvatu
  • Hymn 1224 Inde ndidzaimba nyimbo
  • Hymn 1294 Wakuba uja nachiona,
  • Hymn 470 YESU andikonda ine,
  • Hymn 1088 Mndiyandikitse nanu, Yesu,
  • Hymn 1397 Okwawa pansi inu,
  • Hymn 1038 Limbikani nonse
  • Hymn 257 Ndinasiya amayi,
  • Hymn 245 Ngakhale kuthengo
  • Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,
  • Hymn 1026 Inde nditaya chumacho,
  • Hymn 822 Dzuwa lapitira,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version