Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 215 TATE ndili mwana wanu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 215 TATE ndili mwana wanu,

Hymn 215 TATE ndili mwana wanu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 215 TATE ndili mwana wanu,

 

TATE ndili mwana wanu,
Nkana ndinachimwa,
Ndingolirira kwa Inu;
Khululukireni.

Machimo anga ngambiri
Osaŵerengeka,
Ndingoyang’ana kwa Inu;
Khululukireni.

Ndinachimwa poganiza
Ndi polankhulanso,
M’ntchito zanga ndachimwanso;
Khululukireni.

Ndinachita mphulupulu,
Ndinakunyozani,
M’ntchito zanga ndalephera;
Khululukireni.

Zonse ndinakonda kale
Ndi zopanda pake,
Sindinakhuta nazotu;
Khululukireni.

Post navigation

Previous: Hymn 200 YESU mundimve, ndikuliratu,
Next: Hymn 221 A! CHIKONDI chopambana,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1350 Mvera Yesu, mvera Yesu,
  • Hymn 1372 Zam’madzi zonse zakuopsyazo,
  • Hymn 1279 Kuti munditsogolera paulendopo;
  • Hymn 267 AMBUYE, thandizenitu
  • Hymn 350 Yesu ati,
  • Hymn 1159 Mwalembedwa mukalata
  • Hymn 1071 Kumwamba Yesu mthandize,
  • Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,
  • Hymn 137 UTHENGA wa Ambuye
  • Hymn 48 IMFA ya Mwana wa Mulungu,
  • Hymn 656 Ndipumulire panupo,
  • Hymn 1004 A! mizimu yakuipa
  • Hymn 598 Mlungu ali nane;
  • Hymn 816 Mdima wafika,
  • Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,
  • Hymn 1231 Nlokoma dzinalo la Yesu, ndilo thanthwe langa,
  • Hymn 480 TIANA ife tingofoka,
  • Hymn 450 YESU, munditsogoza
  • Hymn 1191 Ambuyanga Yesu
  • Hymn 49 Ndi ife akudziwa
  • Hymn 367 MPULUMUTSI, tikagona
  • Hymn 1722 Ambuye tikondweratu
  • Hymn 1158 Yesu ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 59 Tinachoka munjira ya imfa,
  • Hymn 281 Atate, ndipempha
  • Hymn 1163 Tili ndi mtendere
  • Hymn 269 NDILIRA ine kukayenda
  • Hymn 97 Maso ndi maso ndi Kristu,
  • Hymn 643 Mukhale nawo, yesu,
  • Hymn 1366 Sititha ifedi
  • Hymn 803 Mulungu wanga, Dzuwatu
  • Hymn 489 YESU ndiye Bwenzi lathu,
  • Hymn 1126 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 76 E, MOYO wanga’we
  • Hymn 1633 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 1070 Mthandize Mbuye, timvetu,
  • Hymn 1426 Wina panalibe
  • Hymn 109 MUTHIRE, Yesu, m’mtimanga
  • Hymn 753 Getsemane ndionako
  • Hymn 1840 Ndiye M’busa wanga,
  • Hymn 745 Anatifera nsembe Iyeyo,
  • Hymn 768 Ndi ife tinga mbewuzo
  • Hymn 430 MLUNGU akuyang’aniredí,
  • Hymn 256 Ndilira, ndilira,
  • Hymn 1638 Alinkudza wansoni Munthu
  • Hymn 703 Dzuwa, madzi, kudya, mpweya,
  • Hymn 710 Nthano ya Hananiyayo
  • Hymn 743 Mudze, anthuni, talawani ‘nu
  • Hymn 1330 Etu, zilira konseko
  • Hymn 459 KALE anthu m’kholamo,
  • Hymn 1133 Ngatitu abwenzi anga
  • Hymn 1771 Iye natsitsa kunsi
  • Hymn 18 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 123 Koma mudzisungire chuma cha Kumwamba
  • Hymn 335 Mtembenuke mtima wanu,
  • Hymn 700 Mzimu woonadi
  • Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,
  • Hymn 793 Tikondwera kuti
  • Hymn 196 NDI inetu sinditha’yi
  • Hymn 683 Musamaopa kanthu ‘yi, tamani Yesuyo;

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version