Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 194 AMBUYE’naitan’ne;

  1. Home   »  
  2. Hymn 194 AMBUYE’naitan’ne;

Hymn 194 AMBUYE’naitan’ne;

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 194 AMBUYE’naitan’ne;

 

AMBUYE’naitan’ne;
“Dzapumulire kuno,
Tsamira mutu, mwana’we
M’chifuwa mwanga muno.”

Ndabwera kwa Ambuyeyo;
Wolema, wachisoni;
Anandipulumutsako,
Nakondweretsa ine.

Ambuye naitana’ne;
“Ndipatsa anthu madzi,
Wotopa ndi waludzu’we
Dzamwere moyo kuno.”

Ndabwera kwa Ambuyeyo.
Ndamwera madzi awa;
Laleka ndithu ludzulo,
Tsopano moyo wadza

Ambuye naitana’ne;
“La dziko ndine Dzuŵa,
Yang’ana Ine, kwacha’we,
Wachoka mdima uja.”

Ndayang’anira Mbuyeyo
Ndzapeza Dzuŵa langa
Londiyendetsa bwinoli
Pa njira yanga yonse.

Post navigation

Previous: Hymn 193 THANTHWE long’ambikatu,
Next: Hymn 195 YESU wondikondadi,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 11 NDI mitima yokondwera,
  • Hymn 268 Potuluka m’mudzimo
  • Hymn 37 YESU analikhanda
  • Hymn 1662 Msandipitire, Yesu,
  • Hymn 1281 Ndikhulupirira, Yesu, mndibvomereko;
  • Hymn 1438 Yesu akukonda,
  • Hymn 52 POTULUKA m’mudzimo
  • Hymn 1430 Ndipo pakulowa
  • Hymn 290 Ndi miyendo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 153 Pemphero ndiko kufuna,
  • Hymn 732 1 Ndinamva njala, Yesu,
  • Hymn 230 Ndisamba ndiyera,
  • Hymn 518 Ana a Yerusalemu
  • Hymn 1365 Zozizwa za m’dziko,
  • Hymn 1652 Mabala ajawo
  • Hymn 204 Kumandako, kumanda
  • Hymn 1527 Ndiye Mzimu Wakuyera
  • Hymn 1856 Mzimu, msandipitirire,
  • Hymn 44 Mlungu dalitsani Malawi,
  • Hymn 541 Ana inu, yamikani
  • Hymn 1506 Ndikamfunafuna Iye,
  • Hymn 48 Ngakhale alemera
  • Hymn 1037 Mapemphero athu
  • Hymn 218 Mbuye Yesu ndi Atate,
  • Hymn 285 Ndipempha, Ambuye,
  • Hymn 480 TIANA ife tingofoka,
  • Hymn 886 Chikondi, chimwemwe,
  • Hymn 751 Mongatu mawu anuwo,
  • Hymn 1649 Kutenga inetu, kutenga inetu
  • Hymn 198 CHITSIMECHO cha mwaziwo
  • Hymn 492 DZIKO lilipolo
  • Hymn 1798 Mukondwe anthu a Mulungu,
  • Hymn 1215 Ndimkonde Kristuyo,
  • Hymn 1236 Mbuye ndimva leroli
  • Hymn 1481 Timsankhe Yesu Mbuyeyo,
  • Hymn 513 Atipempherera
  • Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,
  • Hymn 126 Mwa ine, moyo wanga ndi Yesu
  • Hymn 1786 Ndikonda Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 1086 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini moyo,
  • Hymn 580 Mwana wakuyera ‘Nu,
  • Hymn 549 Ndiye Mbuye, Mfumu yanga,
  • Hymn 1309 Ndi inetu ndidziwedi
  • Hymn 164 WANENA ndi Yesu,
  • Hymn 962 Inde Mbuye, tibweradi,
  • Hymn 239 TILI ndi mtendere
  • Hymn 1640 Alinkudza Ambuye Yesu
  • Hymn 605 Chifukwa cha zokoma mtima zonse za ulerezo,
  • Hymn 583 Anabadwa,
  • Hymn 246 NAMONDWE akawombabe,
  • Hymn 534 Bwerani, kondwerani,
  • Hymn 1766 Ndilikulemekeza
  • Hymn 250 Lidze msanga dzuwa lanu
  • Hymn 1772 Iye amakhutitsa
  • Hymn 1834 Chisomo ndi zokoma zake sizileka konse;
  • Hymn 1443 Ambuye Yesu anatsira
  • Hymn 735 Mwa chikho chokumbutsa
  • Hymn 201 NDILINKUDZA kwa Ambuye,
  • Hymn 784 Mugwade pansi m’nyumbayo,
  • Hymn 608 Maluwa abwino aphuka m’mapiri ndi m’madambomo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version