Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 194 AMBUYE’naitan’ne;

  1. Home   »  
  2. Hymn 194 AMBUYE’naitan’ne;

Hymn 194 AMBUYE’naitan’ne;

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 194 AMBUYE’naitan’ne;

 

AMBUYE’naitan’ne;
“Dzapumulire kuno,
Tsamira mutu, mwana’we
M’chifuwa mwanga muno.”

Ndabwera kwa Ambuyeyo;
Wolema, wachisoni;
Anandipulumutsako,
Nakondweretsa ine.

Ambuye naitana’ne;
“Ndipatsa anthu madzi,
Wotopa ndi waludzu’we
Dzamwere moyo kuno.”

Ndabwera kwa Ambuyeyo.
Ndamwera madzi awa;
Laleka ndithu ludzulo,
Tsopano moyo wadza

Ambuye naitana’ne;
“La dziko ndine Dzuŵa,
Yang’ana Ine, kwacha’we,
Wachoka mdima uja.”

Ndayang’anira Mbuyeyo
Ndzapeza Dzuŵa langa
Londiyendetsa bwinoli
Pa njira yanga yonse.

Post navigation

Previous: Hymn 180 MALO alimo m’nyumba ya Yesu,
Next: Hymn 201 NDILINKUDZA kwa Ambuye,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1111 Pamene ndilemedwa
  • Hymn 415 Tidzalandirabe komwe
  • Hymn 1445 Tiyeni tonse, tinkeko
  • Hymn 1346 Ndaima pano, ndaima pakhomo:Lowa, lowa, lowa, lowa!
  • Hymn 464 Yesu atiuza tiyambemo,
  • Hymn 446 Yesu alandira
  • Hymn 912 Makomo afanana
  • Hymn 1597 Timchimwira kopambana,
  • Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,
  • Hymn 1119 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 319 Koma zina sizinadziwa ayi,
  • Hymn 731 Mundionetse, Yesu,
  • Hymn 1693 Koma masauko ake Aleluya
  • Hymn 1379 Mulungu yemweyo
  • Hymn 1109 Pamene ndisauka,
  • Hymn 232 Uchita kwombola,
  • Hymn 238 MULUNGU wanga,
  • Hymn 1727 Pokumbukira mtandawo
  • Hymn 950 Sindidapempha kale Mbuye ‘yi,
  • Hymn 178 Machimo anga ngambiri
  • Hymn 44 NTHAWIYO anam’gwira Yesu,
  • Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,
  • Hymn 464 AKAZI anadza kwa Yesu ndi anawo,
  • Hymn 200 YESU mundimve, ndikuliratu,
  • Hymn 971 Ndinu Mbusa wanga;
  • Hymn 220 Kalekale ndinathawa,
  • Hymn 517 “Osana m’Mwambamwamba!”
  • Hymn 1260 Yesu, mulikundipempha, Munaterodi:
  • Hymn 221 Yesu and’itana,
  • Hymn 110 Ndaima nji pa Kristuyo,
  • Hymn 779 Yesu Mbuye wanga,
  • Hymn 1844 Pamaso pa adaniwo mwayala gome langa;
  • Hymn 1519 M’Buku lakuyerali
  • Hymn 443 M’MAŴA tizifesa
  • Hymn 1832 Za m’mdima, imfa, nkhondo ndi zoipa sindiopa;
  • Hymn 1816 Anatikondakonda ‘Ye,
  • Hymn 1681 Mphamvu za imfa ndi za Satana
  • Hymn 1355 Atate, Mwana, Mzimunso,
  • Hymn 1793 Pakuwoloka mtsinje wa imfa
  • Hymn 197 Tidzatama Atate wathu
  • Hymn 1748 Ambuye tsopano lino,
  • Hymn 1412 Imfa idzafika msanga;
  • Hymn 642 Mulunzanitse awa,
  • Hymn 339 Tipempha,
  • Hymn 227 NDIM’KONDE Kristuyo,
  • Hymn 266 Ukondwere moyo wanga,
  • Hymn 1336 Mwamva mawu a Mulungu;
  • Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 1161 Wapumitsa mtima wanga,
  • Hymn 1152 Pokonda Yesuyo, mtendere!
  • Hymn 10 TSOPANO linoli,
  • Hymn 483 NTHAŴI yaubwana yatha,
  • Hymn 272 Ankhondowo poona
  • Hymn 387 MUDZE, anthuni, talaŵani ’nu
  • Hymn 736 Mndidyetse m’chipululu
  • Hymn 1578 Onsewa ‘nachimwa
  • Hymn 1686 Ndi mtima wonse mwimbedi
  • Hymn 834 Tiyamike Mlungu wotipatsa zachifundozi,
  • Hymn 898 Mndidziwitse ntchito yanga,
  • Hymn 634 Mtifungatire ndi mapiko paulendo pathu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version