Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,

Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,

 

AMBIRI tikondwera mwa Yesu,
Nanga inu? Nanga inu?
Tapeza chipulumutso ndithu;
Nanga inu?

Masiku onse timakondwera
Pakumva Mawu ake a Yesu;
Wolalikira tidzamumvera;
Nanga inu?

Ife tiyembekezera YESU,
Nanga inu? Nanga inu?
Chimwemwecho chilimumtimamu;
Nanga inu?

Titasokera tinabwerera,
Nanga inu? Nanga inu?
Tidziŵa kuti ndiwo uchimo;
Nanga inu?

Tinachoka munjira ya imfa,
Nanga inu? Nanga inu?
Takopeka ndi Mawu a Yesu;
Nanga inu?

Post navigation

Previous: Hymn 190 CHITETEZO chachikulu
Next: Hymn 192 ZAKEYU mkulu wa misonkho,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 438 Yesu ndiye Mbusa
  • Hymn 518 Ana a Yerusalemu
  • Hymn 1212 Zina ndi zinanso
  • Hymn 411 Yesu adza kukundika
  • Hymn 64 LERO Kristu anauka,
  • Hymn 1416 Mbuye wanga ndilikumva,
  • Hymn 1719 Ku Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 640 Anakwatira kale
  • Hymn 461 Inu nonse anzanga,
  • Hymn 430 MLUNGU akuyang’aniredí,
  • Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga
  • Hymn 695 Pomveka konsekonse mbiri
  • Hymn 807 Mpulumutsi tikagona
  • Hymn 755 Pamene padzakhalapo
  • Hymn 1330 Etu, zilira konseko
  • Hymn 1524 Ndiwo alimbitsa
  • Hymn 1547 Mtisangalatse m’zonse,
  • Hymn 304 Imva kulira kwa Yesu
  • Hymn 1029 Nkhawa tilibe; Yesuyo
  • Hymn 25 ANGELO amayimba,
  • Hymn 744 Kristu ndi mwini moyo wathuwu,
  • Hymn 182 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 904 Komweko akhala Yesuyo
  • Hymn 1185 Imfa ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 294 POYESEDWA ine
  • Hymn 719 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 204 Kumandako, kumanda
  • Hymn 476 MBUYE, tili ana anu,
  • Hymn 1844 Pamaso pa adaniwo mwayala gome langa;
  • Hymn 382 Mwadzoza mutu wanga ndi
  • Hymn 953 Ichi chindisangalatsa
  • Hymn 1466 Ambuye wathu Yesu
  • Hymn 2 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 1357 Mlemekeze, anakonda
  • Hymn 1175 Sindinanyengedwa konse,
  • Hymn 450 Koma usalole
  • Hymn 52 POTULUKA m’mudzimo
  • Hymn 1213 Mwamva Yesu m’mtimamo,
  • Hymn 1487 Bvumbulutsa zonse zako
  • Hymn 241 Munadzera ndi Mawu a moyo
  • Hymn 456 ANA inu, ana inu,
  • Hymn 403 NDIYIMBA ndi chimwemwe lero,
  • Hymn 1712 E! Yesu Mbuye wangadi,
  • Hymn 496 MBUYE dalitsani Afirika.
  • Hymn 40 Padziko pano tikhalira
  • Hymn 360 KRISTU wakuyeratu,
  • Hymn 613 Dziko lonse nla Mulungu
  • Hymn 1468 Zobvala zake zonse
  • Hymn 773 Mtsinje woyerawo
  • Hymn 275 NTHAWI yathu yafikatu,
  • Hymn 609 Zanu zapansi nzokoma Mbuye; tikondwera ‘fe,
  • Hymn 687 Bukitsani mawunso
  • Hymn 1176 Sandinyenga, salephera;
  • Hymn 1598 Mtiphunzitse, Mbuye Yesu,
  • Hymn 1672 Lambira Mfumuyo,
  • Hymn 1724 Ambuye mthandize inetu
  • Hymn 634 Mtifungatire ndi mapiko paulendo pathu,
  • Hymn 1537 Mulowe m’mtima, mdzazetu
  • Hymn 374 Pakuti Mfumuyo
  • Hymn 1797 Chikondi chake chindidzera

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version