Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,

Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,

 

AMBIRI tikondwera mwa Yesu,
Nanga inu? Nanga inu?
Tapeza chipulumutso ndithu;
Nanga inu?

Masiku onse timakondwera
Pakumva Mawu ake a Yesu;
Wolalikira tidzamumvera;
Nanga inu?

Ife tiyembekezera YESU,
Nanga inu? Nanga inu?
Chimwemwecho chilimumtimamu;
Nanga inu?

Titasokera tinabwerera,
Nanga inu? Nanga inu?
Tidziŵa kuti ndiwo uchimo;
Nanga inu?

Tinachoka munjira ya imfa,
Nanga inu? Nanga inu?
Takopeka ndi Mawu a Yesu;
Nanga inu?

Post navigation

Previous: Hymn 180 MALO alimo m’nyumba ya Yesu,
Next: Hymn 201 NDILINKUDZA kwa Ambuye,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 59 Tinachoka munjira ya imfa,
  • Hymn 45 Malawi dziko lokongola,
  • Hymn 108 Tikondwera ife tonse
  • Hymn 1510 Mtume tsopanoli
  • Hymn 407 ADZAPAMBANA Yesu ponse
  • Hymn 826 Mutonthoze mtima
  • Hymn 1180 Ndine kapolo wa Mbuye wanga;
  • Hymn 836 Kamoyo kanga katha lero lino,
  • Hymn 1093 Odala ndi onsewo
  • Hymn 153 Pemphero ndiko kufuna,
  • Hymn 1047 Ambuye, chotsani zonse zomwezo
  • Hymn 236 Omvana ndi Yesu,
  • Hymn 491 KWA Yesu ndi kwabwinoko,
  • Hymn 621 Wolenga ndi Yemweyo
  • Hymn 1485 Unachimwachimwa ndithu,
  • Hymn 24 “Ndakupeza womanga,
  • Hymn 396 Mtitsogolere nthawi zonsezo;
  • Hymn 1427 Penyetsetsa Yesu,
  • Hymn 204 Kumandako, kumanda
  • Hymn 440 Yesu wakufatsa mtima
  • Hymn 1218 Pakufa pangapo
  • Hymn 328 Yesu ndiye mphamvu yanga,
  • Hymn 1293 Chitsimecho cha mwaziwo
  • Hymn 1340 Perekani mtima wanu
  • Hymn 220 Kalekale ndinathawa,
  • Hymn 59 IMVANI uthenga,
  • Hymn 1144 Khalani duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 400 ONA Mwana wa Nkhosa,
  • Hymn 617 Nthawi yina Mbuyeyu
  • Hymn 1355 Atate, Mwana, Mzimunso,
  • Hymn 650 Tikondwa tonse ndi kukuthokazani Nu
  • Hymn 1161 Wapumitsa mtima wanga,
  • Hymn 1000 Amatininkha zida zoteteza mtima, ndizo:
  • Hymn 1413 Ndichitenji kukapeza
  • Hymn 1294 Wakuba uja nachiona,
  • Hymn 215 Choka, choka,
  • Hymn 1418 Khulupirani kuti mukalowe m’Mwambamo,
  • Hymn 761 Natamndira Mlunguyo
  • Hymn 1134 Pansi pano ndili mlendo,
  • Hymn 574 A! Yesu Mbuye wakuyera,
  • Hymn 325 KODI uli ndi chisoni
  • Hymn 658 Ndichitireni, Mbuye ‘ne,
  • Hymn 900 Mutipatse leroli
  • Hymn 820 Ndife ananu,
  • Hymn 205 KWA Inu Yesu ndilira,
  • Hymn 202 NDIKHULUPIRIRA, Yesu,
  • Hymn 1691 Lero Kristu anauka, Aleluya,
  • Hymn 1516 Pakudera nkhawa ‘ne,
  • Hymn 916 Akondwerera anthu
  • Hymn 428 Tiyandika, Mbuye,
  • Hymn 1198 Mabala ake m’manja
  • Hymn 610 Nafenso tidzadzuka kwa ‘ke ngati maluwawo,
  • Hymn 1039 Usafune chuma chokha,
  • Hymn 1208 Kalelo! Kalelo!
  • Hymn 351 Titi bwanji?
  • Hymn 1523 Atisangalatsa,
  • Hymn 401 A MULUNGU,
  • Hymn 344 ’TATE, ’Nu.
  • Hymn 392 Chimwemwe chomwe mpatseko
  • Hymn 696 Ufumu wake udalitsa

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version