Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 143 KONZA mtima iwe mbale,

  1. Home   »  
  2. Hymn 143 KONZA mtima iwe mbale,

Hymn 143 KONZA mtima iwe mbale,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 143 KONZA mtima iwe mbale,

 

KONZA mtima iwe mbale,
Pakuleka tchimo;
Siya zonse uzikonda,
Ndikutsata Yesu.

Konza mtima wako lero,
Yesu alowemo;
Ndipo usachedwe iwe,
Taata Yesu lero.

Imva kuyankhula kwake,
Mawu a chikondi;
Ayankhula iwe lero,
Kuti upumule.

Nthawi ya chisomo m’dziko,
Ndi inotu mbale;
Yom’dziwatu Mpulumutsi,
Ukali ndi moyo.

Post navigation

Previous: Hymn 140 NDINAMIRA m’machimo, wosaonekanso,
Next: Hymn 161 LERO lino mbale wanga,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 126 DAVIDE kubusa kuja,
  • Hymn 1421 Alongo ‘nu, alongo ‘nu,
  • Hymn 1426 Wina panalibe
  • Hymn 241 Munadzera ndi Mawu a moyo
  • Hymn 564 Ndi chifukwa atikonda,
  • Hymn 1083 “Khala mwa Ine,” Yesu anatero;
  • Hymn 717 Ambuye zathu zonsezi
  • Hymn 1357 Mlemekeze, anakonda
  • Hymn 1676 Kondwerani dzuwa lino Aleluya,
  • Hymn 149 RUTE, Rute anaumilira,
  • Hymn 1479 Ndi Yesu yemwe kalelo
  • Hymn 280 Tisonkhane tonsefe,
  • Hymn 565 Koma sitimpenya m’khola
  • Hymn 432 Ulendo ungoyamba
  • Hymn 340 PEMPHERA m’mbanda kucha,
  • Hymn 748 Ndiye wa moyo wonse Mwiniyo,
  • Hymn 234 IMFA ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 1604 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 296 Mngelo anatumidwa
  • Hymn 89 Muli mphamvu yodabwitsatu
  • Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,
  • Hymn 811 Wopulumutsa mudzetu;
  • Hymn 1474 Zilepheradi zonse kugula moyowo,
  • Hymn 154 Pemphero ndiko kulira,
  • Hymn 832 Zochimwa za usana uno mndikhululukire ‘ne;
  • Hymn 1101 Ngati mtima sumakonda
  • Hymn 1109 Pamene ndisauka,
  • Hymn 1732 Anapachikidwatu,
  • Hymn 1460 Akuti anthu akumvera
  • Hymn 1820 Kwezani nane Ambuyathu,
  • Hymn 375 YESU m’khale nafe
  • Hymn 466 Yesu, muli pa chimpando
  • Hymn 644 M’wasunge, m’wayendetse
  • Hymn 372 Potero onsewo
  • Hymn 681 Ankhondo a Mulungu ‘nu, yendani m’njiramo,
  • Hymn 285 Ndipempha, Ambuye,
  • Hymn 1674 Lambira Yesuyo,
  • Hymn 143 Lero lino Mbuye Yesu
  • Hymn 569 Tiimbe ndi kulalikira
  • Hymn 181 PANALITU wakudwala
  • Hymn 1736 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 360 Muli ndi ludzu, idzani
  • Hymn 873 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 1568 Kudzoza kwanu kutipatsa
  • Hymn 22 Mbuye mtsitsimutse!
  • Hymn 186 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 1293 Chitsimecho cha mwaziwo
  • Hymn 447 Usachimwe konse,
  • Hymn 566 Ana inu, ana inu,
  • Hymn 204 Kumandako, kumanda
  • Hymn 433 MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku
  • Hymn 924 Kodi uli ndi chisoni
  • Hymn 86 IYE wokhulupilira Yesu,
  • Hymn 616 Dziko lathu lonseli
  • Hymn 415 Tidzalandirabe komwe
  • Hymn 1601 Zina za Yesu ndimvetu,
  • Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,
  • Hymn 1090 Chitsime chakuyera ine
  • Hymn 1316 Ndabwera kwa Ambuyeyo:
  • Hymn 85 Mtima wanga wabvutika,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version