Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 143 KONZA mtima iwe mbale,

  1. Home   »  
  2. Hymn 143 KONZA mtima iwe mbale,

Hymn 143 KONZA mtima iwe mbale,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 143 KONZA mtima iwe mbale,

 

KONZA mtima iwe mbale,
Pakuleka tchimo;
Siya zonse uzikonda,
Ndikutsata Yesu.

Konza mtima wako lero,
Yesu alowemo;
Ndipo usachedwe iwe,
Taata Yesu lero.

Imva kuyankhula kwake,
Mawu a chikondi;
Ayankhula iwe lero,
Kuti upumule.

Nthawi ya chisomo m’dziko,
Ndi inotu mbale;
Yom’dziwatu Mpulumutsi,
Ukali ndi moyo.

Post navigation

Previous: Hymn 142 MULUNGU aŵakonda anthu
Next: Hymn 144 AMENE adzavomereza ndithu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1473 Anasenza pa bwanji uchimo wonsewo,
  • Hymn 953 Ichi chindisangalatsa
  • Hymn 1426 Wina panalibe
  • Hymn 987 Ambuye wa Kumwamba,
  • Hymn 1064 Moyowo
  • Hymn 579 Pochezera m’dambomo,
  • Hymn 4 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 1551 Mukhale m’kati mwathu,
  • Hymn 925 Kodi umadandaula:
  • Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,
  • Hymn 848 Mudze, mlowe m’mtimamu,
  • Hymn 119 Tamverani anthu inu,
  • Hymn 1007 M’mene umauka m’mawa,
  • Hymn 1591 Sizitha ntchito zangazo,
  • Hymn 1437 Yesu ndi wokonda;
  • Hymn 1085 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini mphamvu,
  • Hymn 335 Mtembenuke mtima wanu,
  • Hymn 641 Awiri aimamu,
  • Hymn 1313 Zindichulukirazi
  • Hymn 819 Lero tigone,
  • Hymn 1250 Mndilandire ine Mbuye
  • Hymn 146 KODI ulikulemedwa
  • Hymn 1776 Tiyeni timgwadire
  • Hymn 588 Mlungu, Inutu,
  • Hymn 260 Angelo aitana,
  • Hymn 698 Polenga dzikoli,
  • Hymn 1819 Pokondwa ndi poona bvuto
  • Hymn 564 Ndi chifukwa atikonda,
  • Hymn 423 MUNENE Mbuye, ’nenetu,
  • Hymn 1348 Akupeza, akupeza,
  • Hymn 265 MUDZAZE Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
  • Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo
  • Hymn 782 Aleluya, aleluya,
  • Hymn 1153 Mtendere uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 793 Tikondwera kuti
  • Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
  • Hymn 1765 Zoonazi amithenga
  • Hymn 501 Yesu andikonda ine;
  • Hymn 450 Koma usalole
  • Hymn 202 Timpemphere kutipatsa
  • Hymn 558 Mwanayo wa Mulunguyo
  • Hymn 828 Ndidzukanso m’mawa,
  • Hymn 816 Mdima wafika,
  • Hymn 755 Pamene padzakhalapo
  • Hymn 1298 Ndikhulupira ‘Nu,
  • Hymn 151 UKAPENYA kwa Yesu uliko moyoko,
  • Hymn 1285 Yesu, n’kupatsani zonse,
  • Hymn 408 ABALE nonse mulindiranji?
  • Hymn 196 Tidzimba komweko nyimbo
  • Hymn 1282 Ndilinkudza kwa Ambuye,
  • Hymn 1567 Mubwere Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 1231 Nlokoma dzinalo la Yesu, ndilo thanthwe langa,
  • Hymn 1397 Okwawa pansi inu,
  • Hymn 714 Dzuwa ndi mvula yonseyo
  • Hymn 271 Zoipa zangazi
  • Hymn 1558 Wosangalatsa, ine ndikalira
  • Hymn 330 Yesu ndiye Mtsogoleri
  • Hymn 460 KULI kaphiri m’talimo
  • Hymn 144 Yesu, ndipemphera
  • Hymn 1409 Kodi mufunatu Yesu?

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version