Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,

Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,

 

MZIMU Woyera, mudzetu,
Tiyeretsedwe m’mtimamu;
Mupatse anthu anuwa
Mitulo yanu yonseyo.

Kudzoza kwa Kumwambako
Kutitonthoza m’mtimamo,
Ndi kutidzutsa m’moyomu,
Tikhale okondanatu.

Pankhope pathu mthirepo
Chisomo chanu chijacho;
Mtendere mutininkhebe,
Mutiyendetse ponse phee!

Tionetseni tonsetu
Umodzi wanu wonsemo,
Atate, Mwana, Mzimu ’Nu
Tiimbe Nthaŵi zonsezo:

Titamire Nthaŵi zonse
’Tate, Mwana, Mzimu, Nonse.
Amen

Post navigation

Previous: Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,
Next: Hymn 107 MUBWERE kuno Mzimu ’Nu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1232 Ambuye ndinu Mbusa, Bwenzi, ndi Wansembe wanga,
  • Hymn 1166 Masauko athu
  • Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,
  • Hymn 233 M’mene ndapenya mwazi wa
  • Hymn 1598 Mtiphunzitse, Mbuye Yesu,
  • Hymn 585 Alanditsa,
  • Hymn 1654 Mbuye, mutsaganetu
  • Hymn 400 Dzuwa liwala, m’tulotu
  • Hymn 136 Atumwi atummika, atumika,
  • Hymn 570 Ndikhulupirira Yesu
  • Hymn 312 Atate, mupatse zomwe tapemphazi,
  • Hymn 1761 Amithenga anaimba
  • Hymn 1132 Mlungu adzandilandila,
  • Hymn 186 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 419 ANYAMATA a Mulungu,
  • Hymn 1210 Kumwamba ndidzanenadi
  • Hymn 664 Komwe asauka anthu
  • Hymn 620 Mphatso zonse zathu
  • Hymn 1220 Bwenzi ndinamkomanayo
  • Hymn 1158 Yesu ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 1765 Zoonazi amithenga
  • Hymn 1543 Idzani, Mzimu Inu,
  • Hymn 1201 Kumwamba kwanuko
  • Hymn 1721 Mapazi ake namvatu
  • Hymn 470 YESU andikonda ine,
  • Hymn 1034 Mkristu, ulimbike
  • Hymn 415 PAMAYIKO pali mdima,
  • Hymn 1296 Chionerere mwaziwo
  • Hymn 156 OKOMA ndiwo mawu
  • Hymn 1803 Nowayo nayendamo,
  • Hymn 146 KODI ulikulemedwa
  • Hymn 478 Ndife ana, mutikonda,
  • Hymn 145 MBIRI yakale lomwe
  • Hymn 503 Ndikondwa kuti Yesu
  • Hymn 732 1 Ndinamva njala, Yesu,
  • Hymn 373 NYUMBA ya Mulungu, ili pano,
  • Hymn 1024 Anasauka Mbuyeyo,
  • Hymn 466 OSANATU, osana,
  • Hymn 277 GWIRA zintchito zako,
  • Hymn 1284 Kale ndinalira Inu,
  • Hymn 234 IMFA ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 524 Wokoma Mbuyathu
  • Hymn 447 Usachimwe konse,
  • Hymn 668 Achisoni, obvutidwa,
  • Hymn 117 Atate wondipatsazo,
  • Hymn 1769 Ndiye amachitira
  • Hymn 683 Musamaopa kanthu ‘yi, tamani Yesuyo;
  • Hymn 1603 Zina za Yesu m;Mwambamo,
  • Hymn 368 Yehova ndiye Mlungudi,
  • Hymn 984 Mpingo wa Mulungu
  • Hymn 643 Mukhale nawo, yesu,
  • Hymn 1327 Bwezatu, bwezatu,
  • Hymn 840 Ambuye munapatsa tsiku
  • Hymn 161 LERO lino mbale wanga,
  • Hymn 1002 Haya! ‘Nzanga taonani Yoonekayo
  • Hymn 321 Ndi ponse paphiri ndi padambopo
  • Hymn 1627 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 398 Lero lino mwatipatsa
  • Hymn 809 Madzulo aja kalelo
  • Hymn 826 Mutonthoze mtima

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version