Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu

  1. Home   »  
  2. Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu

Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu

 

MUBWERE Mzimu Inu
Woyera, wakufatsa,
Muchotse mdima m’mtima mwathu
Tikapenye m’maso.

Mtisangalatse m’zonse,
Ndi wachifundo Inu,
Tiyembekeze kumapazi
A Mbuyathu Yesu.

Mtitsitsimutse ife
Kuchotsa nkhaŵa zathu,
Muyatse moto wachikondi
Mu mitima yathu.

Mtitsutse titachimwa
kutilapitsa m’mtima,
Mwonetsenso chikondi chokhululukira tchimo.

Kutiyeretsa m’mtima
Ndi ntchito yanu yokha,
Kupatsa moyo watsopano
M’mene timafoka.

Mukhale m’kati mwathu,
Mutichotsere mantha,
Tidzayamika ’Tate wathu,
Mwana wawo ndi ’Nu.

Post navigation

Previous: Hymn 103 MPUME pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
Next: Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 62 Tchimo lonse ligonjera
  • Hymn 1237 Ine kanthu ndilibe
  • Hymn 1043 Mbiri yake ubukitse,
  • Hymn 326 Yesu, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 1724 Ambuye mthandize inetu
  • Hymn 1176 Sandinyenga, salephera;
  • Hymn 1550 Kutiyeretsa m’mtima
  • Hymn 81 Imva mawu akewo,
  • Hymn 1568 Kudzoza kwanu kutipatsa
  • Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,
  • Hymn 463 Yesu atiuza tiwale ‘fe,
  • Hymn 517 “Osana m’Mwambamwamba!”
  • Hymn 429 M’DZANJA lanu Ambuye,
  • Hymn 1164 Tikakhulupira
  • Hymn 154 SING’ANGA ‘mkulu ndiye Yesu,
  • Hymn 882 Kodi tikulema nazo
  • Hymn 3 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 185 NDINE Mbusayo wabwino,
  • Hymn 1315 Ambuye ‘naitana ‘ne:
  • Hymn 598 Mlungu ali nane;
  • Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,
  • Hymn 452 Tiana ife tingofoka,
  • Hymn 579 Pochezera m’dambomo,
  • Hymn 396 PETURO ’nafunsa Hananiya:
  • Hymn 1716 Anena mawu m’mtanda momwe,
  • Hymn 85 Mtima wanga wabvutika,
  • Hymn 208 “Lowa, lowa
  • Hymn 211 Chakudya ichi ndi cha iwenso,
  • Hymn 1272 Muyambe ntchito yanuyi,
  • Hymn 699 Inu wakudzatu
  • Hymn 89 Muli mphamvu yodabwitsatu
  • Hymn 345 Ubwere,
  • Hymn 676 Adze amitundu yonse,
  • Hymn 1220 Bwenzi ndinamkomanayo
  • Hymn 443 M’MAŴA tizifesa
  • Hymn 1744 Kale ophunzira ake
  • Hymn 494 Yesu, E, ndikufunani,
  • Hymn 1686 Ndi mtima wonse mwimbedi
  • Hymn 464 AKAZI anadza kwa Yesu ndi anawo,
  • Hymn 545 Anatifera tonsefe
  • Hymn 1826 Amadyetsa Iye mbalame zam’mwamba,
  • Hymn 130 PHWANDO la Belisazara,
  • Hymn 445 Mlewe oipawo,
  • Hymn 773 Mtsinje woyerawo
  • Hymn 1368 Mitambo inu yakumwambako,
  • Hymn 357 TAMANDANI Mbuye,
  • Hymn 852 Munkhani zako zonsetu
  • Hymn 702 Mbuye wathu mutipatsa
  • Hymn 1560 Mthandizi ndinu, mndithangate ine
  • Hymn 601 Akaona masautso
  • Hymn 267 AMBUYE, thandizenitu
  • Hymn 823 M’mwambamo nyenyezi
  • Hymn 837 Koma kalelo mnakhalitsa pano,
  • Hymn 1058 Chimwemwe chija chamumtima
  • Hymn 892 Tilibe madalitso
  • Hymn 12 Kumva milandu yathu mudzabwera
  • Hymn 965 Mundiuze, aulendo,
  • Hymn 55 Ambiri tikondwera mwa Yesu,
  • Hymn 933 M’mene imfa yathu idza,
  • Hymn 1651 Kwa Mulungu m’Mwambamo

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version