Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu

  1. Home   »  
  2. Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu

Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu

 

MUBWERE Mzimu Inu
Woyera, wakufatsa,
Muchotse mdima m’mtima mwathu
Tikapenye m’maso.

Mtisangalatse m’zonse,
Ndi wachifundo Inu,
Tiyembekeze kumapazi
A Mbuyathu Yesu.

Mtitsitsimutse ife
Kuchotsa nkhaŵa zathu,
Muyatse moto wachikondi
Mu mitima yathu.

Mtitsutse titachimwa
kutilapitsa m’mtima,
Mwonetsenso chikondi chokhululukira tchimo.

Kutiyeretsa m’mtima
Ndi ntchito yanu yokha,
Kupatsa moyo watsopano
M’mene timafoka.

Mukhale m’kati mwathu,
Mutichotsere mantha,
Tidzayamika ’Tate wathu,
Mwana wawo ndi ’Nu.

Post navigation

Previous: Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
Next: Hymn 121 MULUNGU, anthu ’fe

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 518 Ana a Yerusalemu
  • Hymn 1386 Ndi chifundo atipenya
  • Hymn 1057 Ndilira ine kukayenda
  • Hymn 400 ONA Mwana wa Nkhosa,
  • Hymn 1610 Waleka koronayo,
  • Hymn 822 Dzuwa lapitira,
  • Hymn 445 Mlewe oipawo,
  • Hymn 1299 Mzimu mndipatseko,
  • Hymn 13 Mtiwerengere m’Mwamba ndi oyera;
  • Hymn 383 Zokoma ndi zakuyanja
  • Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,
  • Hymn 52 Mbwere Mzimu, mbwere!
  • Hymn 1825 Zobvuta zoopsa ndi zosaukazi
  • Hymn 899 ‘Tate wa Kumwambako,
  • Hymn 975 Tiyeni, Akristu inu,
  • Hymn 435 ANAKWATIRA kale
  • Hymn 415 Tidzalandirabe komwe
  • Hymn 193 THANTHWE long’ambikatu,
  • Hymn 397 Yesu Mbusa, mutimvere,
  • Hymn 1687 Alonda onsewo
  • Hymn 223 Ndafoka, ndaipa,
  • Hymn 152 AMBUYE wathu Yesu
  • Hymn 1774 Poti akumbukira
  • Hymn 1427 Penyetsetsa Yesu,
  • Hymn 157 Mbuye, Mzimu Woyera
  • Hymn 1637 Tisaleke kugwirabe
  • Hymn 260 Angelo aitana,
  • Hymn 241 MTENDERE uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 246 NAMONDWE akawombabe,
  • Hymn 1713 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 513 Atipempherera
  • Hymn 1376 Akulu nonse ndi mafumu ‘nu,
  • Hymn 1052 Ndilira mtima wotamanda
  • Hymn 1786 Ndikonda Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 1157 Mtendere wapambana m’Mwambamo
  • Hymn 1278 Kuti muyeretsa mtima ndibvomeratu;
  • Hymn 47 Anthu m’maiko onse
  • Hymn 956 Mbuye munditsogolere,
  • Hymn 192 Apita anzathu dzuwa lino Kosaoneka,
  • Hymn 472 YESU, ndikabwera
  • Hymn 655 Ndiphunzitseni, Mbuyetu,
  • Hymn 141 Yenda iwe, yenda,
  • Hymn 1570 Mutidziwitse ‘Tate wathu,
  • Hymn 26 “Ndakukonda ku imfa
  • Hymn 327 NTCHITO yonse yakeyo
  • Hymn 1749 Chifukwa chipulumutso
  • Hymn 1211 Mwakhulupiriradi
  • Hymn 311 Tifuna kuchita chifuniro chanu,
  • Hymn 255 KHALA chete mtima wanga
  • Hymn 360 KRISTU wakuyeratu,
  • Hymn 333 M’DZIKO lino tikhalamo
  • Hymn 341 PAKUPEMPHERATU
  • Hymn 1674 Lambira Yesuyo,
  • Hymn 480 Tifunitsa Inu tere,
  • Hymn 464 AKAZI anadza kwa Yesu ndi anawo,
  • Hymn 1535 Lichepa dontho lokhali,
  • Hymn 1708 Pakugomedwapo
  • Hymn 1162 Mumvetu abwenzi athu,
  • Hymn 430 Tero tidzakwera
  • Hymn 651 Ikhale ngati nyali

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version