Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,

  1. Home   »  
  2. Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,

Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,

 

Yesu, dzina lakukonda,
Lopambana onse ena,
Tonse tidzaligwadira
Ndi mitima yochepetsa.

Yesu, dzina lokondwetsa
Akuipa a padziko,
Kale linatidziŵitsa
Mpulumutsi ndiye Yesu.

Yesu dzina lakufatsa,
Anamutcha ’kali Mwana,
M’mene analoŵa kale
M’dziko lino lakudana.

Yesu, dzina ndi lomweli
La pa dziko lino lonse,
Ndi lamphamvu yolanditsa
Anthu mu masoka onse.

Yesu, dzina lakukonda
La Mwanayo wa Mulungu,
Ife anthu osauka
Tithaŵira nalo kwanu.

Post navigation

Previous: Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye
Next: Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 159 Kamwana Yesu ‘nabadwa,
  • Hymn 1805 Anafa m’mvula muja
  • Hymn 266 Ukondwere moyo wanga,
  • Hymn 1318 Ndibwera kwa Ambuyeyo,
  • Hymn 1716 Anena mawu m’mtanda momwe,
  • Hymn 1778 Angelo kwezani
  • Hymn 1417 Atate ‘nu, atate ‘nu,
  • Hymn 1426 Wina panalibe
  • Hymn 1551 Mukhale m’kati mwathu,
  • Hymn 546 Kulibe wokwanira ‘yi
  • Hymn 1440 Yesu alindira,
  • Hymn 173 MWAMVA Mawu a Mulungu;
  • Hymn 451 MLUNGU alinane;
  • Hymn 330 Yesu ndiye Mtsogoleri
  • Hymn 119 M’BUKU la moyotu Mbuye,
  • Hymn 305 NDALIMVA dziko la m’talimo,
  • Hymn 615 Yamikani nonse ‘nu,
  • Hymn 1268 Mundilandiretu,
  • Hymn 1296 Chionerere mwaziwo
  • Hymn 1272 Muyambe ntchito yanuyi,
  • Hymn 1607 Yesu, dzina ndi lomweli
  • Hymn 801 Lero mwatipatsa moyo,
  • Hymn 1418 Khulupirani kuti mukalowe m’Mwambamo,
  • Hymn 573 Ambuye, tikutamandani
  • Hymn 2 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 274 E! tidzakomanansotu
  • Hymn 1626 Mbuye Yesu adzabwera,
  • Hymn 460 E! ang’ono ndifetu,
  • Hymn 15 YEHOVA ndiye Mbusa wanga,
  • Hymn 117 CHOLIMBITSA mtima ndi chonditsogolera;
  • Hymn 129 WODALA ndiye munthuyo,
  • Hymn 246 NAMONDWE akawombabe,
  • Hymn 351 CHIYEMBEKEZO changacho,
  • Hymn 208 “Lowa, lowa
  • Hymn 112 ELISA mneneri,
  • Hymn 402 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 89 INDE, ndifuna kumvatu,
  • Hymn 1236 Mbuye ndimva leroli
  • Hymn 70 Mbuye ndinu bwenzi langa ndithu,
  • Hymn 731 Mundionetse, Yesu,
  • Hymn 598 Mlungu ali nane;
  • Hymn 272 AMBUYE, ndifuna nditsukenitu;
  • Hymn 107 MUBWERE kuno Mzimu ’Nu
  • Hymn 441 MBUYE, tikuthokozani,
  • Hymn 1254 Mukhululukire ine,
  • Hymn 140 NDINAMIRA m’machimo, wosaonekanso,
  • Hymn 786 Yesu mkhale nafe
  • Hymn 61 Ndi chimwemwe ndimaona
  • Hymn 1089 Ndionetsere kuunika
  • Hymn 238 Mbuye Yesu, lowani m’mtima,
  • Hymn 1498 Simbani Mbiri yonse
  • Hymn 1058 Chimwemwe chija chamumtima
  • Hymn 1582 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 383 KASUPE ali wodzaza
  • Hymn 35 KODI mwaona chiyani,
  • Hymn 1539 Kudzoza kwa Kumwambako
  • Hymn 180 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 549 Ndiye Mbuye, Mfumu yanga,
  • Hymn 1338 Munachita nthantha kale,
  • Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version