Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,

  1. Home   »  
  2. Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,

Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,

 

Yesu, dzina lakukonda,
Lopambana onse ena,
Tonse tidzaligwadira
Ndi mitima yochepetsa.

Yesu, dzina lokondwetsa
Akuipa a padziko,
Kale linatidziŵitsa
Mpulumutsi ndiye Yesu.

Yesu dzina lakufatsa,
Anamutcha ’kali Mwana,
M’mene analoŵa kale
M’dziko lino lakudana.

Yesu, dzina ndi lomweli
La pa dziko lino lonse,
Ndi lamphamvu yolanditsa
Anthu mu masoka onse.

Yesu, dzina lakukonda
La Mwanayo wa Mulungu,
Ife anthu osauka
Tithaŵira nalo kwanu.

Post navigation

Previous: Hymn 87 IDZANI nonse ’nu
Next: Hymn 89 INDE, ndifuna kumvatu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1178 Mawu omwewo, nyimbo yomweyi,
  • Hymn 1301 Moyo ukatha zi,
  • Hymn 1828 Timtamande Iye ndi moyo wathunso
  • Hymn 536 Ana inu, myamikeni
  • Hymn 1417 Atate ‘nu, atate ‘nu,
  • Hymn 321 Ndi ponse paphiri ndi padambopo
  • Hymn 999 Amaliwongo ochuluka amalowa m’mtima
  • Hymn 678 Ibukike mbiri yanu,
  • Hymn 370 Pakuti Mbuye Mlunguyo
  • Hymn 1426 Wina panalibe
  • Hymn 496 MBUYE dalitsani Afirika.
  • Hymn 785 Yehova adalitse ‘nu,
  • Hymn 441 Tamverani, aitana:
  • Hymn 1604 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 189 MLENDO ali pakhomo,
  • Hymn 1607 Yesu, dzina ndi lomweli
  • Hymn 494 YESU Mbusa, mutimvere,
  • Hymn 1082 Ndidzaonana nanu
  • Hymn 131 Lolani ana, mumve Mlungu,
  • Hymn 529 Zili nazotu nkhwimba zirombozo,
  • Hymn 532 Ukondwere mtima wanga
  • Hymn 87 IDZANI nonse ’nu
  • Hymn 1194 Padziko lapansi
  • Hymn 148 Ndisauka, ndimasowa
  • Hymn 894 Mbuye, ndinu Mfumu yanga
  • Hymn 1076 Khalatu woyera,
  • Hymn 255 Pakuona imfayo
  • Hello world!
  • Hymn 1234 Ati Yesu Mbuyeyo:
  • Hymn 1546 Mubwere Mzimu Inu
  • Hymn 610 Nafenso tidzadzuka kwa ‘ke ngati maluwawo,
  • Hymn 481 USACHIMWE konse,
  • Hymn 1646 M’busa wokoma ndi Mbuyangayo,
  • Hymn 9 TAMANI Ambuye,
  • Hymn 598 Mlungu ali nane;
  • Hymn 397 MBUYE wathu, mutipatsa
  • Hymn 1738 “Senzani mtanda wanuwo.”
  • Hymn 935 Mtima ukachita nkhawa
  • Hymn 913 Kulibe gombe, nyanja,
  • Hymn 1811 Tipulumuka mommo,
  • Hymn 1735 “Sezani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 1232 Ambuye ndinu Mbusa, Bwenzi, ndi Wansembe wanga,
  • Hymn 77 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 163 MALO anachepa,
  • Hymn 332 NDIKONDWA kuganizirabe
  • Hymn 159 Kamwana Yesu ‘nabadwa,
  • Hymn 1117 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 43 GETSEMANI, Getsemani,
  • Hymn 62 Tchimo lonse ligonjera
  • Hymn 1504 Kodi ali ndi chilemba
  • Hymn 319 NDIDZATANI ine,
  • Hymn 771 Tsopano alandira
  • Hymn 1676 Kondwerani dzuwa lino Aleluya,
  • Hymn 581 Mtiphunzitse bwinotu,
  • Hymn 157 INU nonse ovutidwa,
  • Hymn 680 Mbendera yake ikupiza m’mlengalengamo,
  • Hymn 1634 Pakwitana Mbuye wanga
  • Hymn 1067 Ambuyathu, ndikhumba tsiku lija
  • Hymn 47 Anthu m’maiko onse
  • Hymn 927 Pakutsazikana nanu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version