Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye

  1. Home   »  
  2. Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye

Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye

 

KUDZA kwa Mbuye
kudzatero monga mphenzi,
Ing’anima M’mwamba choncho Iye,
Dziko lidzanjenjemera oyipa onse,
Nayamba kuthawa powona Iye.

Yesu akhala pampando,
Kuweruza makamuwo;
Nkhosa dzanja lamanjalo,
Mbuzi kudzanja lamanzelero.

Ayimba kumpando’ko wolemekezeka,
Mfumu ya Kumwamba
Mbuye Yesu,
Alira m’Gehenamo moto, moto, moto,
Ndipeze kuti madzi akumwa.

Udzachitanji mbale pobwera Ambuye,
Kudzaweruza dziko lapansi,
Ngati sudakonzeke khulupira Yesu,
Kuti upeze moyo wosatha.

Post navigation

Previous: Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga
Next: Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 477 YESU, muli pa chimpando
  • Hymn 755 Pamene padzakhalapo
  • Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,
  • Hymn 133 NSEMBE yake ya Kaini,
  • Hymn 553 M’munda muja ndaniyo
  • Hymn 1613 A Mulungu
  • Hymn 328 KULIBE vuto
  • Hymn 715 Mwapatsa Mwana wanu, ndi
  • Hymn 433 Zoipa ndi zabwino
  • Hymn 196 Tidzimba komweko nyimbo
  • Hymn 1349 Salephera, salephera,
  • Hymn 681 Ankhondo a Mulungu ‘nu, yendani m’njiramo,
  • Hymn 483 Ndife akuchoka,
  • Hymn 1126 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 484 YESU ndiye Mbusa,
  • Hymn 8 Nanu Atumwi akumveka aja,
  • Hymn 1626 Mbuye Yesu adzabwera,
  • Hymn 56 Masiku onse timakondwera
  • Hymn 941 Ndi Mbuyeyo tikhalamo,
  • Hymn 1395 Mulungu ali nane!
  • Hymn 896 Mbuye, ndinalema ine,
  • Hymn 906 Mulibe zoipa m’Dzikolo,
  • Hymn 183 MUDZE kwa Yesu, musachedwe.
  • Hymn 1119 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 378 KWEZANI mitu yanuyo,
  • Hymn 153 NDAKUMANA ndi bwenzi lokomalo,
  • Hymn 759 Ndilawako tsopanoli
  • Hymn 1640 Alinkudza Ambuye Yesu
  • Hymn 293 Tidziperekadi konse kwa Inu
  • Hymn 186 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 1236 Mbuye ndimva leroli
  • Hymn 482 TCHIMO musalole, musadziipitse,
  • Hymn 234 IMFA ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 85 MASO ndi maso ndi Kristu,
  • Hymn 1560 Mthandizi ndinu, mndithangate ine
  • Hymn 819 Lero tigone,
  • Hymn 729 Ndifuna kumva Inu,
  • Hymn 1820 Kwezani nane Ambuyathu,
  • Hymn 408 ABALE nonse mulindiranji?
  • Hymn 228 Ataya zoipa,
  • Hymn 84 LIDZE msanga dzuŵa lanu
  • Hymn 401 Dzuwa la lero lonseli
  • Hymn 955 Komwe ndi chimwemwe ine
  • Hymn 1441 Wochimwa iwe, bweratu
  • Hymn 1542 Titamire nthawi zonse
  • Hymn 354 Tinafunafunatu,
  • Hymn 1057 Ndilira ine kukayenda
  • Hymn 86 IYE wokhulupilira Yesu,
  • Hymn 83 MBUYEYO adzabwera,
  • Hymn 573 Ambuye, tikutamandani
  • Hymn 1587 Nditama Mlungu m’mtimamo,
  • Hymn 536 Ana inu, myamikeni
  • Hymn 1529 Mndithandize kukondana
  • Hymn 1644 Popachikidwa pa Golgotapo
  • Hymn 1101 Ngati mtima sumakonda
  • Hymn 912 Makomo afanana
  • Hymn 1681 Mphamvu za imfa ndi za Satana
  • Hymn 1715 Kodi misozi itisowa,
  • Hymn 1603 Zina za Yesu m;Mwambamo,
  • Hymn 1523 Atisangalatsa,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version