Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 64 LERO Kristu anauka,

  1. Home   »  
  2. Hymn 64 LERO Kristu anauka,

Hymn 64 LERO Kristu anauka,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 64 LERO Kristu anauka,

 

LERO Kristu anauka,
Aleluya.
Ndilo tsiku lokondwera.
Aleluya.
Iye kale anafera,
Aleluya.
Nawombola otaika,
Aleluya.

Timwimbire zomtamanda
Aleluya.
Ndiye Kristu wa Kumwamba
Aleluya.
Natsikira kumanda,
Aleluya.
Nalanditsa akuipa.
Aleluya

Koma masauko ake,
Aleluya.
Anatiwombola ife.
Aleluya.
Ndiye Mfumu ya mafumu,
Aleluya.
Mwana ndithu wa Mulungu.
Aleluya.

Timwimbire Mulungu wathu,
Aleluya.
Kuti atikonda ndithu:
Aleluya.
Mtamenso angelo inu,
Aleluya.
Ndiye ‘Tate, Mwana, Mzimu
Aleluya.

Post navigation

Previous: Hymn 63 POKUMBUKIRA mtandawo
Next: Hymn 65 NLA Mlungu dzuŵali:

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1770 Iye amazichita zamphamvu
  • Hymn 78 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 245 Ngakhale kuthengo
  • Hymn 893 Mtima wanga ndikonzera,
  • Hymn 693 Adzapambana Yesu ponse
  • Hymn 1010 Ndipo ngati ungolema,
  • Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,
  • Hymn 1136 Mulungu anditsogolera
  • Hymn 698 Polenga dzikoli,
  • Hymn 660 Tumizani kuunikako,
  • Hymn 974 Tsopano timenyana
  • Hymn 1521 Poyensedwa ife
  • Hymn 234 Kwa kutha kwa moyo,
  • Hymn 159 Kamwana Yesu ‘nabadwa,
  • Hymn 1318 Ndibwera kwa Ambuyeyo,
  • Hymn 1391 Ndiye wokondwa, E, munthuyo
  • Hymn 525 Afike masiku
  • Hymn 1182 Chikhulupiro chomwenso
  • Hymn 645 Kristu ndiye mwala wathu,
  • Hymn 83 Mpulumutsi Wokondedwa,
  • Hymn 1132 Mlungu adzandilandila,
  • Hymn 1178 Mawu omwewo, nyimbo yomweyi,
  • Hymn 96 MTIMA wanga uyamiketu,
  • Hymn 1641 Pakufika asonkhanitsa
  • Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu
  • Hymn 1107 Anthu onse pansi pano
  • Hymn 115 NTHAWI ija ya Sauli,
  • Hymn 1632 Ndi chiyembekezo ichi
  • Hymn 471 Mbuye, tili ana anu,
  • Hymn 69 KONDWERANI dzuŵa lino,
  • Hymn 65 Chisomo chodabwitsacho
  • Hymn 431 Pompano pandikonda
  • Hymn 131 MAWU a Mulungu awa,
  • Hymn 1229 Dzinalo la Yesu,
  • Hymn 880 Bwenzi lathu ndiye Yesu
  • Hymn 369 Lowani m’nyumba mwakemu
  • Hymn 1039 Usafune chuma chokha,
  • Hymn 1120 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 109 MUTHIRE, Yesu, m’mtimanga
  • Hymn 1633 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 279 MBUYE, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 463 MNANDIDZERA, Ambuye,
  • Hymn 243 KONDWANI nonsenu,
  • Hymn 1236 Mbuye ndimva leroli
  • Hymn 66 >ALELUYA, Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 1150 Pamtanda Mbuyanga ‘nafera,
  • Hymn 1805 Anafa m’mvula muja
  • Hymn 1485 Unachimwachimwa ndithu,
  • Hymn 1401 Imvani mawu ake, idzanitu,
  • Hymn 1839 Yehova ndiye Mbusa wanga sin’ngasowe konse;
  • Hymn 955 Komwe ndi chimwemwe ine
  • Hymn 1617 Anadzuka,
  • Hymn 1083 “Khala mwa Ine,” Yesu anatero;
  • Hymn 221 A! CHIKONDI chopambana,
  • Hymn 1619 Adzabwera,
  • Hymn 1344 Yamba ulendowo
  • Hymn 343 Auke,
  • Hymn 475 MZINDA woyerawo
  • Hymn 1613 A Mulungu
  • Hymn 313 MUNDIŴALIRE m’njira mwangamo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version