Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 64 LERO Kristu anauka,

  1. Home   »  
  2. Hymn 64 LERO Kristu anauka,

Hymn 64 LERO Kristu anauka,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 64 LERO Kristu anauka,

 

LERO Kristu anauka,
Aleluya.
Ndilo tsiku lokondwera.
Aleluya.
Iye kale anafera,
Aleluya.
Nawombola otaika,
Aleluya.

Timwimbire zomtamanda
Aleluya.
Ndiye Kristu wa Kumwamba
Aleluya.
Natsikira kumanda,
Aleluya.
Nalanditsa akuipa.
Aleluya

Koma masauko ake,
Aleluya.
Anatiwombola ife.
Aleluya.
Ndiye Mfumu ya mafumu,
Aleluya.
Mwana ndithu wa Mulungu.
Aleluya.

Timwimbire Mulungu wathu,
Aleluya.
Kuti atikonda ndithu:
Aleluya.
Mtamenso angelo inu,
Aleluya.
Ndiye ‘Tate, Mwana, Mzimu
Aleluya.

Post navigation

Previous: Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
Next: Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 731 Mundionetse, Yesu,
  • Hymn 343 Auke,
  • Hymn 277 GWIRA zintchito zako,
  • Hymn 1576 Khamulo liliko
  • Hymn 1079 Khalatu woyera,
  • Hymn 172 TADZA kukudyaku,
  • Hymn 1654 Mbuye, mutsaganetu
  • Hymn 767 Munali mwana, Yesu ‘Nu
  • Hymn 62 AMBUYE Yesu,
  • Hymn 1420 Abale ‘nu, abale ‘nu,
  • Hymn 934 Mnamwalira Inu paja,
  • Hymn 1579 Akhala mafumu
  • Hymn 1797 Chikondi chake chindidzera
  • Hymn 995 Taya zako zochenjera,
  • Hymn 1137 Masiku ena pali mdima,
  • Hymn 1402 Mverani Iye ati: idzanitu;
  • Hymn 1533 Ndipatsa inu mtimawu,
  • Hymn 132 MVERA mtima wanga ’we
  • Hymn 1355 Atate, Mwana, Mzimunso,
  • Hymn 63 POKUMBUKIRA mtandawo
  • Hymn 32 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 1300 Poyenda m’mdima bii,
  • Hymn 1237 Ine kanthu ndilibe
  • Hymn 11 NDI mitima yokondwera,
  • Hymn 250 MBUYANGA Yesu,
  • Hymn 1044 Yesu sakusiya konse;
  • Hymn 1317 Ambuye naitana ‘ne:
  • Hymn 142 Kukondwa kwa wodwalayo
  • Hymn 381 Chakudya changa chabwino
  • Hymn 600 Mbuye Yesu, myandikire,
  • Hymn 1212 Zina ndi zinanso
  • Hymn 984 Mpingo wa Mulungu
  • Hymn 158 Mzimu, mlonge m’mtimamo
  • Hymn 1336 Mwamva mawu a Mulungu;
  • Hymn 1770 Iye amazichita zamphamvu
  • Hymn 569 Tiimbe ndi kulalikira
  • Hymn 189 Koma Iye wandipeza;
  • Hymn 1793 Pakuwoloka mtsinje wa imfa
  • Hymn 1310 Yesu wondikondadi,
  • Hymn 723 Mundimvere, Mbuye wanga
  • Hymn 402 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 545 Anatifera tonsefe
  • Hymn 259 Zoipa zakanikadi,
  • Hymn 400 ONA Mwana wa Nkhosa,
  • Hymn 1358 Lemekeza Mfumu yathu,
  • Hymn 843 M’maiko monse, zisi zomwe,
  • Hymn 1350 Mvera Yesu, mvera Yesu,
  • Hymn 1282 Ndilinkudza kwa Ambuye,
  • Hymn 959 Ana akumwamba ndife,
  • Hymn 1056 Mkhalidwe wanu mundipatse,
  • Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 483 NTHAŴI yaubwana yatha,
  • Hymn 739 Ndilibe wondithangata ‘ne ‘yi,
  • Hymn 64 LERO Kristu anauka,
  • Hymn 845 Ufumu wanu, Mbuye Yesu,
  • Hymn 1760 Amithenga a Mulungu
  • Hymn 251 Kuli chimwemwe m’dzuwalo
  • Hymn 354 Tinafunafunatu,
  • Hymn 1058 Chimwemwe chija chamumtima
  • Hymn 1126 Ndifuna Inu, Yesu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version