Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,

Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,

 

AMITHENGA a Mulungu,
Anaimba nyimbo yomwe,
Posonkhana m’mlengalenga,
Natitu usiku womwe;
“Onse azilemekeza
Mlungu Wakumwambamwamba;
Akhalebe ndi mtendere
Anthu ali ponseponse.”

Amithenga anaimba
Ndi usiku m’mlengalenga.

Anamva abusa omwe
Anaŵeta nkhosa zawo.
Mthenga nati:
“Musaope;
Mumve ndikufotokoza:
Wabadwa usiku uno Yesu Kristu Ambuyathu
Ndiye Mpulumutsi wathu;
Anabadwa m’Betlehemu.”

Amithenga anaimba
Ndi usiku m’mlengalenga.

Yesu ndinu Mbuye wathu,
Munasiya za Kumwamba;
Munakhala mwana kuno;
Mnatifera mwaufulu.
Inu nonse amithenga,
Inu mumtamande Iye;
Anthu onse ali pansi Adza akondane naye.

Zoonazi amithenga
Anaimba m’mlengalenga.

Post navigation

Previous: Hymn 33 OWONADI mtima,
Next: Hymn 35 KODI mwaona chiyani,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 318 TINALI ambiri ife,
  • Hymn 327 Yesu salephera ‘yi.
  • Hymn 506 Ndikondwa kuti Yesu akonda,
  • Hymn 1646 M’busa wokoma ndi Mbuyangayo,
  • Hymn 1565 Mufike monga ngati njiwa yamtenderewo,
  • Hymn 97 Maso ndi maso ndi Kristu,
  • Hymn 202 NDIKHULUPIRIRA, Yesu,
  • Hymn 603 Mzimu wanu Wakuyera,
  • Hymn 721 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 58 Titasokera tinabwerera,
  • Hymn 641 Awiri aimamu,
  • Hymn 160 Kamwana kaja ‘nayamba
  • Hymn 845 Ufumu wanu, Mbuye Yesu,
  • Hymn 69 KONDWERANI dzuŵa lino,
  • Hymn 701 Inu Atatuwo,
  • Hymn 1683 Nsinga za imfa Iye ‘nadula,
  • Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 65 NLA Mlungu dzuŵali:
  • Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
  • Hymn 356 Tinafena m’nyanjamo,
  • Hymn 1451 Okoma ndiwo mawu
  • Hymn 1654 Mbuye, mutsaganetu
  • Hymn 491 KWA Yesu ndi kwabwinoko,
  • Hymn 1019 Tsata, tsata, nditsatadi Yesu;
  • Hymn 51 Mbuye dalitsani Afrika,
  • Hymn 7 “Mbuye Woyera! E, Woyeranokha!
  • Hymn 1576 Khamulo liliko
  • Hymn 816 Mdima wafika,
  • Hymn 707 Dalitseni, Mbuye, zonse
  • Hymn 463 MNANDIDZERA, Ambuye,
  • Hymn 392 ANU Mbuye ndifetu!
  • Hymn 781 Tatsegukani inutu,
  • Hymn 677 Ponse padakhala mdima
  • Hymn 478 YESU atiuza tiŵale ’fe.
  • Hymn 1807 Chithawa m’talitali
  • Hymn 59 Tinachoka munjira ya imfa,
  • Hymn 179 Ndinachimwa poganiza
  • Hymn 1168 Aleluya, muyenera!
  • Hymn 189 MLENDO ali pakhomo,
  • Hymn 1783 Tinasokera ngati nkhosa,
  • Hymn 1260 Yesu, mulikundipempha, Munaterodi:
  • Hymn 1799 Mulungu atipatsa mphamvu
  • Hymn 294 Yesu anali khanda
  • Hymn 1056 Mkhalidwe wanu mundipatse,
  • Hymn 123 Koma mudzisungire chuma cha Kumwamba
  • Hymn 1188 Akumangidwa ndi mzimuwo,
  • Hymn 240 Nyama za m’thengo
  • Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,
  • Hymn 1567 Mubwere Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,
  • Hymn 490 Yesu, ndikabwera
  • Hymn 1514 Dzinthu zakumundazo
  • Hymn 1218 Pakufa pangapo
  • Hymn 940 Ndamvatu kuti tifika komweko
  • Hymn 1776 Tiyeni timgwadire
  • Hymn 983 Nkhondo ya Satana
  • Hymn 314 E, moto wanu woyera
  • Hymn 326 Yesu, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 1753 Adzatipulumutsa
  • Hymn 1474 Zilepheradi zonse kugula moyowo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version