Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 12 NDITAMATU Ambuyangayu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 12 NDITAMATU Ambuyangayu,

Hymn 12 NDITAMATU Ambuyangayu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 12 NDITAMATU Ambuyangayu,

 

NDITAMATU Ambuyangayu,
Moyo wanga wonse ndidzam’tamatu;
Ndiponso m’dziko lakumwambako.
Masiku anga onse ndidzam’lemekeza Iye,
Sindizaleka konsekonse mmene ndili moyotu;
Pa dziko pano pena m’Mwambamo.

Ndiye wokondwa, E, munthuyo,
Wokhulupirira Mlungu yekhadi;
Wolenga dziko, nyanja, zonsezi.
Choona chake chonse chingokhalatu chosatha,
Apulumutsa onse namadyetsa anthu akewo;
Wokonda ndiye Mlungu wathuyo.

Mlungu kuwona athiratu,
Inde m’maso awo osapenyawo;
Natuma akumvera mpumulo.
Amathandiza inde aulendo awo ofokatu,
Akazi amasiye, maka ndi ana’wo onsewo;
Olira otonthoza mtimadi.

Nditama Ambuyangayu,
Moyo wanga wonse ndidzam’tamatu;
Ndiponso m’dziko la Kumwambako.
Masiku anga onse ndidzam’lemekeza Iye,
Sindidzaleka konsekonse mmene ndili moyotu;
Padziko pano pena m’Mwambamo.

Post navigation

Previous: Hymn 11 NDI mitima yokondwera,
Next: Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1574 Anthu ose ndi mitundu
  • Hymn 273 Mlungu akuyang’aniredi
  • Hymn 836 Kamoyo kanga katha lero lino,
  • Hymn 1401 Imvani mawu ake, idzanitu,
  • Hymn 656 Ndipumulire panupo,
  • Hymn 217 E! kwa Inu, E! kwa Inu!
  • Hymn 219 YESU Mbuyetu, mwafera
  • Hymn 126 DAVIDE kubusa kuja,
  • Hymn 658 Ndichitireni, Mbuye ‘ne,
  • Hymn 1138 Masiku onse m’mtima mwanga
  • Hymn 379 MTSINJE woyerawo
  • Hymn 848 Mudze, mlowe m’mtimamu,
  • Hymn 440 Yesu wakufatsa mtima
  • Hymn 1029 Nkhawa tilibe; Yesuyo
  • Hymn 275 Mlungu akuyang’aniredi,
  • Hymn 143 Lero lino Mbuye Yesu
  • Hymn 245 Ngakhale kuthengo
  • Hymn 644 M’wasunge, m’wayendetse
  • Hymn 474 Yesu ndafikatu,
  • Hymn 139 Bwerani inu nonse, inu nonse,
  • Hymn 146 Inu ndidzatama
  • Hymn 1544 Wakunga mwana ine,
  • Hymn 1440 Yesu alindira,
  • Hymn 407 ADZAPAMBANA Yesu ponse
  • Hymn 403 NDIYIMBA ndi chimwemwe lero,
  • Hymn 347 YESU, ndipemphera
  • Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,
  • Hymn 110 MZIMU ndi mtogoleri
  • Hymn 877 Zokoma ndithu nthawizi
  • Hymn 32 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 1370 Mphepo yay’kulu yakuombayo,
  • Hymn 74 Ndipereka zanga zonse
  • Hymn 1693 Koma masauko ake Aleluya
  • Hymn 840 Ambuye munapatsa tsiku
  • Hymn 424 MTIDZUTSE, Mbuyetu,
  • Hymn 738 Mommuno, Mbuye, mkate wanuwu,
  • Hymn 436 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 602 Mpulumutsi wakukoma,
  • Hymn 1516 Pakudera nkhawa ‘ne,
  • Hymn 1233 Tsopano ndibukitsabe chikondi chanu chija
  • Hymn 547 Anatikondakonda ‘Ye.
  • Hymn 468 Ife tikondana nanu,
  • Hymn 1083 “Khala mwa Ine,” Yesu anatero;
  • Hymn 110 Ndaima nji pa Kristuyo,
  • Hymn 596 Mlungu ali nane;
  • Hymn 1654 Mbuye, mutsaganetu
  • Hymn 1388 Tiimbire Mlungu wathu
  • Hymn 1103 Ndakudani, mnandikonda
  • Hymn 1202 Ndikhumba mtimawo
  • Hymn 1585 Dzina ili ndi lokoma
  • Hymn 1760 Amithenga a Mulungu
  • Hymn 541 Ana inu, yamikani
  • Hymn 22 Mbuye mtsitsimutse!
  • Hymn 804 Muchotse zonse zoti bii
  • Hymn 161 Tibwera ndi tianato
  • Hymn 790 Zimbalame zonsezi
  • Hymn 1820 Kwezani nane Ambuyathu,
  • Hymn 726 Mundidzze ndi chikondi,
  • Hymn 720 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 33 Tamandani Mbuye,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version