Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 9 TAMANI Ambuye,

  1. Home   »  
  2. Hymn 9 TAMANI Ambuye,

Hymn 9 TAMANI Ambuye,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 9 TAMANI Ambuye,

 

TAMANI Ambuye,
Wamphamvu ndi Iye;
Akhala m’ulemu,
Kumwamba komweko.
Chikopa cholimba,
Ndi kothaŵiranso;
Kwa anthu akewo,
Kotero ndi Mlungu.

Uzani zamphamvu,
Imbani chisomo;
Za Mwini ulemu,
Ambuye wathuyo.
Poomba chimphepo
Mvulanso ndi bingu;
Padziko, pathambo,
Akhala ponsepo.

Zozizwa zam’dziko,
Za M’mwamba zonsezi;
Mulungu wamphamvu,
Munalenga zonse;
Muyendetsa mwezi,
Nyenyezi ndi dzuŵa;
Zolengedwa zonse,
Zimvera Ambuye.

Sitiha ifedi,
Kukamba zokoma;
Za Inu Mulungu,
Wolera anthuwa.
Zifika ndi mphepo,
Ndi mvula ndi dzuŵa;
Zigwera ponsepo,
Pa anthu onsewa.

Wamphamvu yosatha,
Chikondichangwiro;
Angelo akonda,
Kutama Mulungu.
Ndiponso ifetu,
Ana ‘nu tonse ‘fe;
Tiimba nyimboyi,
Yotama Ambuye.

Post navigation

Previous: Hymn 8 MITAMBO inu yakumwambako
Next: Hymn 10 TSOPANO linoli,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1292 Wolapa mtima simunyozadi,
  • Hymn 1471 Ukapenya kwa Yesu uliko moyoko,
  • Hymn 1570 Mutidziwitse ‘Tate wathu,
  • Hymn 459 Aphunzitse anthuwo,
  • Hymn 79 Mlendo ali pakhomo,
  • Hymn 679 Zipata zachitsulo zitseguke zonse mbee!
  • Hymn 1799 Mulungu atipatsa mphamvu
  • Hymn 721 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 337 PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;
  • Hymn 834 Tiyamike Mlungu wotipatsa zachifundozi,
  • Hymn 132 MVERA mtima wanga ’we
  • Hymn 1119 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 466 OSANATU, osana,
  • Hymn 1761 Amithenga anaimba
  • Hymn 77 MMENE Yesu adzabwera,
  • Hymn 897 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 994 Limba mtima mbale wanga,
  • Hymn 1114 Akukumbukira
  • Hymn 228 Ataya zoipa,
  • Hymn 658 Ndichitireni, Mbuye ‘ne,
  • Hymn 1406 Kodi ukafuna
  • Hymn 504 Pakumyamika Iye
  • Hymn 1731 Ife tinachimwadi,
  • Hymn 89 Muli mphamvu yodabwitsatu
  • Hymn 1399 Yesu ponong’oneza, idzanitu;
  • Hymn 77 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 1320 Ndayang’anira Mbuyeyo,
  • Hymn 1174 Sindinanyengedwa konse;
  • Hymn 1141 Pakulekana ifetu
  • Hymn 1738 “Senzani mtanda wanuwo.”
  • Hymn 1402 Mverani Iye ati: idzanitu;
  • Hymn 1640 Alinkudza Ambuye Yesu
  • Hymn 30 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 1186 Yesu anafa pamtandapo,
  • Hymn 218 NDIPEREKA zanga zonse
  • Hymn 1110 Mulungu wanga,
  • Hymn 4 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 1365 Zozizwa za m’dziko,
  • Hymn 389 NDIMAMVA njala, Yesu,
  • Hymn 1711 Kwa munthu wasokerayo
  • Hymn 480 TIANA ife tingofoka,
  • Hymn 1394 Paphiri ndi padambo
  • Hymn 109 Chiyembekezo changacho
  • Hymn 377 Yehova, Mbusa wangadi,
  • Hymn 57 Ife tiyembekezera Yesu,
  • Hymn 1730 Anapeputsidwako,
  • Hymn 477 Mpulumutsi, Mbusa wathu,
  • Hymn 1540 Pankhope pathu mthirepo
  • Hymn 1611 Nadzuka m’mandamo
  • Hymn 490 Yesu, ndikabwera
  • Hymn 756 Sindili woyenera ‘ne,
  • Hymn 226 Nditama mwaziwo!
  • Hymn 1089 Ndionetsere kuunika
  • Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu
  • Hymn 411 TAMVA mawu omwewo,
  • Hymn 1258 Zonse zina sizikwana,
  • Hymn 135 Kudziwa ukudziwa,
  • Hymn 1782 Poyamba paja analenga
  • Hymn 1072 Mudzaze Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
  • Hymn 935 Mtima ukachita nkhawa

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version