Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 9 TAMANI Ambuye,

  1. Home   »  
  2. Hymn 9 TAMANI Ambuye,

Hymn 9 TAMANI Ambuye,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 9 TAMANI Ambuye,

 

TAMANI Ambuye,
Wamphamvu ndi Iye;
Akhala m’ulemu,
Kumwamba komweko.
Chikopa cholimba,
Ndi kothaŵiranso;
Kwa anthu akewo,
Kotero ndi Mlungu.

Uzani zamphamvu,
Imbani chisomo;
Za Mwini ulemu,
Ambuye wathuyo.
Poomba chimphepo
Mvulanso ndi bingu;
Padziko, pathambo,
Akhala ponsepo.

Zozizwa zam’dziko,
Za M’mwamba zonsezi;
Mulungu wamphamvu,
Munalenga zonse;
Muyendetsa mwezi,
Nyenyezi ndi dzuŵa;
Zolengedwa zonse,
Zimvera Ambuye.

Sitiha ifedi,
Kukamba zokoma;
Za Inu Mulungu,
Wolera anthuwa.
Zifika ndi mphepo,
Ndi mvula ndi dzuŵa;
Zigwera ponsepo,
Pa anthu onsewa.

Wamphamvu yosatha,
Chikondichangwiro;
Angelo akonda,
Kutama Mulungu.
Ndiponso ifetu,
Ana ‘nu tonse ‘fe;
Tiimba nyimboyi,
Yotama Ambuye.

Post navigation

Previous: Hymn 1858 Ha! Chikondi cha Mulungu,
Next: Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 965 Mundiuze, aulendo,
  • Hymn 1130 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja
  • Hymn 812 Ndi ena sanamvera ‘yi,
  • Hymn 1222 Bwenzi ndimamkomanayo
  • Hymn 923 Dothili kudothilo,
  • Hymn 790 Zimbalame zonsezi
  • Hymn 275 Mlungu akuyang’aniredi,
  • Hymn 1716 Anena mawu m’mtanda momwe,
  • Hymn 1793 Pakuwoloka mtsinje wa imfa
  • Hymn 875 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 87 IDZANI nonse ’nu
  • Hymn 1430 Ndipo pakulowa
  • Hymn 1485 Unachimwachimwa ndithu,
  • Hymn 930 Leroli chisoni chokha,
  • Hymn 39 Poyang’ana ena ndi ndalamatu,
  • Hymn 1812 Kuzani Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 468 NDIKONDWA kuti
  • Hymn 329 MUMZINDA wa Mulungu
  • Hymn 296 TIYENI Akhristu,
  • Hymn 1393 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 1275 Mtima ‘we siya ndi Yesu nsonizi,
  • Hymn 641 Awiri aimamu,
  • Hymn 550 Wosauka Iyedi
  • Hymn 651 Ikhale ngati nyali
  • Hymn 169 ’MVANI liu lomwe
  • Hymn 349 Aitana,
  • Hymn 771 Tsopano alandira
  • Hymn 950 Sindidapempha kale Mbuye ‘yi,
  • Hymn 16 Chikhulupiriro chathu
  • Hymn 448 Yesu ndi wofatsa,
  • Hymn 116 Nkhosa zanga zimandimva
  • Hymn 75 MBUYE, mutsaganetu
  • Hymn 592 Kuti m’Mwambamo
  • Hymn 580 Mwana wakuyera ‘Nu,
  • Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 160 MADALITSO ngati mvumbi,
  • Hymn 727 Imfa ikandifikira,
  • Hymn 402 BWERANITU, bweranitu,
  • Hymn 1136 Mulungu anditsogolera
  • Hymn 731 Mundionetse, Yesu,
  • Hymn 978 Mtima wanu wonse ndithu
  • Hymn 16 MTIMA wanga lemekeza,
  • Hymn 1384 Mphamvu yake inalenga
  • Hymn 526 Mnandidzera, Ambuye,
  • Hymn 1234 Ati Yesu Mbuyeyo:
  • Hymn 427 AULENDO amayenda
  • Hymn 178 ZAMBIRI zogona m’kholamo,
  • Hymn 79 Mlendo ali pakhomo,
  • Hymn 268 Potuluka m’mudzimo
  • Hymn 1759 Powalitsira omwe
  • Hymn 1559 Wotsogolera, munditsogolere
  • Hymn 464 Yesu atiuza tiyambemo,
  • Hymn 1108 Khala chete mtima wanga,
  • Hymn 1302 Ndi inetu sinditha ‘yi
  • Hymn 167 KODI mwalandira Yesu?
  • Hymn 461 ANA inu, myamikeni
  • Hymn 385 SINDILI woyenera ’ne,
  • Hymn 86 Mwandipatulira ine,
  • Hymn 1370 Mphepo yay’kulu yakuombayo,
  • Hymn 313 Muthire, Yesu, m’mtimanga

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version