Hymn 240 Nyama za m’thengo December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Believers Christian Hymns Chichewa Believers Christian Hymns Hymn 240 Nyama za m’thengo Nyama za m’thengo Ndi mbalamezo Zili nazo zogonamo, Koma Mwana wa Mlungu Analibe nyumba, M’mapululu nagonatu.