Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 240 Nyama za m’thengo
Nyama za m’thengo
Ndi mbalamezo
Zili nazo zogonamo,
Koma Mwana wa Mlungu
Analibe nyumba,
M’mapululu nagonatu.
Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 240 Nyama za m’thengo
Nyama za m’thengo
Ndi mbalamezo
Zili nazo zogonamo,
Koma Mwana wa Mlungu
Analibe nyumba,
M’mapululu nagonatu.