Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,

Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,

 

KONDA dzinalo la Yesu,
Mwana wosawuka’we;
Ndilo lothandiza anthu,
Khala nalo ponse phee.

Dzina la Yesuyo,
N’lokondwetsa onsewo;
M’mwambamo, ponsepo,
Litonthoza m’mtimamo.

Konda dzinalo la Yesu,
M’moyo mwako monsemo;
Mmene ulikuyesedwa,
Tchula dzina lakelo.

Dzina ili ndi lokoma,
La Mtetezi wathuyo;
Mmene adzatilandira,
M’mwamba tidzakondwadi.

Mbuye Yesu tim’tamanda,
Ndi nyimbo zathu zonse;
Mfumu ya mafumu onse,
Yesu timayesadi.

Post navigation

Previous: Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye
Next: Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,
  • Hymn 1039 Usafune chuma chokha,
  • Hymn 214 Msanga adzachitseka chitseko,
  • Hymn 1551 Mukhale m’kati mwathu,
  • Hymn 465 Yesu atiuza tiwale pa
  • Hymn 311 VALANI zida tizinka kwathuko,
  • Hymn 368 MULUNGU wanga, Dzuŵatu
  • Hymn 498 AMBUYE, mtidalitsetu,
  • Hymn 1753 Adzatipulumutsa
  • Hymn 219 Mtenderewo wosanyenga
  • Hymn 420 FESANI mbewuzo,
  • Hymn 253 Adzakhala pampandopo
  • Hymn 226 BWENZI ndinamkomanayo
  • Hymn 1848 Tiyamike Mlungu wathu
  • Hymn 295 Kubadwa kwa Yesu
  • Hymn 525 Afike masiku
  • Hymn 1044 Yesu sakusiya konse;
  • Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu
  • Hymn 391 Mufafanize m’bukumo
  • Hymn 1068 Ambuye, thandizenitu
  • Hymn 378 Ku madzi ake odikha
  • Hymn 215 Choka, choka,
  • Hymn 1375 Ndi anamwali obvekedwa mbuu!
  • Hymn 1625 Ife tonse tikumbuke
  • Hymn 173 MWAMVA Mawu a Mulungu;
  • Hymn 259 Zoipa zakanikadi,
  • Hymn 1388 Tiimbire Mlungu wathu
  • Hymn 1705 Pa Iye padzapo
  • Hymn 242 NDIIMBA mumtima mokondwa,
  • Hymn 1331 Yesu wathu Mbuyeyo
  • Hymn 992 Mukandipweteka,
  • Hymn 230 AMBUYANGA Yesu,
  • Hymn 638 Ndi Mzimutu Woyera
  • Hymn 109 MUTHIRE, Yesu, m’mtimanga
  • Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,
  • Hymn 724 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 1593 Wina atikonda ife,
  • Hymn 106 Ife, tapulumukadi,
  • Hymn 1252 Pakukumbukira zanga
  • Hymn 1298 Ndikhulupira ‘Nu,
  • Hymn 1246 Ambuyanga, ndalephera,
  • Hymn 382 M’wabatize anzathuwa,
  • Hymn 1851 Anthu onse, anthu onse,
  • Hymn 1529 Mndithandize kukondana
  • Hymn 1514 Dzinthu zakumundazo
  • Hymn 592 Kuti m’Mwambamo
  • Hymn 1154 Zakutsogolo sitidziwa ‘yi;
  • Hymn 1683 Nsinga za imfa Iye ‘nadula,
  • Hymn 322 PAKUYITANIDWA munthu pa dziko ino,
  • Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 1118 Ndifuna Inu Yesu,
  • Hymn 966 Kodi inu, aulendo,
  • Hymn 1237 Ine kanthu ndilibe
  • Hymn 708 Peturo ‘nafusa Hananiya:
  • Hymn 881 Tili nazo zotiyesa,
  • Hymn 1416 Mbuye wanga ndilikumva,
  • Hymn 721 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 144 Yesu, ndipemphera
  • Hymn 231 Mwazi wa Yesu wokondwa
  • Hymn 308 AULENDO, munka kuti

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version