Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,

Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,

 

KONDA dzinalo la Yesu,
Mwana wosawuka’we;
Ndilo lothandiza anthu,
Khala nalo ponse phee.

Dzina la Yesuyo,
N’lokondwetsa onsewo;
M’mwambamo, ponsepo,
Litonthoza m’mtimamo.

Konda dzinalo la Yesu,
M’moyo mwako monsemo;
Mmene ulikuyesedwa,
Tchula dzina lakelo.

Dzina ili ndi lokoma,
La Mtetezi wathuyo;
Mmene adzatilandira,
M’mwamba tidzakondwadi.

Mbuye Yesu tim’tamanda,
Ndi nyimbo zathu zonse;
Mfumu ya mafumu onse,
Yesu timayesadi.

Post navigation

Previous: Hymn 91 NDITAME Mlungu m’mtimamo,
Next: Hymn 93 YAMIKANI dzina la Yesu Khrisituyo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1034 Mkristu, ulimbike
  • Hymn 1203 Zambiri zangazo
  • Hymn 619 Tilimalima m’minda,
  • Hymn 935 Mtima ukachita nkhawa
  • Hymn 549 Ndiye Mbuye, Mfumu yanga,
  • Hymn 1222 Bwenzi ndimamkomanayo
  • Hymn 362 Imvani Yesu akuti:
  • Hymn 882 Kodi tikulema nazo
  • Hymn 1846 Mtima wanga uyamike
  • Hymn 1415 Iye anatsika m’Mwamba,
  • Hymn 768 Ndi ife tinga mbewuzo
  • Hymn 1377 Ndi amithenga akumwambako,
  • Hymn 977 Musagonje, anthu inu,
  • Hymn 669 Anyamata limikani,
  • Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,
  • Hymn 754 Ndi mtanda uli m’maso mbuu,
  • Hymn 488 Ndikabwera, Mbuye
  • Hymn 1259 Ndikhulupirira bwino
  • Hymn 278 TITHAŴIRENJI ifetu
  • Hymn 1668 Kumdziwitsa ndiko moyo,
  • Hymn 572 Anadza nazo mphatso zake
  • Hymn 113 Likalira llipengalo,
  • Hymn 709 Munthu aganize
  • Hymn 354 Tinafunafunatu,
  • Hymn 1064 Moyowo
  • Hymn 809 Madzulo aja kalelo
  • Hymn 1508 Mundinyemere ‘ne
  • Hymn 839 Adani sindiopa mukalipo;
  • Hymn 1189 Ambuye Mulungu,
  • Hymn 76 Ndipereka zanga zonse
  • Hymn 259 CHISOMO chodabwitsacho,
  • Hymn 1642 M’khola mwa ng’ombe ku Betelehemu
  • Hymn 106 Ife, tapulumukadi,
  • Hymn 774 Tibatizidweko,
  • Hymn 1422 Abwenzi ‘nu, abwenzi ‘nu,
  • Hymn 1758 Poti Mulungu wathu
  • Hymn 95 TAMANI mphamvu ya Yesu,
  • Hymn 1267 Kwa Inu Yesu ndilira,
  • Hymn 65 NLA Mlungu dzuŵali:
  • Hymn 472 YESU, ndikabwera
  • Hymn 1560 Mthandizi ndinu, mndithangate ine
  • Hymn 663 Anyamata a Mulungu,
  • Hymn 1807 Chithawa m’talitali
  • Hymn 121 MULUNGU, anthu ’fe
  • Hymn 775 Mwa anthu onsewo
  • Hymn 1605 Yesu, dzina lokondwetsa
  • Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga
  • Hymn 946 Ngakhale enawo aleke kwimbako,
  • Hymn 1655 Mbuye Yesu,
  • Hymn 962 Inde Mbuye, tibweradi,
  • Hymn 63 POKUMBUKIRA mtandawo
  • Hymn 1833 Podwala ine pobvutidwa Andisamalira;
  • Hymn 271 Zoipa zangazi
  • Hymn 621 Wolenga ndi Yemweyo
  • Hymn 1442 Khulupira mawu onse
  • Hymn 889 Pemphera m’mbanda kucha,
  • Hymn 1849 Nthawi zonse monga ‘Tate
  • Hymn 255 KHALA chete mtima wanga
  • Hymn 714 Dzuwa ndi mvula yonseyo
  • Hymn 1575 Tifuna kuti komweko

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version