Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 9 TAMANI Ambuye,

  1. Home   »  
  2. Hymn 9 TAMANI Ambuye,

Hymn 9 TAMANI Ambuye,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 9 TAMANI Ambuye,

 

TAMANI Ambuye,
Wamphamvu ndi Iye;
Akhala m’ulemu,
Kumwamba komweko.
Chikopa cholimba,
Ndi kothaŵiranso;
Kwa anthu akewo,
Kotero ndi Mlungu.

Uzani zamphamvu,
Imbani chisomo;
Za Mwini ulemu,
Ambuye wathuyo.
Poomba chimphepo
Mvulanso ndi bingu;
Padziko, pathambo,
Akhala ponsepo.

Zozizwa zam’dziko,
Za M’mwamba zonsezi;
Mulungu wamphamvu,
Munalenga zonse;
Muyendetsa mwezi,
Nyenyezi ndi dzuŵa;
Zolengedwa zonse,
Zimvera Ambuye.

Sitiha ifedi,
Kukamba zokoma;
Za Inu Mulungu,
Wolera anthuwa.
Zifika ndi mphepo,
Ndi mvula ndi dzuŵa;
Zigwera ponsepo,
Pa anthu onsewa.

Wamphamvu yosatha,
Chikondichangwiro;
Angelo akonda,
Kutama Mulungu.
Ndiponso ifetu,
Ana ‘nu tonse ‘fe;
Tiimba nyimboyi,
Yotama Ambuye.

Post navigation

Previous: Hymn 8 MITAMBO inu yakumwambako
Next: Hymn 10 TSOPANO linoli,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 965 Mundiuze, aulendo,
  • Hymn 552 Analira ndaniyo
  • Hymn 469 Lero mkhale nafe ndithu,
  • Hymn 67 PAMENEPO pokhala madzulo,
  • Hymn 260 Angelo aitana,
  • Hymn 460 E! ang’ono ndifetu,
  • Hymn 765 Chikondi chili m’chikhomu
  • Hymn 1792 Mulungu ndiye wachifundo,
  • Hymn 689 Anapeza Mwana
  • Hymn 1234 Ati Yesu Mbuyeyo:
  • Hymn 239 TILI ndi mtendere
  • Hymn 636 Yehova Mlungu wathu,
  • Hymn 543 Kuli kaphiri m’talimo
  • Hymn 491 KWA Yesu ndi kwabwinoko,
  • Hymn 1346 Ndaima pano, ndaima pakhomo:Lowa, lowa, lowa, lowa!
  • Hymn 896 Mbuye, ndinalema ine,
  • Hymn 417 M’BWERE Mlungu Mbuye wathu,
  • Hymn 164 WANENA ndi Yesu,
  • Hymn 1675 Lambira Mfumuyo
  • Hymn 317 UKATHA moyo wanga
  • Hymn 186 MVERANI mbiri yozizwitsa
  • Hymn 1647 Kubweza inetu, kubweza inetu,
  • Hymn 139 Bwerani inu nonse, inu nonse,
  • Hymn 1355 Atate, Mwana, Mzimunso,
  • Hymn 845 Ufumu wanu, Mbuye Yesu,
  • Hymn 397 Yesu Mbusa, mutimvere,
  • Hymn 1853 Etu ine, etu ine,
  • Hymn 205 KWA Inu Yesu ndilira,
  • Hymn 1541 Tionetseni tonsetu
  • Hymn 470 Mutiletse tisaname
  • Hymn 589 Koma ineyu
  • Hymn 201 Ngati zakuipa zathu
  • Hymn 43 Ulendo wathu ukadzatha
  • Hymn 315 YENDANI munjira yake,
  • Hymn 600 Mbuye Yesu, myandikire,
  • Hymn 1311 Pothawira pena ‘yi,
  • Hymn 1286 E, ndikukhulupirani,
  • Hymn 1283 Yesu ndikhulupirira
  • Hymn 790 Zimbalame zonsezi
  • Hymn 1383 Dzina lake tibukitsa,
  • Hymn 714 Dzuwa ndi mvula yonseyo
  • Hymn 1504 Kodi ali ndi chilemba
  • Hymn 736 Mndidyetse m’chipululu
  • Hymn 745 Anatifera nsembe Iyeyo,
  • Hymn 1168 Aleluya, muyenera!
  • Hymn 390 A! YESU, ndapangana
  • Hymn 144 AMENE adzavomereza ndithu,
  • Hymn 264 KHALATU woyera, pempheratu m’tseri;
  • Hymn 596 Mlungu ali nane;
  • Hymn 238 Mbuye Yesu, lowani m’mtima,
  • Hymn 300 AKRISTU limbikani,
  • Hymn 1009 Ndi m’kutero udzadziwa
  • Hymn 319 NDIDZATANI ine,
  • Hymn 553 M’munda muja ndaniyo
  • Hymn 75 Ndiperekatu
  • Hymn 1643 Kufuna inetu, kufuna inetu,
  • Hymn 1345 Iwe tiye, iwe tiye,
  • Hymn 105 Tiyamike Mbuye Yesu
  • Hymn 1520 Mbuye, Mawu anu
  • Hymn 133 Yesu watidzera, watidzera,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version