Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 9 TAMANI Ambuye,

  1. Home   »  
  2. Hymn 9 TAMANI Ambuye,

Hymn 9 TAMANI Ambuye,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 9 TAMANI Ambuye,

 

TAMANI Ambuye,
Wamphamvu ndi Iye;
Akhala m’ulemu,
Kumwamba komweko.
Chikopa cholimba,
Ndi kothaŵiranso;
Kwa anthu akewo,
Kotero ndi Mlungu.

Uzani zamphamvu,
Imbani chisomo;
Za Mwini ulemu,
Ambuye wathuyo.
Poomba chimphepo
Mvulanso ndi bingu;
Padziko, pathambo,
Akhala ponsepo.

Zozizwa zam’dziko,
Za M’mwamba zonsezi;
Mulungu wamphamvu,
Munalenga zonse;
Muyendetsa mwezi,
Nyenyezi ndi dzuŵa;
Zolengedwa zonse,
Zimvera Ambuye.

Sitiha ifedi,
Kukamba zokoma;
Za Inu Mulungu,
Wolera anthuwa.
Zifika ndi mphepo,
Ndi mvula ndi dzuŵa;
Zigwera ponsepo,
Pa anthu onsewa.

Wamphamvu yosatha,
Chikondichangwiro;
Angelo akonda,
Kutama Mulungu.
Ndiponso ifetu,
Ana ‘nu tonse ‘fe;
Tiimba nyimboyi,
Yotama Ambuye.

Post navigation

Previous: Hymn 1858 Ha! Chikondi cha Mulungu,
Next: Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 982 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 281 MBUYE, mwatiuza ’fe
  • Hymn 1799 Mulungu atipatsa mphamvu
  • Hymn 379 MTSINJE woyerawo
  • Hymn 875 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 347 Mfumu iyi,
  • Hymn 448 CHIFUKWA cha zokoma mtima zonse zaulelezo,
  • Hymn 755 Pamene padzakhalapo
  • Hymn 126 Mwa ine, moyo wanga ndi Yesu
  • Hymn 1552 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 1730 Anapeputsidwako,
  • Hymn 22 Mbuye mtsitsimutse!
  • Hymn 650 Tikondwa tonse ndi kukuthokazani Nu
  • Hymn 147 Ndisauka, ndinachimwa,
  • Hymn 1296 Chionerere mwaziwo
  • Hymn 693 Adzapambana Yesu ponse
  • Hymn 270 Zoopsya zopambana
  • Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,
  • Hymn 48 Ngakhale alemera
  • Hymn 1776 Tiyeni timgwadire
  • Hymn 1624 Koma anthu onse omwe
  • Hymn 737 Mommuno, Mbuye, tionanetu,
  • Hymn 445 TILIMALIMA m’minda,
  • Hymn 1739 Ife timakufunani
  • Hymn 1681 Mphamvu za imfa ndi za Satana
  • Hymn 15 Mbuye, chifundo chanu chitigwere
  • Hymn 836 Kamoyo kanga katha lero lino,
  • Hymn 1266 E, chimwemwe chachikulu, N’taperekadi
  • Hymn 1139 Namondwe akawombabe,
  • Hymn 318 TINALI ambiri ife,
  • Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,
  • Hymn 259 CHISOMO chodabwitsacho,
  • Hymn 1678 Yesu nkana saoneka, Aleluya,
  • Hymn 1319 Ambuye naitana ‘ne:
  • Hymn 567 M’nyumba zonse ponseponse
  • Hymn 1527 Ndiye Mzimu Wakuyera
  • Hymn 1558 Wosangalatsa, ine ndikalira
  • Hymn 1780 Titame Mlungu Wakumwamba,
  • Hymn 153 Pemphero ndiko kufuna,
  • Hymn 1225 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 415 Tidzalandirabe komwe
  • Hymn 1757 Udzadziwitsa anthu
  • Hymn 1690 Titama Yesuyo,
  • Hymn 1197 Ndafoka ine kale,
  • Hymn 1002 Haya! ‘Nzanga taonani Yoonekayo
  • Hymn 477 YESU, muli pa chimpando
  • Hymn 1348 Akupeza, akupeza,
  • Hymn 1784 Komweko titasaukira,
  • Hymn 937 Chitsime chachikondi
  • Hymn 1004 A! mizimu yakuipa
  • Hymn 254 Adzanena kwa anthuwo
  • Hymn 30 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 998 Anatilemba Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 439 MLUNGU wathu mwatifitsa
  • Hymn 436 YEHOVA Mlungu wathu,
  • Hymn 376 PAMTANDA Mbuye anafera,
  • Hymn 232 WAFUNAFUNA ine
  • Hymn 177 ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,
  • Hymn 389 Ambuye, mtidalitsetu,
  • Hymn 587 Mutitsuke,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version