Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,

  1. Home   »  
  2. Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,

Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,

 

Yesu, dzina lakukonda,
Lopambana onse ena,
Tonse tidzaligwadira
Ndi mitima yochepetsa.

Yesu, dzina lokondwetsa
Akuipa a padziko,
Kale linatidziŵitsa
Mpulumutsi ndiye Yesu.

Yesu dzina lakufatsa,
Anamutcha ’kali Mwana,
M’mene analoŵa kale
M’dziko lino lakudana.

Yesu, dzina ndi lomweli
La pa dziko lino lonse,
Ndi lamphamvu yolanditsa
Anthu mu masoka onse.

Yesu, dzina lakukonda
La Mwanayo wa Mulungu,
Ife anthu osauka
Tithaŵira nalo kwanu.

Post navigation

Previous: Hymn 87 IDZANI nonse ’nu
Next: Hymn 89 INDE, ndifuna kumvatu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 200 Ndi tsopano tilindira
  • Hymn 1280 Kuti mundipatsa mphamvu yopambanayo;
  • Hymn 1335 Wandifera Yesuyo
  • Hymn 758 Sindili woyenera ‘ne;
  • Hymn 766 Monga zomera zonsezo
  • Hymn 994 Limba mtima mbale wanga,
  • Hymn 319 NDIDZATANI ine,
  • Hymn 484 YESU ndiye Mbusa,
  • Hymn 1213 Mwamva Yesu m’mtimamo,
  • Hymn 1060 Mubwere, Mzimu wa mpumulo
  • Hymn 335 Mtembenuke mtima wanu,
  • Hymn 2 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 1828 Timtamande Iye ndi moyo wathunso
  • Hymn 1349 Salephera, salephera,
  • Hymn 386 MONGATU mawu anuwo,
  • Hymn 1495 Simbani bwinobwino
  • Hymn 202 Timpemphere kutipatsa
  • Hymn 1441 Wochimwa iwe, bweratu
  • Hymn 1500 Simbani Mbiri yomwe,
  • Hymn 401 A MULUNGU,
  • Hymn 1237 Ine kanthu ndilibe
  • Hymn 3 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 188 Ine ndili ndi manyazi
  • Hymn 839 Adani sindiopa mukalipo;
  • Hymn 1402 Mverani Iye ati: idzanitu;
  • Hymn 1631 Mudzabwera, mudzabwera;
  • Hymn 1393 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 1546 Mubwere Mzimu Inu
  • Hymn 471 YESU Mbuye ’Nu wofatsa
  • Hymn 871 Tiphatikane tonsefe okonda Yesu Kristu;
  • Hymn 175 A! MBUSA wathu amvatu
  • Hymn 655 Ndiphunzitseni, Mbuyetu,
  • Hymn 1721 Mapazi ake namvatu
  • Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;
  • Hymn 1412 Imfa idzafika msanga;
  • Hymn 262 Tumphatumpha moyo wanga,
  • Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,
  • Hymn 319 Koma zina sizinadziwa ayi,
  • Hymn 1642 M’khola mwa ng’ombe ku Betelehemu
  • Hymn 878 Zokoma inde nthawizi
  • Hymn 910 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 129 WODALA ndiye munthuyo,
  • Hymn 874 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 55 UNAKHETSEDWA mwazi do!
  • Hymn 825 Mpatse ana ‘ng’ono
  • Hymn 1507 Ndikampempha anditenge,
  • Hymn 722 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1307 Ndi ine simufuna ‘yi
  • Hymn 174 Haya, anzathu, itilinda nkhondo;
  • Hymn 792 Dzuwa la Mulungu
  • Hymn 258 Kazembe wanga m’matenda,
  • Hymn 1684 Mbuye mabala anu olimba
  • Hymn 658 Ndichitireni, Mbuye ‘ne,
  • Hymn 896 Mbuye, ndinalema ine,
  • Hymn 1219 Bwenzi ndinamkomanayo
  • Hymn 322 PAKUYITANIDWA munthu pa dziko ino,
  • Hymn 361 AMBUYE munapatsa tsiku
  • Hymn 605 Chifukwa cha zokoma mtima zonse za ulerezo,
  • Hymn 289 Ndi manja athu awa nawo nganu,
  • Hymn 1531 Kudzirala ndi kufatsa,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version