Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,

  1. Home   »  
  2. Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,

Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,

 

Yesu, dzina lakukonda,
Lopambana onse ena,
Tonse tidzaligwadira
Ndi mitima yochepetsa.

Yesu, dzina lokondwetsa
Akuipa a padziko,
Kale linatidziŵitsa
Mpulumutsi ndiye Yesu.

Yesu dzina lakufatsa,
Anamutcha ’kali Mwana,
M’mene analoŵa kale
M’dziko lino lakudana.

Yesu, dzina ndi lomweli
La pa dziko lino lonse,
Ndi lamphamvu yolanditsa
Anthu mu masoka onse.

Yesu, dzina lakukonda
La Mwanayo wa Mulungu,
Ife anthu osauka
Tithaŵira nalo kwanu.

Post navigation

Previous: Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye
Next: Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 3 TIMYAMIKIRE Mlunguyo,
  • Hymn 172 Imfa yalephera
  • Hymn 1164 Tikakhulupira
  • Hymn 374 Pakuti Mfumuyo
  • Hymn 29 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 1534 Mukonze mtima wangawu,
  • Hymn 853 Pa tsikuli, Mbuyanga ‘Nu,
  • Hymn 1327 Bwezatu, bwezatu,
  • Hymn 232 Uchita kwombola,
  • Hymn 1292 Wolapa mtima simunyozadi,
  • Hymn 1308 Ndi ine, m’mtima Mwanu mbee!
  • Hymn 663 Anyamata a Mulungu,
  • Hymn 583 Anabadwa,
  • Hymn 664 Komwe asauka anthu
  • Hymn 430 Tero tidzakwera
  • Hymn 387 MUDZE, anthuni, talaŵani ’nu
  • Hymn 342 BWENZI lathu ndiye Yesu,
  • Hymn 1363 Tamani Ambuye,
  • Hymn 435 ANAKWATIRA kale
  • Hymn 741 Chakudya ichi chidzapita du,
  • Hymn 306 YAMBA ulendo mnzanga,
  • Hymn 587 Mutitsuke,
  • Hymn 314 TIYENI nonsenu okonda YESUYO,
  • Hymn 665 Pomangidwa anthu nayo
  • Hymn 1259 Ndikhulupirira bwino
  • Hymn 171 IWE tiye, iwe tiye,
  • Hymn 1605 Yesu, dzina lokondwetsa
  • Hymn 1122 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 145 MBIRI yakale lomwe
  • Hymn 502 Ndikonda mbiri yomwe
  • Hymn 1233 Tsopano ndibukitsabe chikondi chanu chija
  • Hymn 99 Tsopano ndimwona Iye
  • Hymn 524 Wokoma Mbuyathu
  • Hymn 126 Mwa ine, moyo wanga ndi Yesu
  • Hymn 20 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 685 Tamva mawu amwewo
  • Hymn 1203 Zambiri zangazo
  • Hymn 369 Lowani m’nyumba mwakemu
  • Hymn 1659 Ndiye mtsamiro
  • Hymn 197 Tidzatama Atate wathu
  • Hymn 26 “Ndakukonda ku imfa
  • Hymn 1393 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 216 Ndi misozi ndi chisoni
  • Hymn 744 Kristu ndi mwini moyo wathuwu,
  • Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,
  • Hymn 214 Msanga adzachitseka chitseko,
  • Hymn 894 Mbuye, ndinu Mfumu yanga
  • Hymn 1594 Chikondano chakechi
  • Hymn 202 NDIKHULUPIRIRA, Yesu,
  • Hymn 482 Ndinu wakuyera,
  • Hymn 159 Kamwana Yesu ‘nabadwa,
  • Hymn 244 Ndidze pafupi pa
  • Hymn 441 Tamverani, aitana:
  • Hymn 1822 Lawani chikondano chake;
  • Hymn 971 Ndinu Mbusa wanga;
  • Hymn 1721 Mapazi ake namvatu
  • Hymn 1757 Udzadziwitsa anthu
  • Hymn 898 Mndidziwitse ntchito yanga,
  • Hymn 1636 Potuluka m’manda mwawo
  • Hymn 1711 Kwa munthu wasokerayo

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version