Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye

  1. Home   »  
  2. Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye

Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye

 

KUDZA kwa Mbuye
kudzatero monga mphenzi,
Ing’anima M’mwamba choncho Iye,
Dziko lidzanjenjemera oyipa onse,
Nayamba kuthawa powona Iye.

Yesu akhala pampando,
Kuweruza makamuwo;
Nkhosa dzanja lamanjalo,
Mbuzi kudzanja lamanzelero.

Ayimba kumpando’ko wolemekezeka,
Mfumu ya Kumwamba
Mbuye Yesu,
Alira m’Gehenamo moto, moto, moto,
Ndipeze kuti madzi akumwa.

Udzachitanji mbale pobwera Ambuye,
Kudzaweruza dziko lapansi,
Ngati sudakonzeke khulupira Yesu,
Kuti upeze moyo wosatha.

Post navigation

Previous: Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
Next: Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1036 Mtima wakufatsa
  • Hymn 1686 Ndi mtima wonse mwimbedi
  • Hymn 174 YESU wathu Mbuyeyo
  • Hymn 1762 Anamva abusa omwe
  • Hymn 1239 Ndipo pakuima phe!
  • Hymn 1355 Atate, Mwana, Mzimunso,
  • Hymn 486 Yesu, Yesu,
  • Hymn 1701 Nditani Bwenzi langa
  • Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,
  • Hymn 243 Mtima wanga udzakondwera,
  • Hymn 1186 Yesu anafa pamtandapo,
  • Hymn 544 Zoopsya sitidziwapo
  • Hymn 444 YEMWE afesa nalira,
  • Hymn 1327 Bwezatu, bwezatu,
  • Hymn 505 Ndikondwa kuti Atate wam’Mwamba
  • Hymn 859 Pakufika tsidya lija,
  • Hymn 486 MPULUMUTSI Yesu,
  • Hymn 365 Monga m’Mwamba mupambana
  • Hymn 148 Ndisauka, ndimasowa
  • Hymn 1743 M’kati mwa zobvuta zathu
  • Hymn 768 Ndi ife tinga mbewuzo
  • Hymn 397 MBUYE wathu, mutipatsa
  • Hymn 367 MPULUMUTSI, tikagona
  • Hymn 348 Aitana,
  • Hymn 141 TAONANI pamtandapo,
  • Hymn 1148 Ndiimba mumtima mokondwa
  • Hymn 1662 Msandipitire, Yesu,
  • Hymn 124 PAMTANDAPO, pamtanda,
  • Hymn 849 Tadzuka mzimu wanga’we
  • Hymn 387 Tikutha kupemphera,
  • Hymn 842 Tipempha kuti Mpingo wanu
  • Hymn 1850 Anthu a mitundu yonse,
  • Hymn 502 Ndikonda mbiri yomwe
  • Hymn 1034 Mkristu, ulimbike
  • Hymn 168 Yendani mwaulemerero,
  • Hymn 440 ZIKOMO Ambuye wathu,
  • Hymn 493 Ndimalira kwa Inutu,
  • Hymn 420 Mtima umabisala
  • Hymn 800 Yesu munadzukanso
  • Hymn 919 ‘Tate, mwa kusunga kwanu
  • Hymn 498 Yesu akonda,
  • Hymn 121 Imbira!
  • Hymn 1602 M’mawu a Yesu Mbuyeyo,
  • Hymn 931 Tikagwidwa ndi chisoni,
  • Hymn 1062 Mkatero ndidzayenda m’njira
  • Hymn 538 Iye anachoka kwawo,
  • Hymn 529 Zili nazotu nkhwimba zirombozo,
  • Hymn 1535 Lichepa dontho lokhali,
  • Hymn 908 Ndikonda kuganizirabe
  • Hymn 743 Mudze, anthuni, talawani ‘nu
  • Hymn 1191 Ambuyanga Yesu
  • Hymn 1661 Ndimachitira
  • Hymn 621 Wolenga ndi Yemweyo
  • Hymn 968 Mzimu wakuipa
  • Hymn 66 Chisomocho chachotsadi
  • Hymn 1690 Titama Yesuyo,
  • Hymn 28 Mbuye ndisaukadi,
  • Hymn 647 Tiyamike Mlungu ‘Tate,
  • Hymn 645 Kristu ndiye mwala wathu,
  • Hymn 1409 Kodi mufunatu Yesu?

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version