Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,

  1. Home   »  
  2. Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,

Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,

 

TIYAMIKE Ambuye,
Chifukwa chotilola,
Kulowa m’chaka chino m’tisunge;
Sitingathe ‘fe tokha,
Kuyenda m’chaka chonse;
Ambuye m’titsogoze,
M’tisunge.

M’tisunge, m’tisunge,
Yesu tikupemphani m’tisunge;
Ife timalephera kuyenda m’njira tokha;
Yesu tikupemphani m’tisunge.

Dziko lapansi pano timangoyenda chabe,
Wosaganiziranso za moyo;
Timaganiza kuti moyowu sudzathanso,
Ambuye m’tikumbutse leroli.

Moyowu ngwapafupi, monga kugwa kwa tsamba,
Monga kumanga mtolo m’tisunge;
Ambuye m’tidalitse,
Nthawi isanafike;
Kuti tingataike m’tisunge.

Post navigation

Previous: Hymn 420 FESANI mbewuzo,
Next: Hymn 441 MBUYE, tikuthokozani,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 739 Ndilibe wondithangata ‘ne ‘yi,
  • Hymn 1423 Oipa inu nonsetu,
  • Hymn 114 Ndine Mbusayo wabwino,
  • Hymn 1476 Mipingo iyo idzatu,
  • Hymn 1102 Dziko lonse ndilitaya;
  • Hymn 1027 Tithawiranji ifetu?
  • Hymn 1549 Mtitsutse titachimwa
  • Hymn 423 Koma azibvala
  • Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,
  • Hymn 821 Aleluya!
  • Hymn 58 Titasokera tinabwerera,
  • Hymn 1704 Zintchito zakezi
  • Hymn 988 Ndikhumba Mzimu wanu
  • Hymn 1782 Poyamba paja analenga
  • Hymn 30 YEHOVA, Mbusa wangadi,
  • Hymn 1371 Mitengo yaitalitali ‘nu
  • Hymn 432 Ulendo ungoyamba
  • Hymn 1550 Kutiyeretsa m’mtima
  • Hymn 277 Mbwere nonse muone
  • Hymn 1042 Zonse umazinyadira
  • Hymn 858 Anthu osawerengeka
  • Hymn 349 MOSE anamenya thanthwe kawiri,
  • Hymn 1132 Mlungu adzandilandila,
  • Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,
  • Hymn 323 Tiwaliretu, tiwaliretu
  • Hymn 132 MVERA mtima wanga ’we
  • Hymn 608 Maluwa abwino aphuka m’mapiri ndi m’madambomo,
  • Hymn 402 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 337 ‘Tate ‘Nu,
  • Hymn 1756 Mwana, adzakuyesa
  • Hymn 134 INU ansembe ngakhale mufunsa,
  • Hymn 1492 Sakukanani Yesudi,
  • Hymn 1652 Mabala ajawo
  • Hymn 1080 Ambuye mundisunge
  • Hymn 825 Mpatse ana ‘ng’ono
  • Hymn 10 TSOPANO linoli,
  • Hymn 412 Kudzachera tsiku lijalo
  • Hymn 1438 Yesu akukonda,
  • Hymn 781 Tatsegukani inutu,
  • Hymn 1275 Mtima ‘we siya ndi Yesu nsonizi,
  • Hymn 973 Tigwire nkhondo yomwe
  • Hymn 215 Choka, choka,
  • Hymn 178 Machimo anga ngambiri
  • Hymn 386 MONGATU mawu anuwo,
  • Hymn 956 Mbuye munditsogolere,
  • Hymn 882 Kodi tikulema nazo
  • Hymn 1667 Yesu wakukoma mtima,
  • Hymn 688 Anthu akum’mawa
  • Hymn 1576 Khamulo liliko
  • Hymn 1262 Lero mtima ungolema, Usaukadi;
  • Hymn 1605 Yesu, dzina lokondwetsa
  • Hymn 1354 Mzimu Woyera, m’mtimamo
  • Hymn 378 KWEZANI mitu yanuyo,
  • Hymn 73 M’SANDIPITILIRE Yesu,
  • Hymn 165 Yendanitu m’ulemudi,
  • Hymn 577 Adagona m’ndyeromo
  • Hymn 743 Mudze, anthuni, talawani ‘nu
  • Hymn 168 NDINGANENE malilime,
  • Hymn 971 Ndinu Mbusa wanga;
  • Hymn 1515 Ndikachimwa, Bukuli

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version