Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 417 M’BWERE Mlungu Mbuye wathu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 417 M’BWERE Mlungu Mbuye wathu,

Hymn 417 M’BWERE Mlungu Mbuye wathu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 417 M’BWERE Mlungu Mbuye wathu,

 

M’BWERE Mlungu Mbuye wathu,
Msunge zakuonazo,
Mudalitse anthu onse
Ndi chifumu chanucho.

MMbwere Yesu Mwini moyo,
Ukuletu ’lemuwo;
Gonjetsani anthu onse,
Mpatsenso mtenderewo.

Mbwere Mzimu Wakuyera,
Mutitsitsimutseko;
Muthaŵitse mdima wonse,
Muŵalitse m’mtimamo.

Anthu onse taukani,
Imbirani Mlunguyo;
Zichuluke zomtamanda
Pansi ndi Kumwambako.

Post navigation

Previous: Hymn 400 ONA Mwana wa Nkhosa,
Next: Hymn 421 ANTHU ali m’mdima akuyitanitsa,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1584 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 606 Dzinja lokondweretsa lafikanso,litapumatu,
  • Hymn 375 Zipatso zakezi
  • Hymn 723 Mundimvere, Mbuye wanga
  • Hymn 421 ANTHU ali m’mdima akuyitanitsa,
  • Hymn 496 Yesu Mbuye ‘Nu wabwino,
  • Hymn 331 Yesu ndimafuna Inu,
  • Hymn 1301 Moyo ukatha zi,
  • Hymn 714 Dzuwa ndi mvula yonseyo
  • Hymn 1235 Yesu wathadi
  • Hymn 1022 Mbuye, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 87 Aleluya, mwandigula,
  • Hymn 206 YESU, mulikundipempha
  • Hymn 385 Tsopano, poyamba paja,
  • Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,
  • Hymn 666 Walitsani nyali yanu
  • Hymn 303 Ona pamtanda Yesuyo
  • Hymn 418 M’manja Yesu wanga
  • Hymn 391 MUNDIMVERE, Mbuye wanga
  • Hymn 320 Ambuye, wakuti ndi mwaziwo
  • Hymn 1201 Kumwamba kwanuko
  • Hymn 1759 Powalitsira omwe
  • Hymn 1335 Wandifera Yesuyo
  • Hymn 184 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 1712 E! Yesu Mbuye wangadi,
  • Hymn 929 Chikondano sichifera;
  • Hymn 388 Ambuye, Mzimu wanu
  • Hymn 1243 Kodi mayi wobereka
  • Hymn 1338 Munachita nthantha kale,
  • Hymn 1469 M’kufatsa kwake komwe
  • Hymn 917 Ndi nkhondo ikaleka
  • Hymn 1297 Kumwamba komwe n’dzaimbira
  • Hymn 119 Tamverani anthu inu,
  • Hymn 172 Imfa yalephera
  • Hymn 641 Awiri aimamu,
  • Hymn 505 Ndikondwa kuti Atate wam’Mwamba
  • Hymn 124 Aliponso adani am’kati ndi akunja;
  • Hymn 468 Ife tikondana nanu,
  • Hymn 1473 Anasenza pa bwanji uchimo wonsewo,
  • Hymn 376 Adzadalitsa ‘fe
  • Hymn 199 NDINASOKERA kutali,
  • Hymn 1340 Perekani mtima wanu
  • Hymn 1077 Khalatu woyera,
  • Hymn 280 Tisonkhane tonsefe,
  • Hymn 924 Kodi uli ndi chisoni
  • Hymn 1676 Kondwerani dzuwa lino Aleluya,
  • Hymn 192 ZAKEYU mkulu wa misonkho,
  • Hymn 1572 Mumbveke, mbveke, mbveke,
  • Hymn 301 MBUYE, ndapangana
  • Hymn 1185 Imfa ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 650 Tikondwa tonse ndi kukuthokazani Nu
  • Hymn 1431 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 1366 Sititha ifedi
  • Hymn 1439 Iwetu afuna,
  • Hymn 384 USIKU uja kalero,
  • Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,
  • Hymn 946 Ngakhale enawo aleke kwimbako,
  • Hymn 382 M’wabatize anzathuwa,
  • Hymn 331 NDILI ndi kwathu ine,
  • Hymn 1545 Mundilimbitse m’mtima

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version