Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 416 PALIBE wina Kumwamba,

  1. Home   »  
  2. Hymn 416 PALIBE wina Kumwamba,

Hymn 416 PALIBE wina Kumwamba,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 416 PALIBE wina Kumwamba,

 

PALIBE wina Kumwamba,
Ndinutu Mbuyanga;
Pakati pa mayesero,
Thandizeni Ambuye.

Zonse zam’dziko zidzatha,
Monga Mawu anenera;
Ufumu wanu sudzatha,
Wamuyaya, Wamuyaya.

Palibe wina m’dzikoli,
Ndinutu Mbuyanga;
Pakati pamayesero,
Thandizeni Ambuye.

Nyimbo zonse tidzayimba,
Zanutu Mbuyanga;
Pakati pamayesero,
Thandizeni Ambuye.

Post navigation

Previous: Hymn 400 ONA Mwana wa Nkhosa,
Next: Hymn 421 ANTHU ali m’mdima akuyitanitsa,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 188 Ine ndili ndi manyazi
  • Hymn 80 Utsegule mtimawo,
  • Hymn 307 ABALE anga ine ndikupita,
  • Hymn 189 MLENDO ali pakhomo,
  • Hymn 877 Zokoma ndithu nthawizi
  • Hymn 942 Kaamba chisomo cha Mbuyathu
  • Hymn 340 PEMPHERA m’mbanda kucha,
  • Hymn 291 Ndi milomo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 660 Tumizani kuunikako,
  • Hymn 809 Madzulo aja kalelo
  • Hymn 755 Pamene padzakhalapo
  • Hymn 86 IYE wokhulupilira Yesu,
  • Hymn 350 MBUYE ndayima pano,
  • Hymn 1780 Titame Mlungu Wakumwamba,
  • Hymn 32 YENDANI, Mfumu yamtendere
  • Hymn 555 Mkucha wake ndaniyo
  • Hymn 122 KUNALI munthu wa Mlungu,
  • Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 974 Tsopano timenyana
  • Hymn 991 Ndi zapansi pano
  • Hymn 1774 Poti akumbukira
  • Hymn 31 Tamandani mbuye,
  • Hymn 1416 Mbuye wanga ndilikumva,
  • Hymn 911 Mokhala mokhamokha
  • Hymn 345 ATATE, ndipempha
  • Hymn 1729 Munthu Wazisoniyo
  • Hymn 343 Auke,
  • Hymn 833 Mundilimbitse ndikayese manda ngati mphasayi,
  • Hymn 252 M’dziko lino chimwemwecho
  • Hymn 436 YEHOVA Mlungu wathu,
  • Hymn 860 Nthawi yina adzadzuka
  • Hymn 676 Adze amitundu yonse,
  • Hymn 1661 Ndimachitira
  • Hymn 52 POTULUKA m’mudzimo
  • Hymn 416 PALIBE wina Kumwamba,
  • Hymn 1084 “Khala mwa Ine,” munachotsa tsoka,
  • Hymn 144 AMENE adzavomereza ndithu,
  • Hymn 1354 Mzimu Woyera, m’mtimamo
  • Hymn 200 Ndi tsopano tilindira
  • Hymn 1041 Zosauka unvomere,
  • Hymn 241 MTENDERE uli m’mtima mwathumu,
  • Hymn 304 POZUNZIDWA inu ponseponse
  • Hymn 1762 Anamva abusa omwe
  • Hymn 261 Munafera pa mtanda
  • Hymn 765 Chikondi chili m’chikhomu
  • Hymn 897 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 1426 Wina panalibe
  • Hymn 332 Perekani mtima wanu,
  • Hymn 341 Ayenda,
  • Hymn 1432 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 247 MULUNGU anditsogolera,
  • Hymn 408 Oipa tili tonsefe;
  • Hymn 1831 M’mitsinje yamtendere mtima wanga aumwetsa;
  • Hymn 519 Mverani, aimba anawo,
  • Hymn 371 AMBUYE, tasonkhana
  • Hymn 1 NDINU wakuyera! Wamphamvu zonse.
  • Hymn 1021 Kunsi kudambo, pena m’mwamba m’phirimo,
  • Hymn 195 Bwinoli tipita,
  • Hymn 288 Ndi maso athu awa nawo nganu,
  • Hymn 842 Tipempha kuti Mpingo wanu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version