Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 401 A MULUNGU,

  1. Home   »  
  2. Hymn 401 A MULUNGU,

Hymn 401 A MULUNGU,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 401 A MULUNGU,

 

A MULUNGU,
Munatuma Yesuyo,
Mwana wanu Yekhayo.

Anabadwa,
Anabadwa motere,
Monga mmphaŵi m’kholamo.

Anakonda
Anakonda anthuwo,
Naŵapulumutsanso.

Anafera,
Anafera m’mtandamo,
Anafera ifenso.

Anadzuka
Anadzuka m’mandamo,
Anatenga moyowo.

Anakwera,
Anakwera m’Mwambamo
Kwa Mulungu ’Tatewo.

Adzabwera,
Adzabwera Iyeyo
Tsiku lomalizalo.

Aleluya,
Aleluya Yesuyo,
Tizitama dzinalo.

Post navigation

Previous: Hymn 400 ONA Mwana wa Nkhosa,
Next: Hymn 421 ANTHU ali m’mdima akuyitanitsa,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 451 Yesu ndi Mbuyako,
  • Hymn 1140 Paja athira Yesutu
  • Hymn 913 Kulibe gombe, nyanja,
  • Hymn 769 Ndi kutsukidwa m’mwazimo
  • Hymn 354 Tinafunafunatu,
  • Hymn 127 Mwazi wake ndi chitsime changa,
  • Hymn 897 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 1679 Tiyamike Dzina lake, Aleluya,
  • Hymn 1311 Pothawira pena ‘yi,
  • Hymn 1739 Ife timakufunani
  • Hymn 574 A! Yesu Mbuye wakuyera,
  • Hymn 1334 Walandira inetu
  • Hymn 1132 Mlungu adzandilandila,
  • Hymn 619 Tilimalima m’minda,
  • Hymn 1039 Usafune chuma chokha,
  • Hymn 1080 Ambuye mundisunge
  • Hymn 1594 Chikondano chakechi
  • Hymn 1657 Mbuye, mutsaganebe
  • Hymn 1318 Ndibwera kwa Ambuyeyo,
  • Hymn 1857 Ndinagona mwa zoipa,
  • Hymn 1419 Amayi ‘nu, amayi ‘nu,
  • Hymn 1004 A! mizimu yakuipa
  • Hymn 1385 Anatsogolera kale
  • Hymn 127 POLUMIDWA ndi njokazo,
  • Hymn 1842 Pabande lolunjika andilondolera njira;
  • Hymn 31 MULUNGU Wamkulu,
  • Hymn 62 AMBUYE Yesu,
  • Hymn 1156 Imfa ndi manda sitiopa ‘yi,
  • Hymn 1178 Mawu omwewo, nyimbo yomweyi,
  • Hymn 1426 Wina panalibe
  • Hymn 409 Yesu adza kuwerenga
  • Hymn 53 AMBUYE Yesu anamva chisoni,
  • Hymn 5 Inu Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 1222 Bwenzi ndimamkomanayo
  • Hymn 1137 Masiku ena pali mdima,
  • Hymn 373 Ayamikire ‘Nu
  • Hymn 837 Koma kalelo mnakhalitsa pano,
  • Hymn 342 Ambiri,
  • Hymn 279 Mbwere mudzamve nonse
  • Hymn 1768 Ndiye wamphamvu zonse
  • Hymn 91 NDITAME Mlungu m’mtimamo,
  • Hymn 330 N’LOKOMA Dziko langa!
  • Hymn 378 Ku madzi ake odikha
  • Hymn 597 Mlungu ali nane
  • Hymn 42 Masiku tikatsala ife
  • Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,
  • Hymn 1151 Pomulambira Yesu Mbuyanga,
  • Hymn 1719 Ku Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 1405 Ati: “Undiuze
  • Hymn 150 Ndisauka, sindiona;
  • Hymn 1239 Ndipo pakuima phe!
  • Hymn 434 CHIKONDI cha Mulunguyo,
  • Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu
  • Hymn 1633 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 83 MBUYEYO adzabwera,
  • Hymn 368 MULUNGU wanga, Dzuŵatu
  • Hymn 15 Mbuye, chifundo chanu chitigwere
  • Hymn 687 Bukitsani mawunso
  • Hymn 818 Mkhululukire,
  • Hymn 1288 Yesu mundimve, ndikuliratu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version