Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 397 MBUYE wathu, mutipatsa

  1. Home   »  
  2. Hymn 397 MBUYE wathu, mutipatsa

Hymn 397 MBUYE wathu, mutipatsa

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 397 MBUYE wathu, mutipatsa

 

MBUYE wathu, mutipatsa
Zonse tili nazozo,
Mutikomeratu mtima
Osaleka konseko,
Mutikonda, mutisunga,
Mutisamalira ’fe.

Dzuŵa, madzi, kudya, mpweya,
Moyo, zonse nzanuzi,
Si za ife, nzaulere,
Tingozilandiradi;
Zifumira kwa Aate
Wotikondakondatu.

Monga tilandira, Mbuye,
Mtiphunzitse tonsefe
Tipere chuma chathu
Ndi kusangalalatu;
Zakukhala m’manja mwathu
Tiziyese nzanudi.

Tikhaletu nawo, Mbuye,
Mtima wosauma ’yi
Ndi wofatsa ndi wabwino
Ndi woyerayeradi,
Kuti tiyenere Dzina
La Mbuyathu Yesuyo.

Tisaiwalire ’bale
Athu osadziŵa ’Nu,
Akulira ndi odwala
Tiŵapemphereratu;
Titsanzenso Mbuye Yesu
Ndi k’ŵathangatira ’wo.

Dalitseni, Mbuye, zonse
Zomwe taperekazi,
Mzilandire, nsembe yathu,
Mziyeretse Inudi
Ndi mitima yathu yonse
Tikuyamikirani.

Post navigation

Previous: Hymn 380 ATATE, muwapenya
Next: Hymn 401 A MULUNGU,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 430 Tero tidzakwera
  • Hymn 698 Polenga dzikoli,
  • Hymn 1290 Ndilibe malo mokhaliramo,
  • Hymn 750 Yesu Mbuyathu, Inu nomwe ‘Nu,
  • Hymn 1351 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 1685 Nla Mlungu dzuwali;
  • Hymn 736 Mndidyetse m’chipululu
  • Hymn 798 M’nyumba yanu, Mlungu, ‘yi
  • Hymn 485 POMPANO pandikonda
  • Hymn 1169 Mwazi wa Yesu
  • Hymn 211 Chakudya ichi ndi cha iwenso,
  • Hymn 386 MONGATU mawu anuwo,
  • Hymn 201 Ngati zakuipa zathu
  • Hymn 1052 Ndilira mtima wotamanda
  • Hymn 409 Yesu adza kuwerenga
  • Hymn 979 Limbikani inu nonse,
  • Hymn 831 Mundikumbutse, ndikapanda tulo, za Kumwambako;
  • Hymn 1809 Yampatsa Nowa yemwe,
  • Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,
  • Hymn 317 UKATHA moyo wanga
  • Hymn 1151 Pomulambira Yesu Mbuyanga,
  • Hymn 30 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 1144 Khalani duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 1089 Ndionetsere kuunika
  • Hymn 1741 Yesu munalaswa m’mtima,
  • Hymn 206 YESU, mulikundipempha
  • Hymn 1296 Chionerere mwaziwo
  • Hymn 1639 Aleluya, aleluya,
  • Hymn 496 Yesu Mbuye ‘Nu wabwino,
  • Hymn 1185 Imfa ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 892 Tilibe madalitso
  • Hymn 1836 Ndi wamwayi munthu uja
  • Hymn 761 Natamndira Mlunguyo
  • Hymn 294 Yesu anali khanda
  • Hymn 1161 Wapumitsa mtima wanga,
  • Hymn 18 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 325 Walira Yesu wolimbitsayo,
  • Hymn 69 KONDWERANI dzuŵa lino,
  • Hymn 703 Dzuwa, madzi, kudya, mpweya,
  • Hymn 546 Kulibe wokwanira ‘yi
  • Hymn 42 “SENZANI mtanda wanuwu,
  • Hymn 1396 Ndi maso Ambuyathu
  • Hymn 111 Nkhope yake ‘kabisika,
  • Hymn 739 Ndilibe wondithangata ‘ne ‘yi,
  • Hymn 1339 Musaope pokumbuka
  • Hymn 1320 Ndayang’anira Mbuyeyo,
  • Hymn 1562 Mzimu Woyera, mudze mumitima mwathumo,
  • Hymn 276 MKRISTU, ulimbike
  • Hymn 320 Ambuye, wakuti ndi mwaziwo
  • Hymn 502 Ndikonda mbiri yomwe
  • Hymn 139 Bwerani inu nonse, inu nonse,
  • Hymn 382 Mwadzoza mutu wanga ndi
  • Hymn 381 MONGA zomera zonsezo
  • Hymn 319 NDIDZATANI ine,
  • Hymn 660 Tumizani kuunikako,
  • Hymn 1447 Yesu ngwachifundodi,
  • Hymn 731 Mundionetse, Yesu,
  • Hymn 1611 Nadzuka m’mandamo
  • Hymn 599 Mlengi wathu Wakuyera,
  • Hymn 231 Mwazi wa Yesu wokondwa

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version