Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,

  1. Home   »  
  2. Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,

Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,

 

KWACHA lero kwati mbee,
Tsiku la Mulunguli;
Dzuŵa liŵaliradi
Thambo ndi zapansipa
Upumira mpweyawu
Wa Mulungu konseku.

M’nyumba yanu, Mlungu, ’yi
Tisonkhana teretu,
Ndi mitundu yonseyi
Tikulambireni ’Nu:
Yesu Mbuye wathuyo
Ndiye Mfumu ponsepo.

Inu Mlungu kalelo
Mutalenga zonsezi
Munapuma tsikulo;
Tipumadi ifenso.
Mommo tilandiratu
Zopumitsa mtimawu.

Yesu munadzukanso
M’manda lero lomwetu;
Ntchito munayambayo
Yakudzutsa anthu ’fe,
Kuti ndi mitimayi
Tigwirebe ntchitozi.

Post navigation

Previous: Hymn 360 KRISTU wakuyeratu,
Next: Hymn 381 MONGA zomera zonsezo

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1306 Ndi ine ndasaukadi,
  • Hymn 1458 Satana ndi unyolo
  • Hymn 1451 Okoma ndiwo mawu
  • Hymn 1819 Pokondwa ndi poona bvuto
  • Hymn 228 Ataya zoipa,
  • Hymn 1013 Tizifesa m’dzuwa,
  • Hymn 1413 Ndichitenji kukapeza
  • Hymn 249 MBUYANGA Yesu, mundigwire
  • Hymn 701 Inu Atatuwo,
  • Hymn 1594 Chikondano chakechi
  • Hymn 1517 Lindionetsera ‘ne,
  • Hymn 572 Anadza nazo mphatso zake
  • Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 220 MULUNGU mundichitire chifundo,
  • Hymn 132 Ganizansoni, ali pano,
  • Hymn 1738 “Senzani mtanda wanuwo.”
  • Hymn 619 Tilimalima m’minda,
  • Hymn 84 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,
  • Hymn 269 Atate ‘nu, amayi ‘nu, nonsenu,
  • Hymn 229 Woba wakufa ‘napenya
  • Hymn 29 CHIKONDI cha
  • Hymn 1684 Mbuye mabala anu olimba
  • Hymn 255 KHALA chete mtima wanga
  • Hymn 355 DZIKO lonse mlambire
  • Hymn 1175 Sindinanyengedwa konse,
  • Hymn 1813 Pochimwa anthu onsewo
  • Hymn 48 IMFA ya Mwana wa Mulungu,
  • Hymn 385 SINDILI woyenera ’ne,
  • Hymn 1354 Mzimu Woyera, m’mtimamo
  • Hymn 1080 Ambuye mundisunge
  • Hymn 399 Tchimo lathu lonse, Yesu,
  • Hymn 1185 Imfa ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 780 Kwezani mitu yanuyo,
  • Hymn 495 Wonga Inu ndikhaledi,
  • Hymn 1151 Pomulambira Yesu Mbuyanga,
  • Hymn 1215 Ndimkonde Kristuyo,
  • Hymn 426 MBUYE, Mpingo wanu usauka kwakukuludi;
  • Hymn 686 Imbadi za Iyeyo,
  • Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,
  • Hymn 892 Tilibe madalitso
  • Hymn 1157 Mtendere wapambana m’Mwambamo
  • Hymn 1188 Akumangidwa ndi mzimuwo,
  • Hymn 478 Ndife ana, mutikonda,
  • Hymn 1367 Wamphamvu yosatha,
  • Hymn 1522 Tikaona bvuto,
  • Hymn 392 ANU Mbuye ndifetu!
  • Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo
  • Hymn 1140 Paja athira Yesutu
  • Hymn 1084 “Khala mwa Ine,” munachotsa tsoka,
  • Hymn 136 Atumwi atummika, atumika,
  • Hymn 1741 Yesu munalaswa m’mtima,
  • Hymn 156 OKOMA ndiwo mawu
  • Hymn 1712 E! Yesu Mbuye wangadi,
  • Hymn 263 AMBUYE mundisunge
  • Hymn 1159 Mwalembedwa mukalata
  • Hymn 427 AULENDO amayenda
  • Hymn 1812 Kuzani Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 1705 Pa Iye padzapo
  • Hymn 1580 Akadakhalabe

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version