Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,

  1. Home   »  
  2. Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,

Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,

 

KWACHA lero kwati mbee,
Tsiku la Mulunguli;
Dzuŵa liŵaliradi
Thambo ndi zapansipa
Upumira mpweyawu
Wa Mulungu konseku.

M’nyumba yanu, Mlungu, ’yi
Tisonkhana teretu,
Ndi mitundu yonseyi
Tikulambireni ’Nu:
Yesu Mbuye wathuyo
Ndiye Mfumu ponsepo.

Inu Mlungu kalelo
Mutalenga zonsezi
Munapuma tsikulo;
Tipumadi ifenso.
Mommo tilandiratu
Zopumitsa mtimawu.

Yesu munadzukanso
M’manda lero lomwetu;
Ntchito munayambayo
Yakudzutsa anthu ’fe,
Kuti ndi mitimayi
Tigwirebe ntchitozi.

Post navigation

Previous: Hymn 369 LERO mwatipatsa moyo,
Next: Hymn 371 AMBUYE, tasonkhana

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 493 Ndimalira kwa Inutu,
  • Hymn 1657 Mbuye, mutsaganebe
  • Hymn 1685 Nla Mlungu dzuwali;
  • Hymn 1642 M’khola mwa ng’ombe ku Betelehemu
  • Hymn 717 Ambuye zathu zonsezi
  • Hymn 157 Mbuye, Mzimu Woyera
  • Hymn 14 Tsiku ndi tsiku timalemekeza;
  • Hymn 1139 Namondwe akawombabe,
  • Hymn 450 Koma usalole
  • Hymn 416 Woyenera ndani kunka
  • Hymn 770 Atate, muwapenye
  • Hymn 134 INU ansembe ngakhale mufunsa,
  • Hymn 59 IMVANI uthenga,
  • Hymn 527 Idzani mumtima mwanga,
  • Hymn 758 Sindili woyenera ‘ne;
  • Hymn 117 CHOLIMBITSA mtima ndi chonditsogolera;
  • Hymn 736 Mndidyetse m’chipululu
  • Hymn 1384 Mphamvu yake inalenga
  • Hymn 457 KALE m’mzinda wachifumu
  • Hymn 442 Posachedwa tilekana
  • Hymn 871 Tiphatikane tonsefe okonda Yesu Kristu;
  • Hymn 832 Zochimwa za usana uno mndikhululukire ‘ne;
  • Hymn 582 A! Mulungu,
  • Hymn 381 Chakudya changa chabwino
  • Hymn 204 Kumandako, kumanda
  • Hymn 323 Tiwaliretu, tiwaliretu
  • Hymn 1563 Mufike monga nyali younika m’mtimamo,
  • Hymn 1177 Ndidziwitsitsa Yesu ndi wanga,
  • Hymn 1210 Kumwamba ndidzanenadi
  • Hymn 1270 Ndayesa kudzikonzadi,
  • Hymn 477 Mpulumutsi, Mbusa wathu,
  • Hymn 1454 Ambuye, musendeze
  • Hymn 1504 Kodi ali ndi chilemba
  • Hymn 810 Tsopano lino kwada bii,
  • Hymn 227 NDIM’KONDE Kristuyo,
  • Hymn 476 MBUYE, tili ana anu,
  • Hymn 1101 Ngati mtima sumakonda
  • Hymn 1652 Mabala ajawo
  • Hymn 1346 Ndaima pano, ndaima pakhomo:Lowa, lowa, lowa, lowa!
  • Hymn 1377 Ndi amithenga akumwambako,
  • Hymn 1126 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 1628 Dziko lino linaona
  • Hymn 466 OSANATU, osana,
  • Hymn 443 M’MAŴA tizifesa
  • Hymn 524 Wokoma Mbuyathu
  • Hymn 1734 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 58 Titasokera tinabwerera,
  • Hymn 542 Kuli kaphiri m’talimo
  • Hymn 1480 Afika Yesu leroli,
  • Hymn 562 Mwa ubwana wake wonse
  • Hymn 765 Chikondi chili m’chikhomu
  • Hymn 1172 Adzabweranso
  • Hymn 181 Zonse ndinakonda kale
  • Hymn 761 Natamndira Mlunguyo
  • Hymn 1728 Zofuna zanga zonsezo
  • Hymn 369 LERO mwatipatsa moyo,
  • Hymn 1569 Mtima wodetsa mukonzere,
  • Hymn 1171 Mulungu wanga
  • Hymn 32 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 1736 “Senzani mtanda wanuwu.”

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version