Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,

Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,

 

ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,
Mavuto, mayesero adza kwa ine;
Komatu ndidziŵitsitsa kuti Mbuye wanga,
Asunga moyo wanga kosalekeza.

Ndine wanu Mbuye wanga,
Mavuto, mayesero adza kwa ine;
Komatu ndidziwitsitsa
Kuti Mbuye wanga,
Asunga moyo wanga kosalekeza.

Chifukwa cha dzina lake
Ndanyozedwa ‘ne,
Adani achuluka, ndachepa ine;
Ndiwakonda onse
Koma andisautsa ‘ne,
Pukutani m’maso mwanga misoziyi.

Tiyeni abale tonse
Tilimbe ndithu,
Pogwira ntchito zake
Za Mbuye wathu;
Iye analonjezatu
Tsiku lomaliza,
Tidzakhala muulemelero wake.

Post navigation

Previous: Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
Next: Hymn 301 MBUYE, ndapangana

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1516 Pakudera nkhawa ‘ne,
  • Hymn 1444 Wamoyo ndiye Yesudi,
  • Hymn 507 Yesu ndimkonda, akondanso ine,
  • Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,
  • Hymn 578 Falitsani mbiriyi,
  • Hymn 443 M’MAŴA tizifesa
  • Hymn 864 Ndi chikondi mtithandize kuigwira nkhondoyi;
  • Hymn 1206 Ndidzakukondani
  • Hymn 586 Yesu Mfumu,
  • Hymn 911 Mokhala mokhamokha
  • Hymn 244 Ndidze pafupi pa
  • Hymn 750 Yesu Mbuyathu, Inu nomwe ‘Nu,
  • Hymn 478 Ndife ana, mutikonda,
  • Hymn 481 Yesu wa Kumwamba,
  • Hymn 415 PAMAYIKO pali mdima,
  • Hymn 761 Natamndira Mlunguyo
  • Hymn 44 Mlungu dalitsani Malawi,
  • Hymn 977 Musagonje, anthu inu,
  • Hymn 734 Ndi mkate wanu, Yesu
  • Hymn 133 NSEMBE yake ya Kaini,
  • Hymn 1436 Inde, lero lino Yesu
  • Hymn 24 “Ndakupeza womanga,
  • Hymn 411 TAMVA mawu omwewo,
  • Hymn 91 Ufuna kuyera kopambana?
  • Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 1696 Mndiletse, ndisateme ‘yi
  • Hymn 157 Mbuye, Mzimu Woyera
  • Hymn 384 Mulungu akhale nawo
  • Hymn 1585 Dzina ili ndi lokoma
  • Hymn 610 Nafenso tidzadzuka kwa ‘ke ngati maluwawo,
  • Hymn 655 Ndiphunzitseni, Mbuyetu,
  • Hymn 1063 Pokhala mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 1421 Alongo ‘nu, alongo ‘nu,
  • Hymn 1111 Pamene ndilemedwa
  • Hymn 342 BWENZI lathu ndiye Yesu,
  • Hymn 76 E, MOYO wanga’we
  • Hymn 155 Pemphero ndiko kufuna
  • Hymn 462 ANANU, ziimbani,
  • Hymn 407 ADZAPAMBANA Yesu ponse
  • Hymn 255 KHALA chete mtima wanga
  • Hymn 1254 Mukhululukire ine,
  • Hymn 192 Apita anzathu dzuwa lino Kosaoneka,
  • Hymn 415 Tidzalandirabe komwe
  • Hymn 1450 Ndi angelo akumwamba
  • Hymn 111 Nkhope yake ‘kabisika,
  • Hymn 355 DZIKO lonse mlambire
  • Hymn 250 MBUYANGA Yesu,
  • Hymn 1073 Mwa ine myatse moto wanu wakuyera mbuu,
  • Hymn 293 Tidziperekadi konse kwa Inu
  • Hymn 67 PAMENEPO pokhala madzulo,
  • Hymn 1708 Pakugomedwapo
  • Hymn 491 N’takafika kwanu
  • Hymn 180 MALO alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 1675 Lambira Mfumuyo
  • Hymn 141 TAONANI pamtandapo,
  • Hymn 727 Imfa ikandifikira,
  • Hymn 99 TIYAMIKE mbuye Yesu
  • Hymn 206 YESU, mulikundipempha
  • Hymn 787 Mzimu Wakuyera
  • Hymn 55 Ambiri tikondwera mwa Yesu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version