Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,

Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,

 

ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,
Mavuto, mayesero adza kwa ine;
Komatu ndidziŵitsitsa kuti Mbuye wanga,
Asunga moyo wanga kosalekeza.

Ndine wanu Mbuye wanga,
Mavuto, mayesero adza kwa ine;
Komatu ndidziwitsitsa
Kuti Mbuye wanga,
Asunga moyo wanga kosalekeza.

Chifukwa cha dzina lake
Ndanyozedwa ‘ne,
Adani achuluka, ndachepa ine;
Ndiwakonda onse
Koma andisautsa ‘ne,
Pukutani m’maso mwanga misoziyi.

Tiyeni abale tonse
Tilimbe ndithu,
Pogwira ntchito zake
Za Mbuye wathu;
Iye analonjezatu
Tsiku lomaliza,
Tidzakhala muulemelero wake.

Post navigation

Previous: Hymn 290 NAMONDWE wawuka,
Next: Hymn 292 NDIPULUMUTSENI Mbuye,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 96 Kodi mudzampembedza Mbuye
  • Hymn 938 A! Yesu Bwenzi langa
  • Hymn 217 CHIPULUMUTSO chathu chayandika,
  • Hymn 1808 Kutuma wabwereza,
  • Hymn 418 M’manja Yesu wanga
  • Hymn 512 ‘Natipulumutsa
  • Hymn 89 INDE, ndifuna kumvatu,
  • Hymn 221 A! CHIKONDI chopambana,
  • Hymn 665 Pomangidwa anthu nayo
  • Hymn 1112 Masiku anga onse
  • Hymn 307 ABALE anga ine ndikupita,
  • Hymn 1107 Anthu onse pansi pano
  • Hymn 537 Aleluya! Aleluya!
  • Hymn 1614 Anabadwa,
  • Hymn 1789 Nditani ine kubwezera Mbuye
  • Hymn 394 TATENGA mphatso zotani?
  • Hymn 277 GWIRA zintchito zako,
  • Hymn 167 Yendanitu, Wansembe wathu,
  • Hymn 42 “SENZANI mtanda wanuwu,
  • Hymn 268 Potuluka m’mudzimo
  • Hymn 161 LERO lino mbale wanga,
  • Hymn 438 Yesu ndiye Mbusa
  • Hymn 47 YESU panjirayo,
  • Hymn 460 E! ang’ono ndifetu,
  • Hymn 298 “Tadodoma, abusa,
  • Hymn 1623 Adzatenga anthu ake
  • Hymn 1414 Zonse zinathedwadi;
  • Hymn 210 Nyumba yodyera ilikudzaza;
  • Hymn 366 Anthu onse a padziko
  • Hymn 431 Pompano pandikonda
  • Hymn 1718 Ona chikondi cha Mulungu,
  • Hymn 770 Atate, muwapenye
  • Hymn 654 Ndilimbikitse, Mbuye, nji!
  • Hymn 104 M’mene ntchito yathatu,
  • Hymn 195 YESU wondikondadi,
  • Hymn 786 Yesu mkhale nafe
  • Hymn 577 Adagona m’ndyeromo
  • Hymn 162 Angelo anu asunga
  • Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,
  • Hymn 416 PALIBE wina Kumwamba,
  • Hymn 1563 Mufike monga nyali younika m’mtimamo,
  • Hymn 482 TCHIMO musalole, musadziipitse,
  • Hymn 1163 Tili ndi mtendere
  • Hymn 676 Adze amitundu yonse,
  • Hymn 362 Imvani Yesu akuti:
  • Hymn 295 AMBUYE wa Kumwamba,
  • Hymn 354 Tinafunafunatu,
  • Hymn 496 Yesu Mbuye ‘Nu wabwino,
  • Hymn 132 Ganizansoni, ali pano,
  • Hymn 1069 Zochimwa zathu m’mtimamo
  • Hymn 426 Mpulumutsi Yesu,
  • Hymn 262 Tumphatumpha moyo wanga,
  • Hymn 131 Lolani ana, mumve Mlungu,
  • Hymn 864 Ndi chikondi mtithandize kuigwira nkhondoyi;
  • Hymn 55 UNAKHETSEDWA mwazi do!
  • Hymn 304 POZUNZIDWA inu ponseponse
  • Hymn 1316 Ndabwera kwa Ambuyeyo:
  • Hymn 1370 Mphepo yay’kulu yakuombayo,
  • Hymn 527 Idzani mumtima mwanga,
  • Hymn 795 Sitinanyalanyalaza

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version