Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,

Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,

 

AMBUYE m’chipululu,
Analefuka ndi njala;
Polowa m’mayesero,
Anagonjetsatu Satana.
M’dziko lapansi lero lino,
Alipo omutsata,
Angoyima pa
Mulungu nji!
Ndizo mbewu zosawonongeka.

Nyamulani maso anu,
Muyang’ane m’kati mwanu;
Alipo anthu ena,
Oyitanidwa, nasankhidwa.
Mutawayang’ana iwo,
Akunga a umphawi;
Angoyima pa
Mulungu nji!
Ndizo mbewu zosawonongeka.

Kuwachotsa kwa Mbuye,
Satanayo walephera;
Powazunza iwotu,
Achiyesa chimwemwe ndithu.
Ambuye nawalimbikitsa,
Napukuta misozi;
Nawalonjeza koronayo,
Ndizo mbewu zosawonongeka.

Akhrisitu tilimbike,
Kugwira ntchito ya Mbuye;
Timvere mawu ake,
Tidzagonjetsatu Satana.
Pomalizatu moyo uno,
Tidzapita Kumwamba;
Tidzayimbira Mulunguyo,
Ndife mbewu zosawonongeka.

Post navigation

Previous: Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
Next: Hymn 301 MBUYE, ndapangana

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 672 Mbwere Yesu Mwini moyo,
  • Hymn 1063 Pokhala mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 1855 Yesu, msandipitirire
  • Hymn 1518 Zonse mwazilembamo,
  • Hymn 1247 A Chikondi chopambana,
  • Hymn 1802 Mulungu anatuma,
  • Hymn 1096 Tifuna Inu, Mbuye,
  • Hymn 1582 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 1119 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 1065 Ngakhale Satana andizunza ‘ne,
  • Hymn 1010 Ndipo ngati ungolema,
  • Hymn 1744 Kale ophunzira ake
  • Hymn 1540 Pankhope pathu mthirepo
  • Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,
  • Hymn 1383 Dzina lake tibukitsa,
  • Hymn 462 Pothandiza amathu,
  • Hymn 880 Bwenzi lathu ndiye Yesu
  • Hymn 358 Dzina lake Yesuyo,
  • Hymn 1308 Ndi ine, m’mtima Mwanu mbee!
  • Hymn 1477 Anena anthu onsewo,
  • Hymn 1741 Yesu munalaswa m’mtima,
  • Hymn 1720 Padzanja lachifundolo
  • Hymn 1612 Adzadza indetu
  • Hymn 1350 Mvera Yesu, mvera Yesu,
  • Hymn 689 Anapeza Mwana
  • Hymn 441 Tamverani, aitana:
  • Hymn 221 A! CHIKONDI chopambana,
  • Hymn 160 Kamwana kaja ‘nayamba
  • Hymn 1499 Simbanitu mwachete
  • Hymn 1550 Kutiyeretsa m’mtima
  • Hymn 313 MUNDIŴALIRE m’njira mwangamo,
  • Hymn 1581 Ndi nyimbo yabwino
  • Hymn 1599 Inde, ndifuna kumvatu
  • Hymn 816 Mdima wafika,
  • Hymn 1485 Unachimwachimwa ndithu,
  • Hymn 1608 Yesu, dzina lakukonda
  • Hymn 1613 A Mulungu
  • Hymn 1636 Potuluka m’manda mwawo
  • Hymn 360 KRISTU wakuyeratu,
  • Hymn 1288 Yesu mundimve, ndikuliratu,
  • Hymn 350 Yesu ati,
  • Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse
  • Hymn 597 Mlungu ali nane
  • Hymn 1313 Zindichulukirazi
  • Hymn 957 Mundimwetse madzi anu,
  • Hymn 642 Mulunzanitse awa,
  • Hymn 1074 Mubweretu nomwe ‘Nu munatsika kalelo;
  • Hymn 182 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 1689 Dzukani nayetu,
  • Hymn 1088 Mndiyandikitse nanu, Yesu,
  • Hymn 656 Ndipumulire panupo,
  • Hymn 1595 Ndani mwa abale athu
  • Hymn 1306 Ndi ine ndasaukadi,
  • Hymn 103 Bwenzi lathu ndinutu,
  • Hymn 267 AMBUYE, thandizenitu
  • Hymn 1001 Mafumu atiuza tikaletse ukapolo,
  • Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,
  • Hymn 186 MVERANI mbiri yozizwitsa
  • Hymn 478 Ndife ana, mutikonda,
  • Hymn 420 FESANI mbewuzo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version