Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira

  1. Home   »  
  2. Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira

Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira

 

MBUYE ndamva mwawazira
Anthu ena madalitso;
Mvula yanu yawagwera;
Mbuye, ine mudalitse.

Etu ine, etu ine,
Mbuye, ine mudalitse.

’Tate, msandipitirire,
Ndimaipa mtima ine;
Ndiyenera munditaye,
Koma mukhululukire.

Yesu, msandipitirire
Kuti ndinu ndikondane;
Ndinalira Inu Mbuye,
Msandileke poitana.

Mzimu, msandipitirire,
Mupenyetsatu akhungu
Mboniyo ya Mbuye Yesu,
Mundipatse ine mphamvu.

Ndinagona mwa zoipa,
Ndinakunyozani ine,
Dziko lino ndinakonda,
Mbuye, mukhululukire.

Ha! chikondi cha Mulungu,
Mwazi wa Mbuyathu Yesu,
Chiyanjano cha Mzimuyo
Zonse zidzalemekeza.

Post navigation

Previous: Hymn 265 MUDZAZE Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
Next: Hymn 267 AMBUYE, thandizenitu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1168 Aleluya, muyenera!
  • Hymn 1720 Padzanja lachifundolo
  • Hymn 1162 Mumvetu abwenzi athu,
  • Hymn 1591 Sizitha ntchito zangazo,
  • Hymn 1013 Tizifesa m’dzuwa,
  • Hymn 1605 Yesu, dzina lokondwetsa
  • Hymn 1482 Tsopano inu ‘dzanitu,
  • Hymn 12 NDITAMATU Ambuyangayu,
  • Hymn 587 Mutitsuke,
  • Hymn 1248 ‘Dzanitu Wamphamvu yonse,
  • Hymn 1441 Wochimwa iwe, bweratu
  • Hymn 1294 Wakuba uja nachiona,
  • Hymn 928 Usalire; Mpulumutsi
  • Hymn 1438 Yesu akukonda,
  • Hymn 1637 Tisaleke kugwirabe
  • Hymn 978 Mtima wanu wonse ndithu
  • Hymn 1555 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 405 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 817 Tibvomereze,
  • Hymn 491 N’takafika kwanu
  • Hymn 1401 Imvani mawu ake, idzanitu,
  • Hymn 673 Mbwere Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 1801 Nafuna kwaononga
  • Hymn 27 “Msanga ndidzabweratu,
  • Hymn 1643 Kufuna inetu, kufuna inetu,
  • Hymn 1243 Kodi mayi wobereka
  • Hymn 320 Ambuye, wakuti ndi mwaziwo
  • Hymn 1669 Ukafuna kumdziwitsa,
  • Hymn 947 Akristu tonsefe, tikondwe m’Dzikoli
  • Hymn 167 KODI mwalandira Yesu?
  • Hymn 981 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 1110 Mulungu wanga,
  • Hymn 1192 Pamtanda woopsa
  • Hymn 1745 Yesu aitana ife:
  • Hymn 187 UFUNA kuwomboledwa kodi?
  • Hymn 286 ZOVUTA zoopsya ndi zosaukazi
  • Hymn 1578 Onsewa ‘nachimwa
  • Hymn 248 Pena pakufadi,
  • Hymn 501 Yesu andikonda ine;
  • Hymn 33 OWONADI mtima,
  • Hymn 171 IWE tiye, iwe tiye,
  • Hymn 220 MULUNGU mundichitire chifundo,
  • Hymn 1732 Anapachikidwatu,
  • Hymn 851 E, nthawi ya mamawayi
  • Hymn 1563 Mufike monga nyali younika m’mtimamo,
  • Hymn 622 Tiyamikira ‘Tate,
  • Hymn 779 Yesu Mbuye wanga,
  • Hymn 269 NDILIRA ine kukayenda
  • Hymn 672 Mbwere Yesu Mwini moyo,
  • Hymn 720 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 257 NJIRA yanga sindiziŵa,
  • Hymn 363 ATATE ndiyamika,
  • Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,
  • Hymn 1475 Anathera pamtanda zintchito zonsezi
  • Hymn 891 Akakusowa malo
  • Hymn 134 INU ansembe ngakhale mufunsa,
  • Hymn 998 Anatilemba Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 746 Imfa ndi mdima zinathawa zii!
  • Hymn 730 A! Yesu mwapangana
  • Hymn 497 Yesu andikonda ine,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version