Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira

  1. Home   »  
  2. Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira

Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira

 

MBUYE ndamva mwawazira
Anthu ena madalitso;
Mvula yanu yawagwera;
Mbuye, ine mudalitse.

Etu ine, etu ine,
Mbuye, ine mudalitse.

’Tate, msandipitirire,
Ndimaipa mtima ine;
Ndiyenera munditaye,
Koma mukhululukire.

Yesu, msandipitirire
Kuti ndinu ndikondane;
Ndinalira Inu Mbuye,
Msandileke poitana.

Mzimu, msandipitirire,
Mupenyetsatu akhungu
Mboniyo ya Mbuye Yesu,
Mundipatse ine mphamvu.

Ndinagona mwa zoipa,
Ndinakunyozani ine,
Dziko lino ndinakonda,
Mbuye, mukhululukire.

Ha! chikondi cha Mulungu,
Mwazi wa Mbuyathu Yesu,
Chiyanjano cha Mzimuyo
Zonse zidzalemekeza.

Post navigation

Previous: Hymn 260 ODALA ndi onsewo,
Next: Hymn 281 MBUYE, mwatiuza ’fe

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1378 Tsopano linoli
  • Hymn 902 Ndikondwa kuganizabe
  • Hymn 200 YESU mundimve, ndikuliratu,
  • Hymn 446 Yesu alandira
  • Hymn 281 MBUYE, mwatiuza ’fe
  • Hymn 483 NTHAŴI yaubwana yatha,
  • Hymn 830 Atate ndiyamika, mwandisamalira leroli;
  • Hymn 1125 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 1551 Mukhale m’kati mwathu,
  • Hymn 283 Ndalema ndathodwa
  • Hymn 223 Ndafoka, ndaipa,
  • Hymn 443 M’MAŴA tizifesa
  • Hymn 877 Zokoma ndithu nthawizi
  • Hymn 560 Kale m’mzinda wachifumu
  • Hymn 1152 Pokonda Yesuyo, mtendere!
  • Hymn 1047 Ambuye, chotsani zonse zomwezo
  • Hymn 1314 Mulungu ali nane!
  • Hymn 1150 Pamtanda Mbuyanga ‘nafera,
  • Hymn 379 MTSINJE woyerawo
  • Hymn 430 MLUNGU akuyang’aniredí,
  • Hymn 1200 Ambuye, m’imfamo
  • Hymn 66 Chisomocho chachotsadi
  • Hymn 55 Ambiri tikondwera mwa Yesu,
  • Hymn 1222 Bwenzi ndimamkomanayo
  • Hymn 946 Ngakhale enawo aleke kwimbako,
  • Hymn 507 Yesu ndimkonda, akondanso ine,
  • Hymn 1373 Zamoyo zili m’thengo zonsezo,
  • Hymn 1304 Ndi ine sizitheka ‘yi
  • Hymn 361 Munka kangati kulawa
  • Hymn 1426 Wina panalibe
  • Hymn 577 Adagona m’ndyeromo
  • Hymn 186 MVERANI mbiri yozizwitsa
  • Hymn 831 Mundikumbutse, ndikapanda tulo, za Kumwambako;
  • Hymn 1713 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 247 MULUNGU anditsogolera,
  • Hymn 1051 Zin’sowa indedi
  • Hymn 186 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 1650 E, moyo wanga’we
  • Hymn 948 Tiimbe mokondwa, misozi iume;
  • Hymn 868 Atate yemwe anatuma Mpulumutsi mmodzi
  • Hymn 116 Nkhosa zanga zimandimva
  • Hymn 1632 Ndi chiyembekezo ichi
  • Hymn 1493 Mbiri yakalelomwe
  • Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo
  • Hymn 1083 “Khala mwa Ine,” Yesu anatero;
  • Hymn 1181 Adalitsika munthuyo
  • Hymn 1775 Oonadi mtima,
  • Hymn 1258 Zonse zina sizikwana,
  • Hymn 1008 Wakuchezacheza naye
  • Hymn 598 Mlungu ali nane;
  • Hymn 700 Mzimu woonadi
  • Hymn 1289 Ndinasokeratu kutaliko,
  • Hymn 900 Mutipatse leroli
  • Hymn 1798 Mukondwe anthu a Mulungu,
  • Hymn 714 Dzuwa ndi mvula yonseyo
  • Hymn 405 POLENGA dzikoli
  • Hymn 1529 Mndithandize kukondana
  • Hymn 1023 Kodi m’njiramo ndimvadi
  • Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu
  • Hymn 1013 Tizifesa m’dzuwa,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version