Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,

  1. Home   »  
  2. Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,

Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,

 

TIMVE za anamwali khumi,
Okonzeka mosiyana;
Asanu anali opusa zedi,
Ena anachenjeradi.

Asanu anatenga mafuta padera,
Iwowa anachenjera,
Asanu sanatenge mafuta adera,
Iwowa anapusadi.

Mkwati pamene anafika,
Pakati pa usikuwo,
Asanu osatenga mafutawo,
Sanathe kulowa m’nyumba.

Tisakhale ngati opusa,
Osatenga mafutawo.
Tikhale ngatitu ochenjerawo,
Titenge mafuta athu.

Mbale ukhale wochenjera,
Pakulapa zoipazo;
Pakukhulupiliratu Mulungu,
Kuti tikalowe M’mwamba.

Post navigation

Previous: Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
Next: Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 929 Chikondano sichifera;
  • Hymn 1141 Pakulekana ifetu
  • Hymn 51 Mbuye dalitsani Afrika,
  • Hymn 1540 Pankhope pathu mthirepo
  • Hymn 712 Mulungu akondadi leroli
  • Hymn 855 Aulendo amayenda
  • Hymn 435 ANAKWATIRA kale
  • Hymn 573 Ambuye, tikutamandani
  • Hymn 122 KUNALI munthu wa Mlungu,
  • Hymn 378 KWEZANI mitu yanuyo,
  • Hymn 731 Mundionetse, Yesu,
  • Hymn 1228 Lindikomera dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 769 Ndi kutsukidwa m’mwazimo
  • Hymn 324 TIKAGWIDWA ndi chisoni,
  • Hymn 518 Ana a Yerusalemu
  • Hymn 1334 Walandira inetu
  • Hymn 251 Kuli chimwemwe m’dzuwalo
  • Hymn 1625 Ife tonse tikumbuke
  • Hymn 339 Tipempha,
  • Hymn 1397 Okwawa pansi inu,
  • Hymn 473 Mzinda woyerawo!
  • Hymn 1760 Amithenga a Mulungu
  • Hymn 1381 Ndi mitima yokondwera
  • Hymn 996 Leka zakuipa zako,
  • Hymn 45 IFE timakufunani
  • Hello world!
  • Hymn 138 Kumva ulikumva, ulikumva,
  • Hymn 371 AMBUYE, tasonkhana
  • Hymn 858 Anthu osawerengeka
  • Hymn 930 Leroli chisoni chokha,
  • Hymn 1829 Mulungu ndiye Mbusa wanga, sindisowa konse;
  • Hymn 781 Tatsegukani inutu,
  • Hymn 1375 Ndi anamwali obvekedwa mbuu!
  • Hymn 249 Amen, Amen, Amen.
  • Hymn 508 Mzimu Woyera akhala mwa ine,
  • Hymn 1210 Kumwamba ndidzanenadi
  • Hymn 210 Nyumba yodyera ilikudzaza;
  • Hymn 427 AULENDO amayenda
  • Hymn 1372 Zam’madzi zonse zakuopsyazo,
  • Hymn 134 INU ansembe ngakhale mufunsa,
  • Hymn 158 Mzimu, mlonge m’mtimamo
  • Hymn 26 NDIKULEMEKEZA
  • Hymn 44 Mlungu dalitsani Malawi,
  • Hymn 614 Adzabwera Mbuye wathu
  • Hymn 506 Ndikondwa kuti Yesu akonda,
  • Hymn 1021 Kunsi kudambo, pena m’mwamba m’phirimo,
  • Hymn 1715 Kodi misozi itisowa,
  • Hymn 265 Imbirira moyo wanga,
  • Hymn 228 MWAKHULUPIRIRADI
  • Hymn 744 Kristu ndi mwini moyo wathuwu,
  • Hymn 1253 Ndingopatsa Inu Mbuye
  • Hymn 1079 Khalatu woyera,
  • Hymn 1558 Wosangalatsa, ine ndikalira
  • Hymn 1494 Mbiri yakalelomwe,
  • Hymn 137 Yesu Mpulumutsi, Mpulumutsi
  • Hymn 795 Sitinanyalanyalaza
  • Hymn 832 Zochimwa za usana uno mndikhululukire ‘ne;
  • Hymn 1312 Wina sindifuna ‘yi,
  • Hymn 500 >AMEN, Amen, Amen.
  • Hymn 260 ODALA ndi onsewo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version