Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 181 PANALITU wakudwala

  1. Home   »  
  2. Hymn 181 PANALITU wakudwala

Hymn 181 PANALITU wakudwala

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 181 PANALITU wakudwala

 

PANALITU wakudwala
Amene akakhala
Pakhomo la sunagoge:
Kuti anthu ena
Amuone iye.

Yenda iwe, yenda.
Yenda iwe, yenda,
Siliva ndilibe;
Mwa Yesuyo, yenda!

Kukondwa kwa wodwalayo
Kunali kopambana;
Iye anatumphatumpha,
Kuzungulira
Sunagoge yense.

Lero lino Mbuye Yesu
Aitana nonsenu;
Mukamvera ndi kumtsata,
Mudzakondwera
Ndi mdalitso wake.

Post navigation

Previous: Hymn 180 MALO alimo m’nyumba ya Yesu,
Next: Hymn 201 NDILINKUDZA kwa Ambuye,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 290 Ndi miyendo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 769 Ndi kutsukidwa m’mwazimo
  • Hymn 1534 Mukonze mtima wangawu,
  • Hymn 612 Oyamika Mlungu mbwere,
  • Hymn 1395 Mulungu ali nane!
  • Hymn 85 Mtima wanga wabvutika,
  • Hymn 32 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 600 Mbuye Yesu, myandikire,
  • Hymn 397 Yesu Mbusa, mutimvere,
  • Hymn 293 LIMBA mtima mbale wanga
  • Hymn 616 Dziko lathu lonseli
  • Hymn 340 Imvani,
  • Hymn 300 AKRISTU limbikani,
  • Hymn 740 Tsopano nthawi yake phwandili,
  • Hymn 1201 Kumwamba kwanuko
  • Hymn 1267 Kwa Inu Yesu ndilira,
  • Hymn 149 RUTE, Rute anaumilira,
  • Hymn 140 Panalitu wakudwala
  • Hymn 237 Munasiyatu
  • Hymn 393 ZOPEREKA tiperekazi,
  • Hymn 26 “Ndakukonda ku imfa
  • Hymn 426 MBUYE, Mpingo wanu usauka kwakukuludi;
  • Hymn 470 YESU andikonda ine,
  • Hymn 259 CHISOMO chodabwitsacho,
  • Hymn 90 Ufuna kuleka kunyadako?
  • Hymn 88 Ufuna kuwomboledwa kodi?
  • Hymn 1370 Mphepo yay’kulu yakuombayo,
  • Hymn 386 Tiyamike Mlunguyo,
  • Hymn 1683 Nsinga za imfa Iye ‘nadula,
  • Hymn 731 Mundionetse, Yesu,
  • Hymn 3 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 1150 Pamtanda Mbuyanga ‘nafera,
  • Hymn 416 PALIBE wina Kumwamba,
  • Hymn 727 Imfa ikandifikira,
  • Hymn 1678 Yesu nkana saoneka, Aleluya,
  • Hymn 261 Munafera pa mtanda
  • Hymn 552 Analira ndaniyo
  • Hymn 939 Ambuye andisunga
  • Hymn 487 INE ndine mlendo
  • Hymn 1801 Nafuna kwaononga
  • Hymn 1656 Inu mundibisadi
  • Hymn 382 Mwadzoza mutu wanga ndi
  • Hymn 1828 Timtamande Iye ndi moyo wathunso
  • Hymn 417 M’manja a Yesu wanga
  • Hymn 270 Zoopsya zopambana
  • Hymn 228 Ataya zoipa,
  • Hymn 333 Perekani, perekani
  • Hymn 1559 Wotsogolera, munditsogolere
  • Hymn 31 MULUNGU Wamkulu,
  • Hymn 409 Yesu adza kuwerenga
  • Hymn 705 Tikhaletu nawo, Mbuye,
  • Hymn 1841 Kumadzi kuli njiratu andiyendetsa bwino,
  • Hymn 1264 Chifuniro change, Mbuye, Ndiperekachi;
  • Hymn 176 Mleke mdaniyo, mwimbe m’njiramo
  • Hymn 514 Osanatu, osana,
  • Hymn 164 Yendani, Mfumu yamtendere
  • Hymn 1346 Ndaima pano, ndaima pakhomo:Lowa, lowa, lowa, lowa!
  • Hymn 857 Mlungu amaunikira
  • Hymn 667 Akutopa ndi ofoka
  • Hymn 1770 Iye amazichita zamphamvu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version