Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 166 NDICHITENJI kukapeza

  1. Home   »  
  2. Hymn 166 NDICHITENJI kukapeza

Hymn 166 NDICHITENJI kukapeza

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 166 NDICHITENJI kukapeza

 

NDICHITENJI kukapeza
Moyo? thandizeni!
Ndili wakutopa; Mzimu,
Muthandize ine.

Zonse zinathedwadi;
Yesu watha zonsezo;
Sutha ntchito, ungomvera
Mawu ake omwewo.

Iye anatsika m’Mwamba,
Anachoka kwawo,
Anafera anthu, nati:
“Ndatha zonse zawo.”

Mbuye wanga ndili kumva,
Ndikondana nanu;
Umapuma mzimu wanga,
Kwathu ndiko kwanu.

Post navigation

Previous: Hymn 160 MADALITSO ngati mvumbi,
Next: Hymn 181 PANALITU wakudwala

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1341 Tadza kukudyaku,
  • Hymn 993 Pakumalizidwa
  • Hymn 299 “Posunga nkhosa ife
  • Hymn 485 POMPANO pandikonda
  • Hymn 176 Mleke mdaniyo, mwimbe m’njiramo
  • Hymn 1201 Kumwamba kwanuko
  • Hymn 341 PAKUPEMPHERATU
  • Hymn 770 Atate, muwapenye
  • Hymn 1592 Tsono mubwere inunso,
  • Hymn 780 Kwezani mitu yanuyo,
  • Hymn 454 TAONANI, m’kholamo,
  • Hymn 97 Maso ndi maso ndi Kristu,
  • Hymn 1421 Alongo ‘nu, alongo ‘nu,
  • Hymn 1526 Mbuye wondipulumutsa
  • Hymn 950 Sindidapempha kale Mbuye ‘yi,
  • Hymn 185 NDINE Mbusayo wabwino,
  • Hymn 1619 Adzabwera,
  • Hymn 414 INU bambo, inu mayi,
  • Hymn 1460 Akuti anthu akumvera
  • Hymn 1715 Kodi misozi itisowa,
  • Hymn 307 ABALE anga ine ndikupita,
  • Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,
  • Hymn 1328 Ndani afuna kunkako
  • Hymn 1492 Sakukanani Yesudi,
  • Hymn 1280 Kuti mundipatsa mphamvu yopambanayo;
  • Hymn 692 Paulendo wathu
  • Hymn 1081 Ndikabisala mwanu
  • Hymn 65 NLA Mlungu dzuŵali:
  • Hymn 1354 Mzimu Woyera, m’mtimamo
  • Hymn 1650 E, moyo wanga’we
  • Hymn 731 Mundionetse, Yesu,
  • Hymn 729 Ndifuna kumva Inu,
  • Hymn 899 ‘Tate wa Kumwambako,
  • Hymn 496 Yesu Mbuye ‘Nu wabwino,
  • Hymn 968 Mzimu wakuipa
  • Hymn 77 MMENE Yesu adzabwera,
  • Hymn 1803 Nowayo nayendamo,
  • Hymn 958 Ndikalowa m’mtsinje muja,
  • Hymn 400 Dzuwa liwala, m’tulotu
  • Hymn 118 Musaone zobvalazo,
  • Hymn 355 DZIKO lonse mlambire
  • Hymn 396 PETURO ’nafunsa Hananiya:
  • Hymn 1581 Ndi nyimbo yabwino
  • Hymn 1668 Kumdziwitsa ndiko moyo,
  • Hymn 801 Lero mwatipatsa moyo,
  • Hymn 697 Zolengedwa zonse zidze
  • Hymn 1272 Muyambe ntchito yanuyi,
  • Hymn 411 TAMVA mawu omwewo,
  • Hymn 237 SINDINANYENGEDWA konse
  • Hymn 1630 Anthu anu amafoka,
  • Hymn 664 Komwe asauka anthu
  • Hymn 25 ANGELO amayimba,
  • Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,
  • Hymn 1805 Anafa m’mvula muja
  • Hymn 335 Mtembenuke mtima wanu,
  • Hymn 219 Mtenderewo wosanyenga
  • Hymn 1 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 230 AMBUYANGA Yesu,
  • Hymn 1156 Imfa ndi manda sitiopa ‘yi,
  • Hymn 467 Ife ana sitiopa,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version