Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 164 WANENA ndi Yesu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 164 WANENA ndi Yesu,

Hymn 164 WANENA ndi Yesu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 164 WANENA ndi Yesu,

 

WANENA ndi Yesu,
Mawu onse awa;
Mfumu yamtendere,
Yalonjeza kuti:

“Sindim’tulutsa
sindidzam ‘taya;
Wakudza kwa Ine
Sindim’tulutsa,
sindidzam’taya
Wakudza kwa Ine.”

“Mfulu ndi kapolo,
Adzetu kwa Ine;”
Wanena ndi Yesu,
Mawu onse awa.

Onse akulapa,
Adzawona mwayi;
Ndipo adzayimba,
Pamodzi ndi Yesu.

Post navigation

Previous: Hymn 160 MADALITSO ngati mvumbi,
Next: Hymn 181 PANALITU wakudwala

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 242 NDIIMBA mumtima mokondwa,
  • Hymn 505 Ndikondwa kuti Atate wam’Mwamba
  • Hymn 1729 Munthu Wazisoniyo
  • Hymn 1609 Idzani nose’nu
  • Hymn 1142 Tidzathawira kuti ‘fe
  • Hymn 463 MNANDIDZERA, Ambuye,
  • Hymn 869 Anatipatsa Mawu onse olimbitsa mtima;
  • Hymn 1844 Pamaso pa adaniwo mwayala gome langa;
  • Hymn 850 Pemphero, pemphero,
  • Hymn 46 INALIPO nthawi,
  • Hymn 102 Mzimu ndi mtsogoleri
  • Hymn 390 Lalowa dzuwa, kwada bii!
  • Hymn 560 Kale m’mzinda wachifumu
  • Hymn 118 Musaone zobvalazo,
  • Hymn 185 NDINE Mbusayo wabwino,
  • Hymn 237 Munasiyatu
  • Hymn 683 Musamaopa kanthu ‘yi, tamani Yesuyo;
  • Hymn 1832 Za m’mdima, imfa, nkhondo ndi zoipa sindiopa;
  • Hymn 1793 Pakuwoloka mtsinje wa imfa
  • Hymn 1642 M’khola mwa ng’ombe ku Betelehemu
  • Hymn 1755 Choti timtumikire
  • Hymn 259 CHISOMO chodabwitsacho,
  • Hymn 302 Anasenza m’thupi mwake;
  • Hymn 56 KU Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 1546 Mubwere Mzimu Inu
  • Hymn 934 Mnamwalira Inu paja,
  • Hymn 453 Tiana ta Ambuye tili
  • Hymn 1586 Mbuye Yesu timtamanda
  • Hymn 791 Anthu opembedzawo
  • Hymn 1687 Alonda onsewo
  • Hymn 1440 Yesu alindira,
  • Hymn 685 Tamva mawu amwewo
  • Hymn 77 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 458 Anyamata inutu,
  • Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,
  • Hymn 289 ANATILEMBA Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 1560 Mthandizi ndinu, mndithangate ine
  • Hymn 387 MUDZE, anthuni, talaŵani ’nu
  • Hymn 27 “Msanga ndidzabweratu,
  • Hymn 201 Ngati zakuipa zathu
  • Hymn 1452 Inu akutopawo,
  • Hymn 54 MUNTHU wazisoniyo,
  • Hymn 589 Koma ineyu
  • Hymn 223 ATI Yesu Mbuyeyo:
  • Hymn 1771 Iye natsitsa kunsi
  • Hymn 1574 Anthu ose ndi mitundu
  • Hymn 601 Akaona masautso
  • Hymn 169 M’manda nagonamo
  • Hymn 968 Mzimu wakuipa
  • Hymn 1069 Zochimwa zathu m’mtimamo
  • Hymn 1197 Ndafoka ine kale,
  • Hymn 1309 Ndi inetu ndidziwedi
  • Hymn 918 Ntchito yonse yakeyo
  • Hymn 439 MLUNGU wathu mwatifitsa
  • Hymn 379 MTSINJE woyerawo
  • Hymn 636 Yehova Mlungu wathu,
  • Hymn 557 Usikuwo woyerawo!
  • Hymn 1431 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 151 Inde, Yesu, mulandira,
  • Hymn 504 Pakumyamika Iye

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version