Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu

  1. Home   »  
  2. Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu

Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu

 

UTHENGA wa Mulungu
Waloŵa m’mtimamu,
Wochotsa zoipazo
Zakundidetsazo.

Pakuti anthu akumvera
Yesu aŵapulumutsa,
Ine, aŵapulumutsa, indetu.

Ndidziŵa kuti Yesu
Anafa kalelo,
Nafafaniza zonse
Tinazichimwazo.

Satana ndi unyolo
Anandimanga nji!
Ambuye Yesu yekha
Nandimasuladi.

Ambuye muloŵetse
Mtendere m’mtimamo,
Ndimvetse mawu anu
Masiku onsewo.

Akuti anthu akumvera
Yesu aŵapulumutsa,
Inde, aŵapulumutsa, indetu.

Post navigation

Previous: Hymn 154 SING’ANGA ‘mkulu ndiye Yesu,
Next: Hymn 156 OKOMA ndiwo mawu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 769 Ndi kutsukidwa m’mwazimo
  • Hymn 1239 Ndipo pakuima phe!
  • Hymn 1645 Nafera inetu, nafera inetu
  • Hymn 1187 M’mitima mwathu mwakhala mbee!
  • Hymn 379 Anditsogolera m’njira
  • Hymn 87 IDZANI nonse ’nu
  • Hymn 1288 Yesu mundimve, ndikuliratu,
  • Hymn 470 YESU andikonda ine,
  • Hymn 1622 Anthu onse amlambire
  • Hymn 85 Mtima wanga wabvutika,
  • Hymn 631 Mulungu wa Yakobo Inu, mdyetsa anthu anu,
  • Hymn 506 Ndikondwa kuti Yesu akonda,
  • Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu
  • Hymn 836 Kamoyo kanga katha lero lino,
  • Hymn 1826 Amadyetsa Iye mbalame zam’mwamba,
  • Hymn 118 PANALI munthu amene,
  • Hymn 55 UNAKHETSEDWA mwazi do!
  • Hymn 663 Anyamata a Mulungu,
  • Hymn 263 AMBUYE mundisunge
  • Hymn 585 Alanditsa,
  • Hymn 1121 Ndifuna Yesuyo,
  • Hymn 33 OWONADI mtima,
  • Hymn 1071 Kumwamba Yesu mthandize,
  • Hymn 1767 Ndiye anayang’ana
  • Hymn 301 MBUYE, ndapangana
  • Hymn 1256 Chitsime ndi chokoma
  • Hymn 1345 Iwe tiye, iwe tiye,
  • Hymn 1036 Mtima wakufatsa
  • Hymn 621 Wolenga ndi Yemweyo
  • Hymn 288 Ndi maso athu awa nawo nganu,
  • Hymn 790 Zimbalame zonsezi
  • Hymn 1710 Pamtandapo, pamtandapo
  • Hymn 1515 Ndikachimwa, Bukuli
  • Hymn 828 Ndidzukanso m’mawa,
  • Hymn 1324 M’moyo uno kunsiku
  • Hymn 541 Ana inu, yamikani
  • Hymn 1122 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 294 POYESEDWA ine
  • Hymn 219 YESU Mbuyetu, mwafera
  • Hymn 315 YENDANI munjira yake,
  • Hymn 337 PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;
  • Hymn 589 Koma ineyu
  • Hymn 361 Munka kangati kulawa
  • Hymn 1339 Musaope pokumbuka
  • Hymn 1005 Mdani adza nazo mphamvu,
  • Hymn 1441 Wochimwa iwe, bweratu
  • Hymn 945 Tiyeni pamodzi,
  • Hymn 1777 Mulungu wamkulu
  • Hymn 446 Yesu alandira
  • Hymn 460 E! ang’ono ndifetu,
  • Hymn 1796 Ndikhulupira mwa Ambuye
  • Hymn 1186 Yesu anafa pamtandapo,
  • Hymn 417 M’manja a Yesu wanga
  • Hymn 538 Iye anachoka kwawo,
  • Hymn 98 YESU, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 1576 Khamulo liliko
  • Hymn 1458 Satana ndi unyolo
  • Hymn 1705 Pa Iye padzapo
  • Hymn 148 PAKUPEMPHA ife pano,
  • Hymn 1154 Zakutsogolo sitidziwa ‘yi;

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version