Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu

  1. Home   »  
  2. Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu

Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu

 

UTHENGA wa Mulungu
Waloŵa m’mtimamu,
Wochotsa zoipazo
Zakundidetsazo.

Pakuti anthu akumvera
Yesu aŵapulumutsa,
Ine, aŵapulumutsa, indetu.

Ndidziŵa kuti Yesu
Anafa kalelo,
Nafafaniza zonse
Tinazichimwazo.

Satana ndi unyolo
Anandimanga nji!
Ambuye Yesu yekha
Nandimasuladi.

Ambuye muloŵetse
Mtendere m’mtimamo,
Ndimvetse mawu anu
Masiku onsewo.

Akuti anthu akumvera
Yesu aŵapulumutsa,
Inde, aŵapulumutsa, indetu.

Post navigation

Previous: Hymn 140 NDINAMIRA m’machimo, wosaonekanso,
Next: Hymn 161 LERO lino mbale wanga,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1095 Mumtima wakufatsa
  • Hymn 770 Atate, muwapenye
  • Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,
  • Hymn 1657 Mbuye, mutsaganebe
  • Hymn 1815 Choposa nalo thupilo,
  • Hymn 259 Zoipa zakanikadi,
  • Hymn 1217 Chisoni chonsecho
  • Hymn 172 Imfa yalephera
  • Hymn 908 Ndikonda kuganizirabe
  • Hymn 951 Ndi kale lonse mnandisunga ‘ne;
  • Hymn 1594 Chikondano chakechi
  • Hymn 59 Tinachoka munjira ya imfa,
  • Hymn 268 Potuluka m’mudzimo
  • Hymn 841 Mukhale, mukhale,
  • Hymn 490 Yesu, ndikabwera
  • Hymn 270 Zoopsya zopambana
  • Hymn 359 TADZUKA mzimu wanga ‘we,
  • Hymn 777 Mulungu ali muno,
  • Hymn 91 Ufuna kuyera kopambana?
  • Hymn 73 M’SANDIPITILIRE Yesu,
  • Hymn 448 CHIFUKWA cha zokoma mtima zonse zaulelezo,
  • Hymn 1400 Tulani zoipazi, idzanitu,
  • Hymn 1449 Pena imfa idza mawa,
  • Hymn 1271 Onani Mbuye ndigonja,
  • Hymn 1819 Pokondwa ndi poona bvuto
  • Hymn 1059 Kalelo m’mtima ndinakondwa,
  • Hymn 1683 Nsinga za imfa Iye ‘nadula,
  • Hymn 403 NDIYIMBA ndi chimwemwe lero,
  • Hymn 916 Akondwerera anthu
  • Hymn 462 ANANU, ziimbani,
  • Hymn 1514 Dzinthu zakumundazo
  • Hymn 1159 Mwalembedwa mukalata
  • Hymn 498 Yesu akonda,
  • Hymn 1571 Tamani mphamvu ya Yesu,
  • Hymn 247 Tsono poukanso
  • Hymn 1499 Simbanitu mwachete
  • Hymn 1600 E! dzina la Yesu,
  • Hymn 207 Malo alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 1479 Ndi Yesu yemwe kalelo
  • Hymn 390 A! YESU, ndapangana
  • Hymn 1662 Msandipitire, Yesu,
  • Hymn 1210 Kumwamba ndidzanenadi
  • Hymn 1788 Mtimanga, bwera kuti upumule
  • Hymn 1793 Pakuwoloka mtsinje wa imfa
  • Hymn 417 M’manja a Yesu wanga
  • Hymn 608 Maluwa abwino aphuka m’mapiri ndi m’madambomo,
  • Hymn 1625 Ife tonse tikumbuke
  • Hymn 896 Mbuye, ndinalema ine,
  • Hymn 960 Tilikupita kwathu kuja
  • Hymn 486 Yesu, Yesu,
  • Hymn 263 Mulungu wakwezekatu,
  • Hymn 1387 Amaweta nyama zonse,
  • Hymn 426 MBUYE, Mpingo wanu usauka kwakukuludi;
  • Hymn 470 Mutiletse tisaname
  • Hymn 1461 Sing’anga ‘mkulu ndiye Yesu,
  • Hymn 1015 Mbuye, mwatiuza ‘fe
  • Hymn 1619 Adzabwera,
  • Hymn 879 Zokoma etu nthawizi”
  • Hymn 34 Yesu Mbuyetu, mwafera
  • Hymn 1833 Podwala ine pobvutidwa Andisamalira;

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version