Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu

  1. Home   »  
  2. Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu

Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu

 

UTHENGA wa Mulungu
Waloŵa m’mtimamu,
Wochotsa zoipazo
Zakundidetsazo.

Pakuti anthu akumvera
Yesu aŵapulumutsa,
Ine, aŵapulumutsa, indetu.

Ndidziŵa kuti Yesu
Anafa kalelo,
Nafafaniza zonse
Tinazichimwazo.

Satana ndi unyolo
Anandimanga nji!
Ambuye Yesu yekha
Nandimasuladi.

Ambuye muloŵetse
Mtendere m’mtimamo,
Ndimvetse mawu anu
Masiku onsewo.

Akuti anthu akumvera
Yesu aŵapulumutsa,
Inde, aŵapulumutsa, indetu.

Post navigation

Previous: Hymn 140 NDINAMIRA m’machimo, wosaonekanso,
Next: Hymn 161 LERO lino mbale wanga,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 69 Kwathu sipadziko, ndingopitirira,
  • Hymn 378 KWEZANI mitu yanuyo,
  • Hymn 1107 Anthu onse pansi pano
  • Hymn 1850 Anthu a mitundu yonse,
  • Hymn 157 Mbuye, Mzimu Woyera
  • Hymn 436 YEHOVA Mlungu wathu,
  • Hymn 154 SING’ANGA ‘mkulu ndiye Yesu,
  • Hymn 1224 Inde ndidzaimba nyimbo
  • Hymn 757 Sindili woyenera ‘ne;
  • Hymn 1440 Yesu alindira,
  • Hymn 1597 Timchimwira kopambana,
  • Hymn 1075 Ndikhazikike inetu, mumtima muli mwai,
  • Hymn 65 NLA Mlungu dzuŵali:
  • Hymn 449 MLENGI wathu Woyeranu,
  • Hymn 1169 Mwazi wa Yesu
  • Hymn 197 Tidzatama Atate wathu
  • Hymn 465 Yesu atiuza tiwale pa
  • Hymn 1199 Ndikhumba ine ndithu
  • Hymn 68 Kwathu ndidzaimba nyimbo
  • Hymn 26 NDIKULEMEKEZA
  • Hymn 535 Mbuye timlemekeze,
  • Hymn 1803 Nowayo nayendamo,
  • Hymn 1165 Dzanja la Mulungu
  • Hymn 289 Ndi manja athu awa nawo nganu,
  • Hymn 1856 Mzimu, msandipitirire,
  • Hymn 319 Koma zina sizinadziwa ayi,
  • Hymn 336 Perekani mtima wanu
  • Hymn 1554 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 153 Pemphero ndiko kufuna,
  • Hymn 1573 Inu osankhidwa ake,
  • Hymn 67 Chisomo chandisungadi
  • Hymn 162 Angelo anu asunga
  • Hymn 1459 Ambuye mulowetse
  • Hymn 1198 Mabala ake m’manja
  • Hymn 237 Munasiyatu
  • Hymn 358 MLUNGU ali muno,
  • Hymn 1038 Limbikani nonse
  • Hymn 276 Dziko lonse mlambire
  • Hymn 1106 Mlungu ndi wachikhalire.
  • Hymn 1252 Pakukumbukira zanga
  • Hymn 84 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 735 Mwa chikho chokumbutsa
  • Hymn 497 Yesu andikonda ine,
  • Hymn 661 Tamva aku Makedonyako atero,
  • Hymn 1547 Mtisangalatse m’zonse,
  • Hymn 855 Aulendo amayenda
  • Hymn 1033 Mkristu gwiratu ntchito
  • Hymn 1365 Zozizwa za m’dziko,
  • Hymn 1152 Pokonda Yesuyo, mtendere!
  • Hymn 823 M’mwambamo nyenyezi
  • Hymn 921 Komwe Mbusa kwawoko
  • Hymn 1073 Mwa ine myatse moto wanu wakuyera mbuu,
  • Hymn 1125 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 1057 Ndilira ine kukayenda
  • Hymn 227 Kasupe ali wodzaza
  • Hymn 1600 E! dzina la Yesu,
  • Hymn 1281 Ndikhulupirira, Yesu, mndibvomereko;
  • Hymn 1105 Khala chete mtima wanga
  • Hymn 1131 M’mene ine ndisauka
  • Hymn 703 Dzuwa, madzi, kudya, mpweya,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version