Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,

Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,

 

MIPINGO iyo idzatu,
Yoyenda mangu pajapo,
Afuma kuti anthuwo?
Afika bwanji komweko?

Anena anthu onsewo,
“Yesu Sing’anga apitapo.”
Anena anthu onsewo,
“Yesu Sing’anga apitapo”

Azizwa anthu ajawo,
Nafunsa, “Ndani mlendoyo?
Wanzeru monga Iyeyo
Kulibe wina konseko.”

Ndi Yesu yemwe kalelo,
’Nakhala munthu pansipa;
Anthenda onsenthaŵiyo
Nachirayake mphamvuyo

Afika Yesu leroli,
Chifundo m’mtima wakemo,
Timfitse msanga kwathuko
Akhale nafe ponsepo.

Timsankhe Yesu Mbuyeyo,
Timyese Mfumu yathuyo,
Chifukwa tikamkanatu
Tikhala otayikawo.

Tsopano inu’dzanitu,
Asanapitirirepo.
Tsopano inu’dzanitu,
Asanapitirirepo

Post navigation

Previous: Hymn 140 NDINAMIRA m’machimo, wosaonekanso,
Next: Hymn 161 LERO lino mbale wanga,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 999 Amaliwongo ochuluka amalowa m’mtima
  • Hymn 79 Mlendo ali pakhomo,
  • Hymn 355 Tinafuna m’phirimo,
  • Hymn 211 Chakudya ichi ndi cha iwenso,
  • Hymn 664 Komwe asauka anthu
  • Hymn 494 YESU Mbusa, mutimvere,
  • Hymn 322 Walira Yesu m’dziko linoli,
  • Hymn 333 Perekani, perekani
  • Hymn 708 Peturo ‘nafusa Hananiya:
  • Hymn 108 MBUYE wondipulumutsa,
  • Hymn 869 Anatipatsa Mawu onse olimbitsa mtima;
  • Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,
  • Hymn 360 KRISTU wakuyeratu,
  • Hymn 900 Mutipatse leroli
  • Hymn 280 Tisonkhane tonsefe,
  • Hymn 1786 Ndikonda Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 1127 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja;
  • Hymn 1351 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 437 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 1039 Usafune chuma chokha,
  • Hymn 17 MULUNGU ndiye Mbusa wanga,
  • Hymn 551 Ndani kodi Munthuyo
  • Hymn 1494 Mbiri yakalelomwe,
  • Hymn 996 Leka zakuipa zako,
  • Hymn 132 MVERA mtima wanga ’we
  • Hymn 648 Mulungu wa Kumwamba,
  • Hymn 1279 Kuti munditsogolera paulendopo;
  • Hymn 1712 E! Yesu Mbuye wangadi,
  • Hymn 1656 Inu mundibisadi
  • Hymn 315 YENDANI munjira yake,
  • Hymn 473 YESU wa Kumwamba,
  • Hymn 1205 Ndikonda chifukwa
  • Hymn 1593 Wina atikonda ife,
  • Hymn 668 Achisoni, obvutidwa,
  • Hymn 884 Mndikumbutse zomwe
  • Hymn 345 ATATE, ndipempha
  • Hymn 1619 Adzabwera,
  • Hymn 1402 Mverani Iye ati: idzanitu;
  • Hymn 573 Ambuye, tikutamandani
  • Hymn 366 MADZULO aja kalero
  • Hymn 10 Kristu Mfumuyo yaulemerero!
  • Hymn 1084 “Khala mwa Ine,” munachotsa tsoka,
  • Hymn 1251 Ndasokera m’tali ndithu
  • Hymn 1083 “Khala mwa Ine,” Yesu anatero;
  • Hymn 958 Ndikalowa m’mtsinje muja,
  • Hymn 1543 Idzani, Mzimu Inu,
  • Hymn 954 Mbuye andipeza lero,
  • Hymn 1536 Ndilira Mzimu leroli,
  • Hymn 139 Bwerani inu nonse, inu nonse,
  • Hymn 195 Bwinoli tipita,
  • Hymn 71 Andiyembekeza, chinthuchi ndidziwa,
  • Hymn 300 Ona Mwanawankhosayo
  • Hymn 132 Ganizansoni, ali pano,
  • Hymn 740 Tsopano nthawi yake phwandili,
  • Hymn 634 Mtifungatire ndi mapiko paulendo pathu,
  • Hymn 654 Ndilimbikitse, Mbuye, nji!
  • Hymn 1309 Ndi inetu ndidziwedi
  • Hymn 1724 Ambuye mthandize inetu
  • Hymn 680 Mbendera yake ikupiza m’mlengalengamo,
  • Hymn 1141 Pakulekana ifetu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version