Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,

  1. Home   »  
  2. Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,

Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,

 

MKAZI wa ku Samariya,
Napita kukatunga madzi;
Pofika iyetu komweko,
Anapeza Ambuye Yesu.

Ambuye ananena:
“Ndipatseni madzi Ndimweko;
Ukanadziwa mtulo wa Mulunguyo,
Sukanandimana madzi.”

Ambuye nanena naye:
“Kayitane mwamuna wako;”
Mkazi anamuyankha nati:
“Inetu ndilibe mwamuna.”

Mkazi pochoka pomwepo,
Natsimikizatu mumtima;
Nati: “Uyu ndiye Mesiya,
Ndi Mwana wa Mulunguyotu.”

Abale tikhulupi’re,
Kuti Ambuye Yesuyo;
Ndiye Mwanadi wa Mulungu,
Ndiponso ndi Mpulumutsiyo.

Post navigation

Previous: Hymn 120 MUNDINYEMERE ’ne
Next: Hymn 141 TAONANI pamtandapo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 257 NJIRA yanga sindiziŵa,
  • Hymn 1705 Pa Iye padzapo
  • Hymn 803 Mulungu wanga, Dzuwatu
  • Hymn 1374 Inu mumvere anyamatawo,
  • Hymn 169 ’MVANI liu lomwe
  • Hymn 1615 Anakonda,
  • Hymn 1092 Ndimamva njala kuno, Yesu,
  • Hymn 419 ANYAMATA a Mulungu,
  • Hymn 490 YESU adza kuwerenga,
  • Hymn 210 PEREKANI mtima wanu,
  • Hymn 1334 Walandira inetu
  • Hymn 646 Mudalitse nyumba yathu;
  • Hymn 284 MAVUTO ndi ambiri,
  • Hymn 1278 Kuti muyeretsa mtima ndibvomeratu;
  • Hymn 252 M’dziko lino chimwemwecho
  • Hymn 1115 M’munda wa Mbuyako
  • Hymn 1229 Dzinalo la Yesu,
  • Hymn 754 Ndi mtanda uli m’maso mbuu,
  • Hymn 224 Atero ndaniyo?
  • Hymn 1211 Mwakhulupiriradi
  • Hymn 954 Mbuye andipeza lero,
  • Hymn 1782 Poyamba paja analenga
  • Hymn 198 CHITSIMECHO cha mwaziwo
  • Hymn 835 Mukhale ndine, dzuwalo lalowa,
  • Hymn 913 Kulibe gombe, nyanja,
  • Hymn 775 Mwa anthu onsewo
  • Hymn 668 Achisoni, obvutidwa,
  • Hymn 1406 Kodi ukafuna
  • Hymn 216 Ndi misozi ndi chisoni
  • Hymn 113 KALERO anthu onse
  • Hymn 195 YESU wondikondadi,
  • Hymn 29 CHIKONDI cha
  • Hymn 1138 Masiku onse m’mtima mwanga
  • Hymn 1261 Kale ndinakana Inu, Ndinathawatu;
  • Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo
  • Hymn 1666 Yesu, ndinutu chitsime
  • Hymn 1810 Kalelo Mbuye Yesu
  • Hymn 126 Mwa ine, moyo wanga ndi Yesu
  • Hymn 329 Yesu atonthoza mtima
  • Hymn 1369 Paphiri paja papakulupo,
  • Hymn 1802 Mulungu anatuma,
  • Hymn 269 NDILIRA ine kukayenda
  • Hymn 1199 Ndikhumba ine ndithu
  • Hymn 1851 Anthu onse, anthu onse,
  • Hymn 1254 Mukhululukire ine,
  • Hymn 448 Yesu ndi wofatsa,
  • Hymn 504 Pakumyamika Iye
  • Hymn 25 “Akaleka amake
  • Hymn 495 Wonga Inu ndikhaledi,
  • Hymn 1752 Napulumutsa tonse
  • Hymn 527 Idzani mumtima mwanga,
  • Hymn 783 Antchito a Mulungu ‘nu
  • Hymn 854 Timlemekeze Mlunguyu
  • Hymn 169 M’manda nagonamo
  • Hymn 1746 Mwachimwemwe, mwachisoni,
  • Hymn 445 TILIMALIMA m’minda,
  • Hymn 303 MEMA nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 1268 Mundilandiretu,
  • Hymn 288 HAYA! ’nzanga taonani
  • Hymn 1389 Tithawire kwa Mulungu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version