Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 119 M’BUKU la moyotu Mbuye,

  1. Home   »  
  2. Hymn 119 M’BUKU la moyotu Mbuye,

Hymn 119 M’BUKU la moyotu Mbuye,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 119 M’BUKU la moyotu Mbuye,

 

M’BUKU la moyotu Mbuye,
Momwe muli, kulemba;
Tandiuzanitu Mbuye,
Ngati dzina lilimo.

Lilimo dzinali,
M’Buku lanu la moyo;
Tandiuzanitu Mbuye,
Ngati linalembedwa.

Pamene ndidza kwa Inu,
Kulapa machimowo;
M’dzandikhululukiradi,
Ndikundiyeretsanso.

Ambuye mundithandize,
Paulendo wangawu;
Pakufika kuli Inu,
Mundigwire dzanjalo.

Post navigation

Previous: Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
Next: Hymn 121 MULUNGU, anthu ’fe

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 603 Mzimu wanu Wakuyera,
  • Hymn 1116 Kwawo kwa Mbuyako
  • Hymn 1752 Napulumutsa tonse
  • Hymn 341 PAKUPEMPHERATU
  • Hymn 1119 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 1803 Nowayo nayendamo,
  • Hymn 1237 Ine kanthu ndilibe
  • Hymn 1582 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo
  • Hymn 1192 Pamtanda woopsa
  • Hymn 1398 Nditama mphamvu yake
  • Hymn 482 Ndinu wakuyera,
  • Hymn 916 Akondwerera anthu
  • Hymn 107 MUBWERE kuno Mzimu ’Nu
  • Hymn 1223 Ndidzaimba za Mulungu,
  • Hymn 1363 Tamani Ambuye,
  • Hymn 257 NJIRA yanga sindiziŵa,
  • Hymn 193 A! Kumwamba
  • Hymn 174 Haya, anzathu, itilinda nkhondo;
  • Hymn 446 Yesu alandira
  • Hymn 832 Zochimwa za usana uno mndikhululukire ‘ne;
  • Hymn 1618 Anakwera,
  • Hymn 770 Atate, muwapenye
  • Hymn 62 AMBUYE Yesu,
  • Hymn 7 “Mbuye Woyera! E, Woyeranokha!
  • Hymn 208 “Lowa, lowa
  • Hymn 1414 Zonse zinathedwadi;
  • Hymn 261 Munafera pa mtanda
  • Hymn 1726 Linadetsedwa dzuwa bii!
  • Hymn 297 Anapita nasiya
  • Hymn 1798 Mukondwe anthu a Mulungu,
  • Hymn 649 Inde, tikuyamikani, Atate, leroli,
  • Hymn 874 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 340 Imvani,
  • Hymn 1475 Anathera pamtanda zintchito zonsezi
  • Hymn 1389 Tithawire kwa Mulungu,
  • Hymn 119 M’BUKU la moyotu Mbuye,
  • Hymn 333 Perekani, perekani
  • Hymn 1842 Pabande lolunjika andilondolera njira;
  • Hymn 779 Yesu Mbuye wanga,
  • Hymn 594 Monga may’ asusuza
  • Hymn 126 DAVIDE kubusa kuja,
  • Hymn 845 Ufumu wanu, Mbuye Yesu,
  • Hymn 1042 Zonse umazinyadira
  • Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,
  • Hymn 1514 Dzinthu zakumundazo
  • Hymn 1814 Thupi lamwazi wathu’li
  • Hymn 607 Dziko lonse lilikukondwa, mlengalenga mpheponso,
  • Hymn 1466 Ambuye wathu Yesu
  • Hymn 1651 Kwa Mulungu m’Mwambamo
  • Hymn 301 MBUYE, ndapangana
  • Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 370 Pakuti Mbuye Mlunguyo
  • Hymn 446 YAMIKANI nonse ’nu,
  • Hymn 453 Tiana ta Ambuye tili
  • Hymn 139 MLUNGU anapatsa moyo,
  • Hymn 137 UTHENGA wa Ambuye
  • Hymn 1419 Amayi ‘nu, amayi ‘nu,
  • Hymn 1230 Lichiza mzimu wophwetekwa ukakhale bata,
  • Hymn 98 Ndidzamwona maso ndi maso

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version