Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;

  1. Home   »  
  2. Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;

Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;

 

YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;
Wanyenga bambo ake
Kuti, “Inetu ndinetu
Esau mwana wanu.”

Esau analira, “abambo
Inu, abambo anga,
Ndabwera nayo nyama,
Mulandire, mudye.”

Thupi ndi Esau, koma mawuwo,
Ngatitu a Yakobo;
“Bwera mwana wanga,
Bwera pafupi n’kusisite.”

Ndapezatu bwenzi latsopanolo,
Ndi Yesu Mpulumutsi;
Yemwe angathe, kuchotsa,
Machimo anga onse.

Machimo andizunza ine;
Mtima mwangamu inedi,
Ndifuna Inu Mbuye,
Mulowe m’mtima mwanga.

Post navigation

Previous: Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
Next: Hymn 121 MULUNGU, anthu ’fe

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 407 ADZAPAMBANA Yesu ponse
  • Hymn 1664 Ndigwadira Inu, Yesu,
  • Hymn 1829 Mulungu ndiye Mbusa wanga, sindisowa konse;
  • Hymn 966 Kodi inu, aulendo,
  • Hymn 353 Anatuma Mtetezi,
  • Hymn 1784 Komweko titasaukira,
  • Hymn 1630 Anthu anu amafoka,
  • Hymn 777 Mulungu ali muno,
  • Hymn 730 A! Yesu mwapangana
  • Hymn 255 Pakuona imfayo
  • Hymn 1281 Ndikhulupirira, Yesu, mndibvomereko;
  • Hymn 124 Aliponso adani am’kati ndi akunja;
  • Hymn 1276 Ndikhulupirira, Yesu, Inu nokhadi
  • Hymn 1079 Khalatu woyera,
  • Hymn 1653 Mulungu ali wokhulula mtimatu,
  • Hymn 988 Ndikhumba Mzimu wanu
  • Hymn 1619 Adzabwera,
  • Hymn 399 M’KHOLA mwa ng’ombe ku Betlehemu
  • Hymn 574 A! Yesu Mbuye wakuyera,
  • Hymn 522 Akazi anadza
  • Hymn 599 Mlengi wathu Wakuyera,
  • Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
  • Hymn 814 Mutichiritse ifenso
  • Hymn 1172 Adzabweranso
  • Hymn 483 Ndife akuchoka,
  • Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 1186 Yesu anafa pamtandapo,
  • Hymn 488 M’MANJA a Yesu wanga
  • Hymn 1228 Lindikomera dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 724 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 1122 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 1855 Yesu, msandipitirire
  • Hymn 1555 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 252 M’dziko lino chimwemwecho
  • Hymn 1197 Ndafoka ine kale,
  • Hymn 497 Yesu andikonda ine,
  • Hymn 1492 Sakukanani Yesudi,
  • Hymn 1092 Ndimamva njala kuno, Yesu,
  • Hymn 1063 Pokhala mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 22 Mbuye mtsitsimutse!
  • Hymn 413 ZIPATA zachitsulo zitseguke zonse mbee!
  • Hymn 1373 Zamoyo zili m’thengo zonsezo,
  • Hymn 292 NDIPULUMUTSENI Mbuye,
  • Hello world!
  • Hymn 1498 Simbani Mbiri yonse
  • Hymn 36 AMBUYE tsopano lino, monga mwa mawu anu aja,
  • Hymn 108 MBUYE wondipulumutsa,
  • Hymn 1390 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 1297 Kumwamba komwe n’dzaimbira
  • Hymn 1381 Ndi mitima yokondwera
  • Hymn 369 Lowani m’nyumba mwakemu
  • Hymn 373 Ayamikire ‘Nu
  • Hymn 1354 Mzimu Woyera, m’mtimamo
  • Hymn 1816 Anatikondakonda ‘Ye,
  • Hymn 923 Dothili kudothilo,
  • Hymn 1030 Tioperanji ifetu?
  • Hymn 151 Inde, Yesu, mulandira,
  • Hymn 1519 M’Buku lakuyerali
  • Hymn 1246 Ambuyanga, ndalephera,
  • Hymn 1021 Kunsi kudambo, pena m’mwamba m’phirimo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version