Hymn 1213 Mwamva Yesu m’mtimamo, December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Believers Christian Hymns Chichewa Believers Christian Hymns Hymn 1213 Mwamva Yesu m’mtimamo, Mwamva Yesu m’mtimamo, Adzanso kawiri, M’mene ali nanutu Muli ndi chimwemwe. Ntchito zachifundozi Iye watha izi, Kuti mwawo m’Mwambamo Naye tikhalebe.