Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 1213 Mwamva Yesu m’mtimamo,
Mwamva Yesu m’mtimamo,
Adzanso kawiri,
M’mene ali nanutu
Muli ndi chimwemwe.
Ntchito zachifundozi
Iye watha izi,
Kuti mwawo m’Mwambamo
Naye tikhalebe.
Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 1213 Mwamva Yesu m’mtimamo,
Mwamva Yesu m’mtimamo,
Adzanso kawiri,
M’mene ali nanutu
Muli ndi chimwemwe.
Ntchito zachifundozi
Iye watha izi,
Kuti mwawo m’Mwambamo
Naye tikhalebe.