Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 467 NGOLIZO zilira

  1. Home   »  
  2. Hymn 467 NGOLIZO zilira

Hymn 467 NGOLIZO zilira

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 467 NGOLIZO zilira

 

NGOLIZO zilira
Za ’mithengawo,
Ndi zipata zonse
Zatsegudwa mbee!
Kristu, Mfumu yathu,
Mbuye wathudi,
Wapambana monse,
Alamulabe.

Ntchito zake zatha,
Timwimbiretu;
Yesuyo wakwera,
Timtamandetu.

’Natipulumutsa
Natiferako,
Ali mfumu ndithu
Kwa Atatewo;
Osasautsidwa,
Osafanso ’yi
Yesu, Mfumu yathu
Adakweradi.

Atipempherera
M’malo ’dalawo,
Tinke kwathu komwe
Ndi chisomocho;
Akonzera malo
Ana akewo;
Yesu alipobe,
Atikondanso.

Post navigation

Previous: Hymn 466 OSANATU, osana,
Next: Hymn 468 NDIKONDWA kuti

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 330 N’LOKOMA Dziko langa!
  • Hymn 1393 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 459 KALE anthu m’kholamo,
  • Hymn 345 Ubwere,
  • Hymn 1271 Onani Mbuye ndigonja,
  • Hymn 1202 Ndikhumba mtimawo
  • Hymn 620 Mphatso zonse zathu
  • Hymn 827 Wonsewu usiku
  • Hymn 484 YESU ndiye Mbusa,
  • Hymn 447 OYAMIKA Mlungu m’bwere,
  • Hymn 425 Ine ndine mlendo
  • Hymn 278 Aweruza ndi mphamvu
  • Hymn 171 IWE tiye, iwe tiye,
  • Hymn 1504 Kodi ali ndi chilemba
  • Hymn 475 Mbuye ndikhaletu
  • Hymn 1457 Ndidziwa kuti Yesu
  • Hymn 537 Aleluya! Aleluya!
  • Hymn 940 Ndamvatu kuti tifika komweko
  • Hymn 320 Ambuye, wakuti ndi mwaziwo
  • Hymn 1328 Ndani afuna kunkako
  • Hymn 544 Zoopsya sitidziwapo
  • Hymn 230 Ndisamba ndiyera,
  • Hymn 319 NDIDZATANI ine,
  • Hymn 534 Bwerani, kondwerani,
  • Hymn 396 PETURO ’nafunsa Hananiya:
  • Hymn 506 Ndikondwa kuti Yesu akonda,
  • Hymn 937 Chitsime chachikondi
  • Hymn 1524 Ndiwo alimbitsa
  • Hymn 1229 Dzinalo la Yesu,
  • Hymn 830 Atate ndiyamika, mwandisamalira leroli;
  • Hymn 1463 Zoipa zakhululukidwa,
  • Hymn 786 Yesu mkhale nafe
  • Hymn 1255 Chitha nchiani kund’yeretsa?
  • Hymn 149 Ndisauka, sindikhoza
  • Hymn 271 Zoipa zangazi
  • Hymn 135 Kudziwa ukudziwa,
  • Hymn 199 NDINASOKERA kutali,
  • Hymn 1314 Mulungu ali nane!
  • Hymn 1472 Ona! Ona! Onatu!
  • Hymn 1358 Lemekeza Mfumu yathu,
  • Hymn 695 Pomveka konsekonse mbiri
  • Hymn 836 Kamoyo kanga katha lero lino,
  • Hymn 1027 Tithawiranji ifetu?
  • Hymn 847 Konse kuli mdima bii
  • Hymn 780 Kwezani mitu yanuyo,
  • Hymn 204 NDASIYA zonse ndi Yesu kalelo,
  • Hymn 470 YESU andikonda ine,
  • Hymn 1148 Ndiimba mumtima mokondwa
  • Hymn 296 Mngelo anatumidwa
  • Hymn 1214 Mwamva Mzimu wakewo,
  • Hymn 1759 Powalitsira omwe
  • Hymn 1590 Mtima ndimakondweramo,
  • Hymn 978 Mtima wanu wonse ndithu
  • Hymn 699 Inu wakudzatu
  • Hymn 875 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 1109 Pamene ndisauka,
  • Hymn 1120 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 1047 Ambuye, chotsani zonse zomwezo
  • Hymn 896 Mbuye, ndinalema ine,
  • Hymn 1384 Mphamvu yake inalenga

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version