Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 408 ABALE nonse mulindiranji?

  1. Home   »  
  2. Hymn 408 ABALE nonse mulindiranji?

Hymn 408 ABALE nonse mulindiranji?

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 408 ABALE nonse mulindiranji?

 

ABALE nonse mulindiranji?
Bweranitu kwa Yesuyo;
Ali kuyitana inu nonse,
Ndithu bweranitu.

Mvetsa mbale moyo ukutha,
Dziko lingonkabe;
Siya zonse bweratu we,
Yesu adzakondwa.

Tiyeni tonse tilimbiketu,
Kubukitsa Uthengawo;
Womwe Ambuye anadza nawo,
Tisakhale chete.

Tiyeni tifalitse mawuwo,
Tisabise Uthengawo;
Yesu anatiferatu tonse,
Kutipulumutsa.

Post navigation

Previous: Hymn 400 ONA Mwana wa Nkhosa,
Next: Hymn 421 ANTHU ali m’mdima akuyitanitsa,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 57 Ife tiyembekezera Yesu,
  • Hymn 588 Mlungu, Inutu,
  • Hymn 1616 Anafera
  • Hymn 405 POLENGA dzikoli
  • Hymn 70 Mbuye ndinu bwenzi langa ndithu,
  • Hymn 1646 M’busa wokoma ndi Mbuyangayo,
  • Hymn 257 NJIRA yanga sindiziŵa,
  • Hymn 573 Ambuye, tikutamandani
  • Hymn 954 Mbuye andipeza lero,
  • Hymn 53 Dalitsani mafumu athu,
  • Hymn 1683 Nsinga za imfa Iye ‘nadula,
  • Hymn 1423 Oipa inu nonsetu,
  • Hymn 58 PAMTANDAPO Ambuyeyo
  • Hymn 1213 Mwamva Yesu m’mtimamo,
  • Hymn 50 Akhristu nyamulani
  • Hymn 662 Tisaleme pakuchita zabwinozi,
  • Hymn 1281 Ndikhulupirira, Yesu, mndibvomereko;
  • Hymn 192 Apita anzathu dzuwa lino Kosaoneka,
  • Hymn 1228 Lindikomera dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 1766 Ndilikulemekeza
  • Hymn 952 Ndimayenda paulendo,
  • Hymn 547 Anatikondakonda ‘Ye.
  • Hymn 1326 A! Mbusa wathu amvatu
  • Hymn 1775 Oonadi mtima,
  • Hymn 18 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 978 Mtima wanu wonse ndithu
  • Hymn 60 Chitetezo chachikulu
  • Hymn 745 Anatifera nsembe Iyeyo,
  • Hymn 785 Yehova adalitse ‘nu,
  • Hymn 1512 Cholimbitsa mtima ndi
  • Hymn 1447 Yesu ngwachifundodi,
  • Hymn 1176 Sandinyenga, salephera;
  • Hymn 346 Aitana,
  • Hymn 1364 Uzani zamphamvu,
  • Hymn 1182 Chikhulupiro chomwenso
  • Hymn 364 DZUŴA lapitira,
  • Hymn 337 ‘Tate ‘Nu,
  • Hymn 1765 Zoonazi amithenga
  • Hymn 950 Sindidapempha kale Mbuye ‘yi,
  • Hymn 598 Mlungu ali nane;
  • Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,
  • Hymn 1414 Zonse zinathedwadi;
  • Hymn 914 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 308 AULENDO, munka kuti
  • Hymn 1695 Pokumbukira mtandawo
  • Hymn 809 Madzulo aja kalelo
  • Hymn 1106 Mlungu ndi wachikhalire.
  • Hymn 747 Tadzanitu, okhulupiradi,
  • Hymn 1278 Kuti muyeretsa mtima ndibvomeratu;
  • Hymn 480 TIANA ife tingofoka,
  • Hymn 808 Atipsinjadi masoka,
  • Hymn 109 Chiyembekezo changacho
  • Hymn 1816 Anatikondakonda ‘Ye,
  • Hymn 1450 Ndi angelo akumwamba
  • Hymn 1475 Anathera pamtanda zintchito zonsezi
  • Hymn 62 Tchimo lonse ligonjera
  • Hymn 516 Zitsamba zakuyera
  • Hymn 596 Mlungu ali nane;
  • Hymn 378 KWEZANI mitu yanuyo,
  • Hymn 1346 Ndaima pano, ndaima pakhomo:Lowa, lowa, lowa, lowa!

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version