Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 401 A MULUNGU,

  1. Home   »  
  2. Hymn 401 A MULUNGU,

Hymn 401 A MULUNGU,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 401 A MULUNGU,

 

A MULUNGU,
Munatuma Yesuyo,
Mwana wanu Yekhayo.

Anabadwa,
Anabadwa motere,
Monga mmphaŵi m’kholamo.

Anakonda
Anakonda anthuwo,
Naŵapulumutsanso.

Anafera,
Anafera m’mtandamo,
Anafera ifenso.

Anadzuka
Anadzuka m’mandamo,
Anatenga moyowo.

Anakwera,
Anakwera m’Mwambamo
Kwa Mulungu ’Tatewo.

Adzabwera,
Adzabwera Iyeyo
Tsiku lomalizalo.

Aleluya,
Aleluya Yesuyo,
Tizitama dzinalo.

Post navigation

Previous: Hymn 400 ONA Mwana wa Nkhosa,
Next: Hymn 421 ANTHU ali m’mdima akuyitanitsa,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1568 Kudzoza kwanu kutipatsa
  • Hymn 921 Komwe Mbusa kwawoko
  • Hymn 659 Anthu ali m’mdima akuitanitsa
  • Hymn 1363 Tamani Ambuye,
  • Hymn 1005 Mdani adza nazo mphamvu,
  • Hymn 1018 Yesu afuna iwe unnke kwawoko,
  • Hymn 326 TSIKU Iidzafika mbale,
  • Hymn 1036 Mtima wakufatsa
  • Hymn 132 MVERA mtima wanga ’we
  • Hymn 1122 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 202 Timpemphere kutipatsa
  • Hymn 304 POZUNZIDWA inu ponseponse
  • Hymn 1182 Chikhulupiro chomwenso
  • Hymn 835 Mukhale ndine, dzuwalo lalowa,
  • Hymn 1059 Kalelo m’mtima ndinakondwa,
  • Hymn 713 Ambuye, Mwini zonsezi,
  • Hymn 350 Yesu ati,
  • Hymn 321 Ndi ponse paphiri ndi padambopo
  • Hymn 439 MLUNGU wathu mwatifitsa
  • Hymn 1004 A! mizimu yakuipa
  • Hymn 952 Ndimayenda paulendo,
  • Hymn 501 Yesu andikonda ine;
  • Hymn 43 Ulendo wathu ukadzatha
  • Hymn 1816 Anatikondakonda ‘Ye,
  • Hymn 29 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 419 ANYAMATA a Mulungu,
  • Hymn 129 WODALA ndiye munthuyo,
  • Hymn 1086 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini moyo,
  • Hymn 1680 Aleluya, Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 259 CHISOMO chodabwitsacho,
  • Hymn 840 Ambuye munapatsa tsiku
  • Hymn 375 Zipatso zakezi
  • Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,
  • Hymn 317 Zambiri zagona m’kholamo,
  • Hymn 58 Titasokera tinabwerera,
  • Hymn 839 Adani sindiopa mukalipo;
  • Hymn 1765 Zoonazi amithenga
  • Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,
  • Hymn 1550 Kutiyeretsa m’mtima
  • Hymn 1812 Kuzani Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 1735 “Sezani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 220 Kalekale ndinathawa,
  • Hymn 73 Mu ulemerero tidzakhala m’yaya,
  • Hymn 827 Wonsewu usiku
  • Hymn 498 Yesu akonda,
  • Hymn 1403 ‘Mvani liwu lomwe
  • Hymn 1117 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 1423 Oipa inu nonsetu,
  • Hymn 404 Dzuwa la lero lonseli
  • Hymn 201 Ngati zakuipa zathu
  • Hymn 266 Ukondwere moyo wanga,
  • Hymn 1610 Waleka koronayo,
  • Hymn 752 Chakudya chakumwambachi
  • Hymn 1507 Ndikampempha anditenge,
  • Hymn 1458 Satana ndi unyolo
  • Hymn 11 Imfa mutagonjetsa ndi zowawa,
  • Hymn 1388 Tiimbire Mlungu wathu
  • Hymn 841 Mukhale, mukhale,
  • Hymn 950 Sindidapempha kale Mbuye ‘yi,
  • Hymn 587 Mutitsuke,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version