Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 374 NDI lokoma m’Mwambamo,

  1. Home   »  
  2. Hymn 374 NDI lokoma m’Mwambamo,

Hymn 374 NDI lokoma m’Mwambamo,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 374 NDI lokoma m’Mwambamo,

 

NDI lokoma m’Mwambamo,
Mbuye, Bwalo lanulo;
Ndi mwabwino muli ’Nu
Dziko losachimwali;
Mtima wana wonsewu
Umakhumba m’Mwambamo
Nkhope ya Mbuyathuyu,
Mlungu wa chisomoyo.

Zimbalame zonsezi
Zimayamikira ’Nu;
Anthu amakondwanso
Okhumbira m’Mwambamo;
Njiŵa yosapumayo
Inafika m’chombocho;
Okhulupirira ’Nu
Amapuma kwanuno.

Anthu opembedzawo
Amakondwa m’mtimamo;
Munapatsa madzitu,
Munagwetsa manawo;
Mumakoma mtimatu
Tidzayamikiratu,
Pachimpando chanucho
Mkhale Mfumu yathudi.

Post navigation

Previous: Hymn 360 KRISTU wakuyeratu,
Next: Hymn 381 MONGA zomera zonsezo

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 172 TADZA kukudyaku,
  • Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 101 Lodala tsiku lomwelo
  • Hymn 1100 Inde wakukonda ndinu;
  • Hymn 947 Akristu tonsefe, tikondwe m’Dzikoli
  • Hymn 914 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 334 KULI dziko labwino M’mwamba,
  • Hymn 1494 Mbiri yakalelomwe,
  • Hymn 473 YESU wa Kumwamba,
  • Hymn 504 Pakumyamika Iye
  • Hymn 443 Tchimo musalole,
  • Hymn 720 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1271 Onani Mbuye ndigonja,
  • Hymn 989 Yochita ndi yodikha
  • Hymn 316 Ndikhazikike inetu,
  • Hymn 467 NGOLIZO zilira
  • Hymn 315 YENDANI munjira yake,
  • Hymn 926 Mbale wako unamkonda,
  • Hymn 1643 Kufuna inetu, kufuna inetu,
  • Hymn 1428 Penyetsetsa Yesu
  • Hymn 81 Imva mawu akewo,
  • Hymn 124 Aliponso adani am’kati ndi akunja;
  • Hymn 725 Munafera ine kale
  • Hymn 1328 Ndani afuna kunkako
  • Hymn 186 MVERANI mbiri yozizwitsa
  • Hymn 719 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 757 Sindili woyenera ‘ne;
  • Hymn 1146 Khalani duu! Pakufa mnzathuyo,
  • Hymn 80 Utsegule mtimawo,
  • Hymn 82 Mlendo wa Kumwambayo
  • Hymn 1244 Nthawi ilikudza yonse
  • Hymn 339 Tipempha,
  • Hymn 171 M’manda munalibe
  • Hymn 501 Yesu andikonda ine;
  • Hymn 821 Aleluya!
  • Hymn 64 Mantha, nkhawa, ndi chisoni
  • Hymn 310 Tafika kwa inu mutiunikire,
  • Hymn 1501 Inde, pakufa panga
  • Hymn 409 Yesu adza kuwerenga
  • Hymn 159 YESU ndi wokonda,
  • Hymn 309 ANA akumwamba ndife,
  • Hymn 270 Zoopsya zopambana
  • Hymn 151 Inde, Yesu, mulandira,
  • Hymn 868 Atate yemwe anatuma Mpulumutsi mmodzi
  • Hymn 34 Yesu Mbuyetu, mwafera
  • Hymn 112 Pangano lake m’mwaziwo
  • Hymn 188 Ine ndili ndi manyazi
  • Hymn 882 Kodi tikulema nazo
  • Hymn 409 ANTHU akum’maŵa
  • Hymn 204 NDASIYA zonse ndi Yesu kalelo,
  • Hymn 1564 Mufike monga moto wakuotcha zomwezo.
  • Hymn 255 Pakuona imfayo
  • Hymn 686 Imbadi za Iyeyo,
  • Hymn 1722 Ambuye tikondweratu
  • Hymn 1631 Mudzabwera, mudzabwera;
  • Hymn 1626 Mbuye Yesu adzabwera,
  • Hymn 114 Ndine Mbusayo wabwino,
  • Hymn 998 Anatilemba Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,
  • Hymn 1733 Adzabwera Iyenso

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version