Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 374 NDI lokoma m’Mwambamo,

  1. Home   »  
  2. Hymn 374 NDI lokoma m’Mwambamo,

Hymn 374 NDI lokoma m’Mwambamo,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 374 NDI lokoma m’Mwambamo,

 

NDI lokoma m’Mwambamo,
Mbuye, Bwalo lanulo;
Ndi mwabwino muli ’Nu
Dziko losachimwali;
Mtima wana wonsewu
Umakhumba m’Mwambamo
Nkhope ya Mbuyathuyu,
Mlungu wa chisomoyo.

Zimbalame zonsezi
Zimayamikira ’Nu;
Anthu amakondwanso
Okhumbira m’Mwambamo;
Njiŵa yosapumayo
Inafika m’chombocho;
Okhulupirira ’Nu
Amapuma kwanuno.

Anthu opembedzawo
Amakondwa m’mtimamo;
Munapatsa madzitu,
Munagwetsa manawo;
Mumakoma mtimatu
Tidzayamikiratu,
Pachimpando chanucho
Mkhale Mfumu yathudi.

Post navigation

Previous: Hymn 373 NYUMBA ya Mulungu, ili pano,
Next: Hymn 375 YESU m’khale nafe

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 572 Anadza nazo mphatso zake
  • Hymn 952 Ndimayenda paulendo,
  • Hymn 213 INE ndili ndi manyazi
  • Hymn 267 AMBUYE, thandizenitu
  • Hymn 73 M’SANDIPITILIRE Yesu,
  • Hymn 483 Ndife akuchoka,
  • Hymn 343 ZOKOMA ndithu nthaŵizi
  • Hymn 898 Mndidziwitse ntchito yanga,
  • Hymn 89 INDE, ndifuna kumvatu,
  • Hymn 855 Aulendo amayenda
  • Hymn 723 Mundimvere, Mbuye wanga
  • Hymn 799 Inu Mlungu kalelo
  • Hymn 315 YENDANI munjira yake,
  • Hymn 120 MUNDINYEMERE ’ne
  • Hymn 37 YESU analikhanda
  • Hymn 49 Ndi ife akudziwa
  • Hymn 921 Komwe Mbusa kwawoko
  • Hymn 407 ADZAPAMBANA Yesu ponse
  • Hymn 1 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 730 A! Yesu mwapangana
  • Hymn 382 M’wabatize anzathuwa,
  • Hymn 68 Kwathu ndidzaimba nyimbo
  • Hymn 550 Wosauka Iyedi
  • Hymn 153 Pemphero ndiko kufuna,
  • Hymn 816 Mdima wafika,
  • Hymn 534 Bwerani, kondwerani,
  • Hymn 60 Chitetezo chachikulu
  • Hymn 61 Ndi chimwemwe ndimaona
  • Hymn 1424 Malo anachepa,
  • Hymn 728 A! Yesu, ndapangana
  • Hymn 345 Ubwere,
  • Hymn 335 Mtembenuke mtima wanu,
  • Hymn 566 Ana inu, ana inu,
  • Hymn 1272 Muyambe ntchito yanuyi,
  • Hymn 668 Achisoni, obvutidwa,
  • Hymn 282 Ine ndili munthu
  • Hymn 78 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 323 Tiwaliretu, tiwaliretu
  • Hymn 33 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 283 Ndalema ndathodwa
  • Hymn 121 Imbira!
  • Hymn 217 E! kwa Inu, E! kwa Inu!
  • Hymn 713 Ambuye, Mwini zonsezi,
  • Hymn 1213 Mwamva Yesu m’mtimamo,
  • Hymn 1789 Nditani ine kubwezera Mbuye
  • Hymn 1817 Ndi m’munda muja chete, phee!
  • Hymn 136 Atumwi atummika, atumika,
  • Hymn 295 Kubadwa kwa Yesu
  • Hymn 1572 Mumbveke, mbveke, mbveke,
  • Hymn 885 Mndimvetse chisoni
  • Hymn 1644 Popachikidwa pa Golgotapo
  • Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,
  • Hymn 91 NDITAME Mlungu m’mtimamo,
  • Hymn 615 Yamikani nonse ‘nu,
  • Hymn 596 Mlungu ali nane;
  • Hymn 1221 Bwenzi ndinamkomanayo,
  • Hymn 327 NTCHITO yonse yakeyo
  • Hymn 1683 Nsinga za imfa Iye ‘nadula,
  • Hymn 279 MBUYE, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 980 Tiyeni ku nkhondo iyi,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version